Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Chifundo cha Mulungu ndi cha Aliyense

Ark-episkopi wa mzinda wa Vienna mdziko la Australia Ambuye Christopher Schonborn wati chifundo cha Mulungu chilipo kwa  aliyense amene amakhala akusawutsidwa mu mtima.  Malinga ndi malipoti a wailesi...

View Article


Munthu Mmodzi Wafa ndi Matenda a Ebola Mdziko la Liberia

Munthu m`modzi ati wafa  ndi matenda a Ebola m`dziko la Liberia patangotha miyezi yowerengeka, bungwe la zaumoyo pa dziko lonse litalengeza kuti nthendayi yatha m`dzikolo. Malinga ndi malipoti...

View Article


Ambuye Musikuwa Akhazikitsa Mijigo mu Dayosizi YawoAmbuye Musikuwa...

Mpingo wa katolika mu dayosizi ya Chikwawa wapempha boma ndi mabungwe akufuna kwabwino  kuti alimbikitse ntchito yosamalira  anthu omwe akuvutika kamba kosowa zinthu zofunika pamoyo wao wa tsiku ndi...

View Article

Dziko la Kenya Lichita Mapemphero a Ophunzira a pa Sukulu ya Garissa

Anthu m`dziko la Kenya achita mapemphero  okumbukira mizimu ya anthu 148  omwe anafa pa chiwembu chomwe gulu la zigawenga za Al- Shabab zinachita pa sukulu ya ukachenjede ya Garisa m`dzikolo. Malinga...

View Article

Abwenzi ndi Otumikira Radio Maria mu Dayosizi ya Zomba Alonjeza Kugwilira...

Ngati njira imodzi yopititsira patsogolo ntchito za Radio Maria Malawi, abwenzi a wailesiyi ku dayosizi ya Zomba ati agwira ntchito limodzi ndi  otumikira a wailesiyi  potolera thandizo. Wapampando wa...

View Article


Papa Francisco wati Akhristu Akhale Apostoli komanso Wapempha Mtendere Mdziko...

Pamene mpingo umachita chaka cha  lamulungu la chifundo, mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco wapempha akhristu kuti akhale apostoli a chifundo kwa onse osowa. Malipoti a...

View Article

Malema Ayimitsidwa ndi Apolisi pa Nseu

Apolisi m`dziko la  South Africa ati anayimitsa galimoto la mtsogoleri wa chipani chotsutsa boma  cha  Economic Freedom Fighters (EFF)  a Jullious Malema, potsatira zomwe mkuluyu ananena masiku apitawa...

View Article

Amuna Atatu Amangidwa Chifukwa Cholima Chamba

Apolisi m’boma la Ntchisi akusunga mchitokosi amuna atatu kamba kowaganizira kuti amalima chamba. Wofalitsa nkhani za apolisi m’bomalo Sergent Gladson M’bumpha watsimikiza za nkhaniyi.   Sergent...

View Article


Papa Wapempha Akhristu kuti Azivomera Kuyitana kwa Mulungu

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco wapempha akhristu kuti azikhala ndi mitima yotsekula kwa Mulungu nthawi zonse komanso azivomera kulandira uthenga wake wa chipulumutso....

View Article


Pulezidenti Zuma Sachotsedwa pa Udindo Wake

Nyumba ya malamulo m’dziko la South Africa inachita chisankho chakuti asachotse pa udindo mtsogoleri wa dzikolo a Jacob Zuma posayang’anira chigamulo chomwe bwalo lamilandu linapereka pa mlandu omwe...

View Article

Mpingo wa Orthdox Mdziko la Greece ndi Wokonzeka Kulandira Papa Francisco

Mpingo wa Orthodox mdziko la Greece wati ndi wokonzeka kulandira mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco paulendo wake wokayendera anthu othawa kwawo mdzikolo. Malipoti a wailesi...

View Article

Dziko la Egypt Litumiza Zotsatira za Kafukufuku wa Ophunzira yemwe Anaphedwa...

Dziko la Egypt lati litumiza zomwe lapeza pa kafukufuku wokhudza kuphedwa kwa   ophunzira  wa mdziko la Italy  yemwe anapezeka atafa m`dziko la Egypt. Malinga ndi malipoti a wailesi ya BBC, ophunzirayo...

View Article

Papa Francisco wati Akhristu a Mpingo wakatolika ndi Methodists Agwlire...

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco wati akhristu a mpingo wakatolika ndi Methodists akuyenera kuphunzirana kamba koti zolinga zawo ndi zimodzi. Papa Francisco amalankhula izi...

View Article


Papa wati Mabanja Okhazikika Amakhala OpindulaPapa wati Mabanja Okhazikika...

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco wati mabanja okhazikika amakhala opindula kamba koti amachititsa kuti anthu azikhala bwino mmadera komanso ana amakula ndi chikondi,...

View Article

Mpingo Wakatolika ku Burundi Wapempha Mtsogoleri Wa Dzikolo Kuti...

Bungwe la ma Episkopi a mpingo wa Katolika m’dziko la Burundi lati silikugwirizana ndi zomwe m’tsogogoleri wa dzikolo akufuna kuti adzayimenso  pa chisankho cha president kamba koti matelemu ake...

View Article


Radio Maria Ikhazikitsidwa Mdziko la Madagascar

Akuluakulu oyendetsa ntchito za Radio Maria pa dziko lonse alengeza zakubadwa kwa wailesi ina m’dziko la Madagascar Kukhadzikitsidwa kwa wailesiyi kwachulukitsa  nambala ya mayiko amene ali ndi Radio...

View Article

Abwenzi a Radio Maria Malawi Awonetsa Chidwi pa Ntchito ya Mariatona

Akuluakulu a Radio Maria Malawi ayamikira abwenzi a wayilesiyi  kamba kowonetsa chidwi chogwirira ntchito limodzi munyengo ino yomwe wailesiyi ikukonzekera ntchito ya chaka chino yotolera thandizo...

View Article


Mkhristu Wakufuna Kwabwino Apereka Malo ku Radio Maria

Mmodzi mwa akhristu mu mpingo wakatolika wapereka malo ku Radio Maria Malawi  ku Dwangwa m’boma la Nkhotakota ndi cholinga choti wailesiyi idzalepo transmitter yake. Mkhristuyu Martin Mangani wapereka...

View Article

Guelleh Wapambananso pa Mpando wa PulezidentiGuelleh Wapambananso pa Mpando...

Mtsogoleri wa dziko la  Djibouti  a Ismail Omar Guelleh wapambananso pa chisankho chomwe chinachitika m`dzikolo masiku apitawa. Malinga ndi malipoti awailesi ya BBC,   a Guelleh apeza mavoti 87 pa 1...

View Article

Papa wati Mabanja Okhazikika Amakhala Opindula

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco wati mabanja okhazikika amakhala opindula kamba koti amachititsa kuti anthu azikhala bwino mmadera komanso ana amakula ndi chikondi,...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>