Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Papa Abatiza Ana 26 pa Tsiku la Ubatizo wa Ambuye Yesu

$
0
0

Pomwe mpingo wa katolika umachita chaka cha ubatizo wa ambuye Yesu mumtsinje wa Yolodani , mtsogoleri wa mpingo wakatolika anabatiza makanda 26 ku Roma.

Papa Francisco wabatiza anawa pa mwambo wa nsembe ya ukaristia omwe unachitikira m`tchalitchi ya Sistine.

Papa  wati kudzera mu ubatizo  akhristu amapereka chikhulupirilo chao ku m`badwo wina.

Papa anauza makolo a anawa kuti asamayiwale kuti chikhulupirilo ndi chinthu chamtengo wapatali chomwe angasiyire ana awo.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>