Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Bungwe la YCW mu Doyosizi Ya Mangochi

$
0
0
Achinyamata abungwe la YCW mu Doyisizi ya Mangochi awapempha kuti adzidzipeleka pomwe apasidwa kuti agwire ntchito m'malo osiyana siyana Avicar General adoyosiziyi bambo Andrew Nkhata ndi omwe anena izi lamulungu lapitali pomwe achinyamata am'bungweri amachita mwambo wokondwelera nkhonswe yawo joseph wa ntchito padziko lonse mwambowu unachitikira ku St.Augustine Cathedral mu Doyosizi ya Mangochi.

Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>