Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Bungwe la Community of St Egidio Layamba Kuphunzitsa Anthu Kufunika Kolembesa Ana Obadwa Kumene

$
0
0

Bungwe la mpingo wa Akatolika la Community of St Egidio m’dziko muno layamba ntchito yophunzitsa anthu kufunika kwa kalembera wa ana omwe angobadwa kumene.

Polankhula pa mwambo otsegulira maphunziro a ntchitoyi omwe ukuchitikira mu mzinda wa Blantyre mkulu oyendetsa ntchito mu nthambi ya boma yoona za
kalembera ya National Registration Bureau a Francis Chinsinga ati ali ndi chikhulupiriro choti ntchitoyi iyenda bwino kamba ka m’gwirizano omwe ulipo pakati pa boma ndi bungweli m’dziko muno.

 A Chinsinga ati ntchitoyi yomwe yayamba m’boma la Balaka ikuyembekezera kufalikira m’madera ena m’dziko muno.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>