Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Alimbikitsa akhritsu kupemphelela wansembe yemwe anabedwa ndizigawenga dziko la Nigeria.

$
0
0

Akhristu a mpingo wakatolika m’dziko la Nigeria awalimbikitsa kuti apemphelere wa nsembe wa mpingo wakatolika amene anagwidwa ndi anthu ena osadziwika m’dzikomo pa 8 mwezi uno.

Wansembeyo yemwe akudziwika ndi dzina loti Bambo Emmanuel Aking’lbade a matumikira ku Parish ya St Benedect yomwe kupezeka m’dera la Ido-Elklt  m’dzikomo.

  Malingana ndi ena mwa omwe anali limodzi ndi bambowa patsikuli anthuwo anauza bambowo kuti awapatse ndalama zokwanira 20 Million Naira zomwe ndi zochuluka kwambiri .

  Padakalipano ma Episkopi a mpingo wakatolika m’dzikomo alimbikitsa akhristu a mpingowu kuti apempherere bambo-wa kuti zigawenga zomwe zawagwilazo ziwatulutse, komanso kupemphelera zigawengazo kuti zitembenuke mitima ndi kuleka kuchitira anthu za upandu zosiyanasiyana.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>