Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Dziko la Swaziland Likufunika Mwambo wa Mapemphero

$
0
0

Episkopi  wa dziko la Swaziland  wapempha anthu m’dzikolo kuti akhale ndi mwambo wa mapemphero  potsatira ngozi ya pansewu  yomwe inapha  atsikana pafupifupi makumi asanu omwe adali paulendo okapikisana nawo pamwambo osankha mkazi watsopano wa mfumu Mswati ya dzikolo.

 

Malipoti a Catholic News Agency ati anthu mdzikoli akuyenera kukhala ndi mapemphero apadera pofuna kupempha chitetezo kwa mulungu kuti dzikoli lipewe ngozi za mtunduwu.

 

Episkopiyu wapempha anthu mdzikoli kuti akuyenera nthawi zonse kukhala ndi nthawi yopemphera osati kudikira ngozi za mtunduwu kuti zichitike.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>