Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Dziko la Canada Lakhazikitsa Lamulo Lolemekeza Malemu Papa Yohane Paulo Wachiwiri Woyera.

$
0
0

Nyumba ya malamulo mdziko la Canada yakhadzikitsa tsiku lachiwiri m’mwezi wa April chaka chilichonse kuti anthu mdzikolo, adzikumbulira mtsogoleri wakale wa mpingo wakatolika  malemu Papa Yohane Paulo wachiwiri Oyera.                              

Lamulo lokhazikitsira tsikuli, likutsindikanso kuti malemu Papa Yohane Paulo wachiwiri Oyera, akuyenera kulemekezedwa ngati katswiri  yemwe amalemekeza ulemelero wa anthu komanso kulimbikitsa ufulu pakati pa anthu.

Papa Yohane Paulo Wachiwiri Oyera, anamwalira pa 2 April mchaka cha 2005, ndipo patha zaka khumi tsopano chimwalilire cha Papayu.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>