Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

A Mugabe Akuti Akufuna Kulandanso Minda Ina Ya Alimi A Chizungu

$
0
0

M’tsogoleri wa chipani chotsutsa boma cha The Movement For Democratic Change a Morgan Tsvangirai m’dziko la Zimbabwewa dzuzula m’tsogoleri wa dzikolo president Robert Mugabe kaamba kamphekesera yoti akufuna kulanda mwa mtopola minda ina ya alimi achizungu m’dzikolo.

Malinga ndi malipoti a News 24 ati a Morgan Tsvangiraiawuza a Mugabe kuti ndibwino kuti abwere ndi njira zina zothandizira pa ntchito zokweza chuma cha dzikolo ndi kupewa kulandi minda ya alimi a achizungu.

Iwo ati ngati a Mugabe atachitenso izi ndiye kuti zithandizira kukolezera mavuto a zachuma omwe ali m’dzikomo.

Dziko la Zimbabwe ndi limodzi mwa mayiko a u Africa amene analanda minda ya azungu kamba ka nkhani za ndale.  


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875