Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Bungwe la Episcopal Conference of Malawi Layamba Zokambirana Zapachaka Mudzinda wa Lilongwe.

$
0
0

Msonkhano wachiwiri wapachaka wa bungwe la maepiscope a mpingo wa katolika la Episcopal Conference of Malawi (ECM)   wayamba  mudzinda wa Lilongwe.

 Malinga ndi chikalata chomwe bungweli latulutsa ,msokhanowu wayamba lolemba   ndipo utha lachisanu.

Nthumwi ku kumsokhanowu zikukambirana nkhani yokhudza zokonzekera za chikondwerero choti Seminary ya Kachebere  yakwanitsa zaka 75,malamulo owona za chipembedzo mumpingo ndiponso  nkhani zokhudza msonkhano wa Sinodi.  

  Ma Bishopuwanso  akambirana malipoti ochokera mmakomishoni, mmadipatimenti ndi mapulojekiti osiyanasiyana amu`mpingo wakatolika.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>