Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Awapempha Kuti Asamaope Kukhala M’maudindo Osiyanasiyana

$
0
0

Akhristu a mpingo wakatolika m’dziko muno awapempha kuti asamaope kukhala m’maudindo osiyanasiyana kamba koti kudzera m’maudindowa pomwe angathandize pa chitukuko cha dziko lino.

Bambo Hennery Chinkanda a ku  Episcopal Conference Of Malawi (ECM) ndi omwe anena izi ku Limbe Catherdral  pambuyo pa maphunziro a akhristu omwe ali ndi chidwi  chofuna kutenga nawo mbari pa nkhani zokhudza ndale.

Iwo ati kuchita ndale sichimo koma kuti ndalezo zikuyenera kuchitika pofuna kuthandiza pa chitukuko cha dziko .


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>