Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Akhiristu Apita Kumalo Oyera Ku Kibeho Mdziko La Rwanda

$
0
0

Akhristu amene  ali pa ulendo wa ku malo oyeraa KIBEHO m’dziko la RWANDA awapemphaakuti asadere nkhawa pa zaulendowu kaamba koti zomwe achitazi ndi zopambana mu mbiri ya moyo wawo wa chikhristu. Izi analankhula ndi Wachiwiri kwa wapampando wa bungwe lomwe lakonza ulendowu la DEVINE MERCY APOSTOLATE a OSWARD BWEMBA.Iwo ati aliyense amene wayenda pa ulendowu sikuti wataya ndalama koma kuti wasonkhozera madalitso ochuluka pa moyo wake wa chikhristu.

Akhristu a mpingo wakatolikawa anyamuka lachisanu pa 8 SEPTEMBER 2017 kupita  m’dziko la RWANDA , komwe akhakhaleko sabata imodzi ndi kubwelera kuno ku mudzi pa 17 mwezi uno ndipo akhristu pafupifupi 35 ndi omwe akuyenda nawo pa ulendowu. 


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>