Anthu a m’boma la Zomba awalimbikitsa kuti asanyozere koma kuti akalembetse mayina awo mkaundula wa ziphatso za umzika.
Mkulu wa mu ofesi ya bwana mkumbwa pa nkhani za zakalembera a Tobias Lutepo ati kalembela-yu ndi wofuna kwambiri kamba koti azathandiza kuti anthu a m’bomalo akhaledi m’dzika zeni zeni za dziko lino.
Kalembera wa umzika mboma la Zomba akuti ayamba posachedwapa mbomalo.