Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Anthu Asanu Afa ndi Bomba Mdziko la SomaliaAnthu Asanu Afa ndi Bomba Mdziko...

Anthu asanu afa ndipo ena asanu ndi awiri avulala kamba ka bomba lomwe linaphulitsidwa pa malo ena odyera mu mzinda wa Mogadishu mdziko la Somalia. Malinga ndi malipoti a wailesi ya BBC munthu yemwe...

View Article


Ambuye Musikuwa ati Achinyamata Akhale a Makhalidwe AbwinoAmbuye Musikuwa ati...

Episkopi wa mpingo wakatolika wa dayosizi ya Chikwawa, Ambuye Peter Musikuwa walangiza ophunzira msukulu zosiyanasiyana za ukachenjede m’dziko muno kuti asalore kuti ena aziwapotoza ndi kuti azitsatira...

View Article


Papa wati Akhristu Amuyike Mmapemphero

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco wapempha akhristu kuti amuyikize mmapemphero pomwe akukonzekera ulendo wake wokayendera anthu othawa kwao pa doko la Lesbos mdziko la...

View Article

Chiwerengero cha Akhristu Akatolika Chakwera

Lipoti latsopano lomwe likulu la mpingo wakatolika latulutsa, lasonyeza kuti chiwerengero cha akhristu a mpingowu chakwera kwambiri mu zaka zisanu ndi zitatu zapitazi. Lipotilo lati kuyambira mchaka...

View Article

Mkulu wa Maepiskopi Mdziko la Greece wati Ali ndi ManthaMkulu wa Maepiskopi...

Pamene mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco ndi atsogoleri a mpingo wa Orthodox akuyembekezeka kukayendera anthu othawa kwao pa chilumba la Lesbos mdziko la Greece, mkulu wa ma...

View Article


Njala Ikubwezeretsa Ntchito Za Chitukuko

Mavuto anjala ati akubwezeretsa m’mbuyo ntchito za chitukuko komanso maphunziro ku dera la kum’mwera kwa boma la Neno. Phungu wa derali Mayi Mary Maulidi ndi omwe anena izi pomwe bungwe lina lomwe sila...

View Article

Bungwe la Amayi Lilonjeza Kutukula Dayosizi

Wapampando watsopano wa bungwe la amayi mu mpingo wakatolika mu dayosizi ya Zomba , Mayi Elizabeth Meke wati komiti yawo ipitiliza kudzipeleka pa ntchito zotukula dayosiziyo. Mayi Mekeanena izi...

View Article

Mpingo wa Anglican Ukulimbikitsa Maphunziro a Atsikana

Mpingo wa Anglican mu dayosizi ya Uppershire kudzera mu project yomwe mpingowu unakhadzikitsa ya Msamama Community Intergrated wati upitiliza kudzipeleka polimbikitsa maphunziro atsikana. Mkulu...

View Article


Ambuye Stima Ayamikira Asisteri a DMI Pa Chitukuko

Episkopi wa dayosizi ya Mangochi olemekezeka Ambuye Montfort Stima ayamikira asisteri achipani cha Daughters of Mary Immaculate (DMI)kamba kolimbikitsa zitukuko zosiyanasiyana mu dayosiziyo. Ambuye...

View Article


Mpingo Upempha Boma la Nigeria Likambirane ndi Gulu la Boko Haram

Mpingo wakatolika mdziko la Nigeria wati boma la dzikolo likuyenera kuchita zokambirana ndi zigawenga za gulu la Boko Haram ndi cholinga chofuna kupulumutsa atsikana 2 hundred a mtauni ya Chibok omwe...

View Article

Chivomerezi Chapha Anthu Asanu ndi Anayi Ku Japan

Anthu pafupifupi  asanu ndi anayi afa ndipo ena  avulala m’dziko la Japan kaamba ka chivomerezi chomwe chagwedeza mthaka ya dzikolo. Malingana ndi malipoti a wailesi ya BBC anthu ochuluka anathawa...

View Article

Arkidayosizi ya Blanytye Iyamikira Bungwe la CFM

Arkidayosizi ya Blantyre mu mpingo wa Katolika yayamikila mgwilizano ndi luntha lomwe bungwe la mabanja a chi khristu la  Christian Family Movement (CFM) ku parishi ya St Pius likuonetsa potenga mbali...

View Article

Mpingo Wa Katolika Uchita Chaka Cha UtumikiMpingo Wa Katolika Uchita Chaka...

Episkopi wa dayosizi ya Dedza ambuye EmmanuelKanyamawapempha achinyamata kuti akhale ndi udindo waukulu podzipeleka pa ntchito zotumikira mpingo kudzera mmautumiki osiyanasiyana. Ambuye Kanyama anena...

View Article


Maphunziro a Pafupipafupi ndi Othanza kwa Achinyamata

Parishi ya Lirangwe mu Arkidayosizi ya Blantyre ya mpingo wa katolika yati ntchito yosintha kaganizidwe ka achinyamata ati ingatheke ngati pangakhale maphunziro a pafupipafupi kwa achinyamatawa. Bambo...

View Article

Anthu Othawa Kwao Afa Bwato lomwe Anakwera Litamira mu Nyanja ya Mediterranean

Anthu othawa kwawo mazanamazana ati amira bwato lomwe  anakwera litamira panyanja yaikulu ya Meditereanneanm`dziko la Egypt. Malinga ndi malipoti a wailesi ya BBC, anthu 41 ndi omwe apulumitsidwa  pa...

View Article


Papa Francisco Achita Zokambirana ndi Presidenti wa Dziko la Central African...

Mtsogoleri wa dziko laCentral African Republic, a Faustin Archangel Touadera  ali  ku likulu la mpingo wakatolika ku Vatican komwe akuchita zokambirana ndi mtsogoleri wa mpingo wa katolika Papa...

View Article

Alimi Azigwiritsa Ntchito Zipatala Za Mbewu

Alimi m`boma la Mulanje awapempha kuti azigwiritsa ntchito zipatala za mbewu zomwe  ofesi ya za malimidwe inakhazikitsa m`bomalo ngati njira yothanirana ndi matenda osiyanasiyana omwe amagwira mbewu....

View Article


Mfumu Zwelithini ya Mdziko la South Africa Ikuyembekezeka Kudzudzula Anthu...

Mfumu yachizulu Good-will Zwelithini ya mdziko la South Africa ikuyembekezeka kulankhulapo popempha mzika za dzikolo kuti zisiye kuchitira mtopola mzika za mmayiko ena zomwe zikukhala mdzikolo pa...

View Article

Sister Fortina Saiwa Atisiya

Aku likulu la chipani cha asisiteri  cha Tereza Woyera  mu Arkdayosizi ya Lilongwe alengeza za imfa ya Sister  Fortina Saiwa.  Iwo  amwalira lachiwiri ku chipatala cha Mlale m’boma la Lilongwe. Sister...

View Article

Unduna Upempha Anthu Asamukire Kumadera Okwera

Unduna woona za ulimi wa mthirira ndi chitukuko cha madzi wapempha anthu omwe akukhala m`madera otsika m`boma la Karonga kuti asamukire kumadera okwera.   Unduna wu wanena izi kudzera m`chikalata...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>