Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Malema Ayimitsidwa ndi Apolisi pa Nseu

$
0
0

Apolisi m`dziko la  South Africa ati anayimitsa galimoto la mtsogoleri wa chipani chotsutsa boma  cha  Economic Freedom Fighters (EFF)  a Jullious Malema, potsatira zomwe mkuluyu ananena masiku apitawa  kuti mtsogoleri wa dzikolo a Jacob Zuma atule pansi udindo wawo.

Malinga ndi malipoti awailesi ya BBC, a Zuma akuwadzudzula kuti anasakaza ndalama za boma  pokozetsera nyumba yawo yapadera.

Chipani va EFF chati apolisi anayimitsa galimoto  ya mkuluyu munzinda wa Johannesburg ndi kumulozetsa mfuti ngati njira imodzi yomuopseza.

A Zuma ati akukana kuti anawononga ndalamazi koma avomera kuti abweza.

Apolisi m`dziko la  South Africa ati anayimitsa galimoto la mtsogoleri wa chipani chotsutsa boma  cha  Economic Freedom Fighters (EFF)  a Jullious Malema, potsatira zomwe mkuluyu ananena masiku apitawa  kuti mtsogoleri wa dzikolo a Jacob Zuma atule pansi udindo wawo.

Malinga ndi malipoti awailesi ya BBC, a Zuma akuwadzudzula kuti anasakaza ndalama za boma  pokozetsera nyumba yawo yapadera.

Chipani va EFF chati apolisi anayimitsa galimoto  ya mkuluyu munzinda wa Johannesburg ndi kumulozetsa mfuti ngati njira imodzi yomuopseza.

A Zuma ati akukana kuti anawononga ndalamazi koma avomera kuti abweza.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>