Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Alimbikitsa akhritsu kupemphelela wansembe yemwe anabedwa ndizigawenga dziko la Nigeria.

$
0
0

Akhristu a mpingo wakatolika m’dziko la Nigeria awalimbikitsa kuti apemphelere wa nsembe wa mpingo wakatolika amene anagwidwa ndi anthu ena osadziwika m’dzikomo pa 8 mwezi uno.

Wansembeyo yemwe akudziwika ndi dzina loti Bambo Emmanuel Aking’lbade a matumikira ku Parish ya St Benedect yomwe kupezeka m’dera la Ido-Elklt  m’dzikomo.

  Malingana ndi ena mwa omwe anali limodzi ndi bambowa patsikuli anthuwo anauza bambowo kuti awapatse ndalama zokwanira 20 Million Naira zomwe ndi zochuluka kwambiri .

  Padakalipano ma Episkopi a mpingo wakatolika m’dzikomo alimbikitsa akhristu a mpingowu kuti apempherere bambo-wa kuti zigawenga zomwe zawagwilazo ziwatulutse, komanso kupemphelera zigawengazo kuti zitembenuke mitima ndi kuleka kuchitira anthu za upandu zosiyanasiyana.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>