A Blazala awiri a chipani cha Mofolo woyera loweruka awadzodza kukhala madikoni mu mpingo wakatolika .
Mwambowu omwe unachitikira ku parish ya St Louis Montfort ku Balaka anatsogolera ndi episkopi wa dayosiziyi ambuye Montfort Sitima.
Mu ulaliko wawo Ambuye Sitima anati Mulungu amayitana anthu ake kuti akagwire ntchito yolalikira mthenga wachipulumutso ponse ponse.
Polankhulanso utangotha mwambowu madikoniwa ati ndi okondwa kuti Mulungu wawathandiza kufikira pano pomwe adzozedwa kukhala madikoni ndipo ati adzipereka pa ntchito zotumikira mulungu kudzera mu mpingowu.
Madikoni omwe adzozedwawa ndi a Anthony Chilolo ndi Peter Makina.
A Blazala awiri a chipani cha Mofolo woyera loweruka awadzodza kukhala madikoni mu mpingo wakatolika .
Mwambowu omwe unachitikira ku parish ya St Louis Montfort ku Balaka anatsogolera ndi episkopi wa dayosiziyi ambuye Montfort Sitima.
Mu ulaliko wawo Ambuye Sitima anati Mulungu amayitana anthu ake kuti akagwire ntchito yolalikira mthenga wachipulumutso ponse ponse.
Polankhulanso utangotha mwambowu madikoniwa ati ndi okondwa kuti Mulungu wawathandiza kufikira pano pomwe adzozedwa kukhala madikoni ndipo ati adzipereka pa ntchito zotumikira mulungu kudzera mu mpingowu.
Madikoni omwe adzozedwawa ndi a Anthony Chilolo ndi Peter Makina.