Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Chiphwanya ndi Mlembi Watsopano wa CCJP

Aku likulu la mpingo wakatolika mdziko muno alengeza za kusankhidwa kwa a Martin Chiphwanya kukhala mlembi wa bungwe la chilungamo ndi mtendere m’dziko muno. A kulikulu la mpingo-wu ndi omwe alengeza...

View Article


Chaka cha Achinyamata pa Dziko Lonse 2019 Chidzachitikira Mdziko la Panama

Mpingo wakatolika m’dziko la Panama wati ndi wokondwa ndi uthenga umene walandira woti chaka cha achinyamata mu mpingowu pa dziko lonse chidzachitikire  mdzikomo. M’tsogoleri wa mpingo wakatolika pa...

View Article


Papa Fransico Aikiza Mmapemphero Akhristu Omwe Aphewdwa Mdziko La Egypt

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse PAPA FRASISCO anaikiza mmapemphero akhristu a mpingo wina wachikhristuomwe avulazidwa komanso kuphedwa ndi a chiwembu mdziko la EGYPT. Akhristuwa...

View Article

Mtsogoleri Wa Chipani Cha Umodzi Ayamikira Boma

Chipani chotsutsa boma cha Umodzi chati sichikuonapo kulakwikwa kuli konse pa nkhani yoti alimi adzigulitsa chimanga chawo kwa Mavenda. Mtsogoleri wachipanichi PROFESSOR JOHN CHISI ndi amene wanena izi...

View Article

Nsomba Ya Shark Ivulaza Nsodzi Mdziko La Australi

Msodzi wina wavulala kwambiri mdziko la AUSTRALIA boti lomwe amapalasa mutalowa chi nsomba chotchedwa shark cholemera makilogram 200. Malinga ndi malipoti a BBC mwamunayu TERRY SELWOOD(SIWUDU) wa zaka...

View Article


Abwenzi Amalitiri aku Uganda aku Malawi Apita ku Uganda

Abwenzi a AMALITIRI a ku UGANDA a kuno ku MALAWI motsogozedwa ndi episcope wa dayosizi ya mpingo wakatolika ya Mangochi Ambuye Montfort Stima ali nawo ku mwambowu. Akhristuwa adachoka mdziko muno pa 27...

View Article

Mwambo Wopereka Ma Degree ku ICI

Mwambo wopereka ma degree kwa ophunzira omwe amaliza maphunziro awo a Philosophy ku  International Congregation Institute (ICI) m’boma la Balaka wachitika loweluka pa 3 June  Chaka chino. Mmawu awo...

View Article

Phalombe Catholic Parish has called upon well wishers to help in cons

The Parish Priest father Clifford Chiwanda made the call during a Fundraising paper Sunday that was held on Sunday 7th August 2016. The fundraising activity was aimed at sourcing funds to finish the...

View Article


Awapempha Kuti Adzizipeleka Pokweza Ntchito Za Bungwe La Charismatic Renewal

Amsembe m’dziko muno awapempha kuti adzizipeleka pofalitsa mauthenga a ntchito zokweza bungwe la catholic charismatic renewal ndi cholinga choti  lifalikire ponseponse mdziko muno. Bambo Bernard Tiyesi...

View Article


A Mugabe Akuti Akufuna Kulandanso Minda Ina Ya Alimi A Chizungu

M’tsogoleri wa chipani chotsutsa boma cha The Movement For Democratic Change a Morgan Tsvangirai m’dziko la Zimbabwewa dzuzula m’tsogoleri wa dzikolo president Robert Mugabe kaamba kamphekesera yoti...

View Article

Akatekist A Ku Malawi Defense Force Apuma Pa Ntchito Yawo

Yemwe anali Katekist  ku Malawi Defense Force a Benard Mukhula ku Zomba awayamikira kamba kodzipeleka pa ntchito yawo yotumikira mulungu kudzera mu mpingo wakatolika. Bambo Augustine Likado ndi omwe...

View Article

Papa Francisco Wapempha Akhristu Kuti Azikhala Patsogolo Pakugwira Ntchito Za...

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse PAPA FRANCISCO wapempha akhristu kuti azikhala patsogolo pakugwira ntchito za chifundo kwa anthu ovutika ndi osowa. Papa amalankhula izi pa mwambo wa...

View Article

Bungwe CWO Lilongwe Lipindula Ntchito Za Bungwe La TIVET

Bungwe La Technical Entrepreneur And Volcation Education And Training Authority (TIVET) lati lipitiliza kugwira ntchito zake ndi bungwe la amayi achikatolika mu arch-dayosizi ya Lilongwe. Mkulu wa...

View Article


Bungwe La MHRC Lalimbikitsa Ofesi Ya Social Welfare Kuti Isachite mantha...

Bungwe la Malawi Human Rights Commission lalangiza akuluakulu omwe amaona za ma ufulu a ana ku ofesi yoona za chisamaliro cha wanthu ya Social Welfare m’boma la Zomba kuti azigwira ntchito yawo mopanda...

View Article

Mbava Zoopsa Azigwira Mboma La Mchinji.

Apolisi m’boma la Mchinji agwira anthu atatu  omwe akuwaganizira kuti ndi mbava zoopsa kwambiri zomwe zakhala zikubera anthu m’madera osiyanasiyana m’bomalo. Ofalitsa nkhani za apolisi m’bomalo...

View Article


Papa ndi Okhudzidwa ndi Kusowa kwa Mtendere Mdziko la Syria

M’tsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Fransiskowati ndi wokhudzidwa ndi mavuto akusowa kwa mtendere omwe anthu a m’dziko la Syria akupitilira kukumana nawo. Papa wati magulu omwe...

View Article

Mpingo Wakatolika Ugwira Ntchito Zake Ndi Achinyamata

Msonkhano wowunikira momwe ntchito za achinyamata zikuyendera mu Dayosizi ya mpingo wakatolika ya Mangochi wachitika tsopano. Nthumwi zomwe zimakhudzidwa ndi nkhani zokhudza utumiki wa achinymatawu...

View Article


Anthu okwana 43 Afa Pangozi Ya Basi

Anthu okwana 43 afa ndipo ena ambiri avulala pa ngozi ya basi yomwe anakwera itagubuduzika mdera la Nyamakete ku Hurungwe  m’dziko la Zambia. Malingana ndi ofalitsa nkhani za apolisi m’dzikomo  Charity...

View Article

Amuna Awiri Amangidwa Ku Nsanje

Apolisi m’boma la Nsanje akusunga m’chitolokosi amuna awiri kaamba kowaganizira kuti anapha Njati mu nkhalango ya boma ya Mwamvi Game Reserve. Ofalitsa nkhani za apolisi m’bomalo  Sargent Agnesi...

View Article

Papa Wapepesa Dziko la Mexico, America

Mtsogoleri wa mpingo wa katolika pa dziko lonse Papa Fransisko wapereka  uthenga wachipepeso kwa anthu omwe akhuzidwa ndi mphepo ya mphamvu yomwe yakhuza anthu a m’maiko a Mexico komanso America....

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>