Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live
↧

AMBUYE ZIYAYE ASANKHA AKHRISTU OTHANDIZIRA ZOKONZEKERA MSONKHANO WA AMECEA

Arki episikopi wa Arki dayosizi ya Lilongwe Ambuye Tarcisius Ziyaye asankha gulu la akhristu oposa 75 omwe athandize pozokonzekera zansonkhano wa bungwe la aepiskopi la Association of Member Episcopal...

View Article


ULALIKI

kususuka by Fr.Clement M'mana

View Article


CCJP YAKHAZIKITSA NTCHITO YOCHEPETSA KUTHINANA MNDENDE

Mkulu wa ma Jaji Justice Anastanzia Msosa wayamikira bungwe la Catholic Commission for Justice and Peace [CCJP]mu Arki dayosizi ya Lilongwe chifukwa chokhazikitsa pulojekiti yolimbikitsa kuti milandu...

View Article

A MALAWI SITIKUKHWIMA PA NDALE

Mtsogoleri wa mpingo wa Anglican mdziko muno Bishopu Brighton Vita Malasa ati ziwawa zomwe zinachitika pa 8 march kwa Goliati mboma la Thyolo zawonetsa poyera kuti anthu mdziko muno sakukhwima pa...

View Article

NDILEKERANJI KUNTAMANDA

NDILEKERANJI KUNTAMANDA BY LIMBE CATHEDRAL

View Article


A KATOLIKA ATSANZIKANA NDI MONSINYO VAN MEGEN

Wapampando wa bungwe la Episcopal Conference of Malawi ECM wolemekezeka Ambuye Joseph Mukasa Zuza ayamikira yemwe anali woyimira Papa kuno ku Malawi Monsinyo Hubertus Maria Van Megen kamba ka ntchito...

View Article

MAANJA 30,000 AKUPINDULA NDI CADECOM KU DEDZA

Maanja oposa 30,000 akupindula kudzera ku pulojekiti yothandiza anthu kuti azikhala ndi chakudya chokwanira yomwe inakhazikitsidwa ndi bungwe lampingo wakatolika la Catholic Development Commission in...

View Article

AKHRISTU ATSOGOZE MULUNGU MMAUDINDO AWO PA NDALE

Akiepisikopi wa Akidayosizi ya Lilongwe ya mpingo wakatolika Ambuye Tarcizius Ziyaye apempha akhristu kuti alimbikitse ndi kupempherera anzawo omwe akupikisana nawo pa chisankho cha pa 20 May ponena...

View Article


MWAMUNA ADULA ZIWALO ZOBISIKA ZA MKAZI WAKE

Mayi wazaka 26 ali pa ululu waukulu mwamuna wake atamudula ziwalo zobisika mboma la Machinga. Mayiyu yemwe anachitiridwa za nkhanzazi pa 8 mwezi uno m’mudzi mwa Ellioti mfumu yayikulu Nkula mboma la...

View Article


iye ndi mpulumutsi

iye ndi mpulumutsi by fr NthalikaĀ 

View Article

CADRINAL NJUE AFIKA KU MALAWI

Cardinal John Njue wafika ku Malawi kuzakhala nawo pa msonkhano wa nambala 18 wa bungwe la atsogoleri ampingo wakatolika m’maiko amchigawo cha AMECEA omwe ukuyamba pa 16 july mpaka 26 July ku Bingu...

View Article

MA EPISKOPI AKU AMERICA AYAMIKIRA AMECEA

Mpingo wa katolika mdziko la United States ndi bungwe la Catholic Relief Services[CRS] ayamikira bungwe la Association of Member Episcopal Conferences in Eastern Africa [AMECEA] kamba kodzipeleka pa...

View Article

AMECEA IYAMIKIRA MUTHARIKA POKHALA PULEZIDENTI

Bungwe la Association of Member Episcopal Conferences in Eastern Africa (AMECEA) layamikira Pulezidenti wa dziko la Malawi Prof Peter Mutharika chifukwa chakupambana kwake pa chisankho chomwe...

View Article


Ambuye Ziyaye alandira PALLIUM

Akiepiskopi wa Akidayosizi ya Lilongwe Ambuye Tarcisius Ziyaye athokoza mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Fransisko chifukwa chowapatsa Pallium yatsopano chomwe ndi chizindikiro...

View Article

Aepiskopi aku Amecea alandira chilimbikitso cha Papa

Mtsogoleri wa mpingo wa katolika pa dziko lonse Papa Fransisko wafunira mafuno abwino nthumwi za ku nsonkhano wa atsogoleri a mpingowu mdera la AMECEA omwe uli mkati ku Bingu International Conference...

View Article


Ambuye Mtumbuka atsindika za udindo wa sukulu za ukachenjede mu mpingo

Episkopi wa dayosizi ya Karonga ya mpingo wa katolika Ambuye Martin Mtumbuka omwe akuchita nawo msonkhano wa bungwe la Association of Member Episcopal Conferences in Eastern Africa (AMECEA) mumzinda wa...

View Article

Ambuye Ziyaye alandira PALLIUM

Akiepiskopi wa Akidayosizi ya Lilongwe Ambuye Tarcisius Ziyaye athokoza mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Fransisko chifukwa chowapatsa Pallium yatsopano chomwe ndi chizindikiro...

View Article


Chikondwelero Cha Maimbidwe Cha Radio Maria Choir Festival

Komiti yomwe ikuyendetsa chikondwelero cha mayimbidwe cha Radio Maria Choir Festival chomwe chichitike loweruka pa 22 November yati zokonzekera zonse za mwambowu zili kumapeto. Chikondwelerochi...

View Article

Anthu anayi amwalira ndi matenda a Ebola mdziko la Mali

Pafupifupi anthu mazana asanu ndi limodzi (600), ali pakawuniwuni wa matenda a Ebola m’dziko la Mali. Anthuwo akuwunikidwa ndi azaumoyo pamene dzikolo likupitiliza kuyesetsa kuti matendawa omwe apha...

View Article

Chisankho Chapadera Cha Pulezidenti Mdziko la Zambia Chichitika Mwezi wa January

Chisankho cha pulezidenti chapadera mdziko la Zambia chichitika pa 20 January chaka cha mawa pofuna kupeza mtsogoleri yemwe alowe mmalo mwa mtsogoleri wakale wa dzikolo malemu Micheal Sata. Mtsogoleri...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>