Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

nthu ena Anakawombera Mdera la Kumpoto kwa Mzinda wa Paris

$
0
0

Pomwe apolisi mu mzinda wa Paris mdziko la France akupilizabe kuchita kafukufuku wa anthu omwe anachita chiwembu chomwe chinapha anthu pafupifupi 1 hundred 30 mdzikolo, anthu ena omwe sakudziwika ati anakawombera dera la ku mpoto kwa mzindawu.

Malipoti ati dera lomwe anthuwa anakawombera ndi limodzi mwa madera omwe zigawenga za Islamic State linawononga kwambiri pa chiwembu chomwe chinachita mdzikolo posachedwapa.

Malinga ndi malipoti a nyuzi 24   apolisi omwe amagwira ntchito pa nthawiyo avulala.

Padakali pano ndege za asilikali akhondo a mdziko la Russia ndi France zikufunafuna zigawengazi mmadera omwe akuwaganizira mdziko la Syria.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko