Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Anthu anayi amwalira ndi matenda a Ebola mdziko la Mali

$
0
0

Pafupifupi anthu mazana asanu ndi limodzi (600), ali pakawuniwuni wa matenda a Ebola m’dziko la Mali.

Anthuwo akuwunikidwa ndi azaumoyo pamene dzikolo likupitiliza kuyesetsa kuti matendawa omwe apha kale anthu anai m’dzikolo asapitilire kufala. Anthuwo  akuwunikidwa powakaikira kuti agwidwa ndi matendawa pomwenso akuluakulu a boma anakumana pofuna kupeza njira zokhwimitsira chitetezo mmalire a dzikolo ndi maiko ena. Malipoti a BBC asonyeza kuti anthu awiri ndi omwe awapeza ndi matendawa .


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>