Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

PMS Iyamikira a Khristu Pothandiza pa Chaka cha Epifania

$
0
0

Ofesi yoona za mabungwe a utumuki wa a  papa ku likulu la mpingo wakatolika m’dziko muno ya Ponfitical Mission Societies(PMS) yayamikira chidwi chomwe akhristu a mpingowu anaonetsa pothandiza kuti chaka utumiki wa ana cha Epifania chiyende bwino.

Mkulu wa ku ofesi-yi, ku likulu la mpingo-wu m’dziko muno , bambo Vincent Mwakhwawa, ndi yemwe wanena izi pofotokozera Radio Maria Malawi, za momwe chaka-chi chinayendera m’dziko muno.

Bambo Mwakhwawa ati chaka cha Epifania chomwe mpingo-wu unachita chaka chino, chinayenda bwino.

Polankhulanso mkulu wowona za mabungwe-wa mu dayosizi ya Mzuzu, bambo Phillip Shawaathokozanso a ku likulu la ofesiyi ku ECM,kamba ka chidwi chomwe anaonetsa pothandizanso ma dayosizi kuti akonzekere bwino chakachi,  zomwe zathandiziranso kuti chakachi chikhale chopambana.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>