Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Anthu 7 Afa Pa Ngozi Ku Ntcheu

$
0
0

Anthu asanu ndi awiri 7 afa ndipo ena avulala  basi yomwe anakwera itagwa  pa Mlangeni  m`boma la Ntcheu.

Wofalitsa nkhani za apolisi m`bomali a Gift Matewere atsimikiza zankhaniyi  ndipo ati basiyi  yomwe nambala yake ndi   NA 4430      ya  kampani ya   Premier imachokera ku Blantyre kupita ku Lilongwe .

Iwo ati dalaiva wa basiyi a Richard Nyirenda azaka 40  anapephera kukhota pamalo ena kaamba koti panthawiyo amagona zomwe zinachititsa kuti basiyo isemphe msewu ndikugwa. 


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>