Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Atsutsa Kuti Pulezidenti Akunyoza Anthu Osawona

$
0
0

Bungwe la Malawi Union of the Blind latsutsa malipoti akuti mtsogoleri wa dziko lino Professor Peter Mutharika akumanyoza anthu osawona pa misonkhano ya ndale ngakhalenso ya boma.

Wapampando wa bungweli a Ezekiel Kumwenda alankhula izi poyankhapo pa zomwe anthu ena akunena kuti Professor Peter Mutharika akumanyoza anthu osawona.

Iwo ati akukhulupilira kuti m’malakhulidwe a mtsogoleri wa dziko linoyu akumatanthauza kusazindikira kapena kugwira ntchito mobwelera m’mbuyo osati kunyoza anthu osawona.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>