Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Msonkhano wa bungwe la CWO Mu Dayosizi Ya Zomba

$
0
0

Msonkhano wa amayi a wakatolika mu dayosizi ya zomba wayamba pa 31 August 2017 ndipo udzatha pa  3 September 2017.

Polankhula potsekulira msonkhano-wu Episikopi wa mpingo wakatolika mu dayosizi-yi ambuye Gorge Desmond Tambala wayamikira m’gwilizano wa m’phamvu umene amayi-wa akuonetsa pa ntchito zotukula mpingo wakatolika mu dayosizi-yi.

Iwo alimbikitsa amayi-wa kuti pomwe akuchita mkumano-wu akumbukilenso kukambirana njira zothandizira kukwanilitsa mapulani a ntchito za chitukuko omwe dayosizi-yo yakhadzikitsa mchakachi.

Msonkhano wa bungwe la amayi achikatolika la Catholic Women Organisation (CWO) ukuchitira ku Thondwe Pastoral Center mu dayosiziyo  ndipo udzatha la Mulungu pa 3rd  September 2017.  


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>