Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Ambuye Ziyaye Alimbikitsa Pakati pa Akhristu

$
0
0

Ark Episkopi wa Arch Dayosizi ya Lilongwe Ambuye  Tarsizius Ziyaye apempha akhristu a m’parishi ya St Kizito mu Ark dayosiziyo kuti alimbikitse m’gwirizano wabwino pakati pawo.

Ambuye Ziyaye anena izi lamulungu pa mwambo wokhazikitsa bukhu la ndondomeko  za chitukuko m’parishiyi.

Iwo ati mapulani a zachitukuko omwe parishiyo yakonza ndi osavuta kuwakwaniritsa pokhapokha atamanga mgwirizano pakati pawo


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>