Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Ambuye Sitima ati Makwaya Azipeka Nyimbo za Tanthauzo

Episkopi wa Dayosizi ya Mangochi ya mpingo wakatolika Ambuye Montfort Sitima wapempha makwaya mdziko muno kuti aziwonetsetsa nthawi zonse kuti pamene akupeka nyimbo zizikhala za tanthauzo. Ambuye...

View Article


Dziko la Sierra Leone Likondwelera Kutha kwa Matenda a Ebola

Anthu m’dziko la Sierra Leone akupitiliza kuchita chisangalalo chokondwelera kutha kwa matenda a Ebola m’dzikomo.   Bungwe la za umoyo pa dziko lonse la World Health Organization ndi lomwe lalengeza...

View Article


Nsika wa Kasungu Ukufunika Ndalama Zokwana 10 miliyoni Kwacha

Nsika wa Kasungu omwe unapsa mwezi wa October ati ukufunika ndalama zoposa 10 Million Kwacha kuti ukozedwenso.  Wachiwiri kwa Meya wa Manicipality ya Kasungu  a Ephate Joshua ndi yemwe wanena izi pomwe...

View Article

Pulezidenti Kagame Adzudzula Dziko la Burundi

Mtsogoleri wa dziko la Rwanda  Paul Kagame  wadzudzula ziwawa zomwe zikuchitika m`dziko la  Burundi zomwe zikuphetsa anthu ankhanikhani. Pulezidenti Kagame wati  anthu m`dzikolo akungophedwa...

View Article

Atolankhani Azilemba Nkhani za Matenda Osapatsirana

Atolankhani mdziko muno awapempha kuti azilemba nkhani zokwanira zokhudza matenda osapatsirana omwe ndi kuphatizapo a shuga pofuna kuchepetsa imfa zomwe zimachitika kudzera mmatendawa Mkulu wa bungwe...

View Article


Ulendo wa Papa Wokacheza Mdziko la CAR Upereka Chiyembekezo kwa akhristu a...

Akhristu a mpingo wa katolika a m’dziko la Central African Republic omwe akhala akuphana tsiku ndi tsiku kamba ka nkhondo ati akuyembekezera kuti ulendo wa mtsogoleri wa mpingo wa katolika pa dziko...

View Article

Bungwe la Community of St Egidio Layamba Kuphunzitsa Anthu Kufunika Kolembesa...

Bungwe la mpingo wa Akatolika la Community of St Egidio m’dziko muno layamba ntchito yophunzitsa anthu kufunika kwa kalembera wa ana omwe angobadwa kumene.Polankhula pa mwambo otsegulira maphunziro a...

View Article

Apolisi Ati Anthu Azigwiritsa Ntchito Malamulo MoyeneraApolisi Ati Anthu...

Apolisi apempha anthu m’dziko muno kuti azitengera kupolisi anthu onse omwe akuwaganizira kuti apalamula milandu osati kuwalanga okha. Wachiwiri kwa mneneri wa apolisi ku Limbe mu mzinda wa Blantyre...

View Article


nthu ena Anakawombera Mdera la Kumpoto kwa Mzinda wa Paris

Pomwe apolisi mu mzinda wa Paris mdziko la France akupilizabe kuchita kafukufuku wa anthu omwe anachita chiwembu chomwe chinapha anthu pafupifupi 1 hundred 30 mdzikolo, anthu ena omwe sakudziwika ati...

View Article


Matenda a Ebola Akuyembekezeka Kutha Mdziko la GuineaMatenda a Ebola...

Munthu wotsiriza yemwe amadwala matenda a Ebola m`dziko la Guinea wachira ndipo amutulutsa mchipatala.  Malinga ndi wofalitsa nkhani ku nthambi yomwe imayang`anira ntchito zothana ndi matendawa...

View Article

Dziko la Canada Lichepetsa Chiwerengero Chosunga Anthu Othawa Kwawo

Dziko la Canada lati lisunga anthu othawa kwao okwana 10 sauzande ochokera mdziko la Syria chikamatha chaka chino. Malipoti a wailesi ya BBC ati dzikoli poyamba linalonjeza kuti lisunga anthu othawa...

View Article

Anthu Odwala Matenda a Edzi Asasalidwe

Bungwe  la National AIDS Commission NAC lati anthu omwe anapezeka ndi kachilombo koyambitsa  matenda a Edzi sayenera kusalidwa .   Mmodzi mwa akuluakulu ku bungweli  a Ahmidu Tung'ande ndi omwe anena...

View Article

Bungwe la MBTS Lipempha Anthu kuti Agwirane Nalo ManjaBungwe la MBTS Lipempha...

Bungwe lotolera magazi la Malawi Blood Transfussion Service MBTS lamemeza anthu  kuti agwirane nalo manja powonetsetsa kuti zipatala za m'dziko muno zili ndi magazi okwanira komanso a ukhondo.   Mkulu...

View Article


Bungwe la Community of Saint Egidio Likondwelera Zaka 47 Chilikhazikitsire

Bungwe la Community of Saint Egidio lati ndi lokondwa kuti tsopano lakwanitsa zaka 47 kuchokera pomwe bungweli linayamba kugwira ntchito zake zolimbikitsa moyo wa mapemphero ndi kudzipeleka pogwira...

View Article

Bambo Corna a Mdziko la Italy Amwalira

A ku Likulu la chipani cha Mofolo Woyera ku Rome mdziko la Italy alengeza za imfa ya Bambo Attilio Corna omwe anamwalira  lachiwiri pa 10 February 2015 mu mzinda wa Bergamo mdzikolo. Bambo Corna...

View Article


Sister Martha Clemence Manuel Makhasa a Chipani cha SBVM Amwalira

Sister Martha Clemence Manuel Makhasa a Chipani cha Servants of Blessed Virgin Mary (SBVM), amwalira lachisanu. Malinga ndi akulikulu la chipanichi Sister Martha anabadwa pa 8 September 1932 ndipo...

View Article

KUTHETSA MLILI WA HIV: KUWUNIKA UDINDO WA MPINGO PA NDONDOMEKO YA 90-90-90

            - Osatopa ndikuchita zinthu zabwino- (2 Thess. 3:13) Uthenga wa HIV ndi EDZI m’chaka cha 2015 From ECM Health Commission   1.0 CHIYAMBI Lero ndi lamulungu loyamba  munyengo ya Adventi....

View Article


Papa Francisco Alimbikitsa Achinyamata Kuzamitsa Moyo wa Uzimu

Muuthenga  wachaka cha achinyamata chaka chino, mtsogoleri wampingo wakatolika padziko lonse Papa Francisco, wapempha akhristu mumpingowu kuti azamitse  moyo wawo wauzimu poyeretsa mitima yawo....

View Article

Zigawenga za Boko Haram Zilepheretsa Zisankho Mdziko la Nigeria

Mtsogoleri wa gulu la zigawenga za Boko Haram Abubakar Shekau, wanenetsa kuti alepheretsa zisankho za atsogoleri zomwe dzikolo likuyembekezeka kukhala nazo pa 28 March chaka chino. Iye wanena izi...

View Article

Mpingo wa Katolika ku Vatican Uganizira Anthu Osowa

Mpingo wa katolika ku Vatican wakhazikitsa malo ometera awulele a anthu osowa kwawo. Pa mwambowu womwe unatsekuliridwa ndi mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco kunafika anthu...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>