Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Arkidayosizi ya Blanytye Iyamikira Bungwe la CFM

$
0
0

Arkidayosizi ya Blantyre mu mpingo wa Katolika yayamikila mgwilizano ndi luntha lomwe bungwe la mabanja a chi khristu la  Christian Family Movement (CFM) ku parishi ya St Pius likuonetsa potenga mbali pa ntchito yothandiza kukonzanso Nyungwi Parish yomwe inakhudzidwa ndi ngozi ya moto.

A Vicar General a Akidayosizi-yi, Bambo Boniface Tamani ndiwo anena izi mmalo mwa mpingowu.

Iwo ayamikira bungwe la mabanjali kamba kothandiza pa ntchitoyi ndi ndalama zokwanira  3 hundred thousand kwacha.

Wapampando wa bungwe la mabanjali ku St. Pius a Aidan Gumeni ati bungwe lawo ndilokhuzidwa  ndi ngoziyi nchifukwa chake atenga nawo mbali pa ntchito yokonzanso tchalichili.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>