Mariatona
Mariatona ndi ndi dongosolo lapadela limene limachitika ndi cholinga chofuna kupeza ndalama, ndipo amene amakhudzidwa ndi onse woyendetsa ntchito za wailesi monga ma volunteer, abwenzi a Radio...
View ArticleAnthu Achitepo Kanthu Pofuna Kuchepetsa Imfa za pa Nyanja
Mtsogoleri wampingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco wapempha mayiko padziko lonse kuti achitepo kanthu pofuna kuchepetsa imfa za anthu omwe akumwalira panyanja, paulendo opita mmayiko a ku...
View ArticleBungwe la Law Society ndi lokhudzidwa ndi Mavuto omwe Dziko Lino Likukumana Nawo
Bungwe lowona za malamulo mdziko muno la Law Society lati ndi lokhudzidwa kwambiri ndi mavuto omwe dziko lino layamba kukumana nawo posachedwapa pankhani zosiyanasiyana. Ena mwa mavuto omwe bungweli...
View ArticleMsonkhano Wa Bungwe La Tilitonse Wachitika Ku Lilongwe
Msonkhano wa aphunzitsi a m’bungwe la utumiki wa ana la Tilitonse wachitika mu arkidayosizi ya mpingo wakatolika ya Lilongwe. Ofesi yoona za ma utumiki a Papa la Pontifical Missionary Societies (PMS)...
View ArticleBoma Liyamikira Bungwe La St. Egidio Polimbikitsa Kaundula
Boma la Malawi layamikira mpingo wakatolika mdziko muno kamba kotengapo mbali pa ntchito yolimbikitsa anthu kuti azilembetsa ana awo mukaundula wa dziko lino, akabadwa. Mkulu woyendetsa ntchito yolemba...
View ArticleDayosizi Ya Zomba Ipempha Anthu Kuthana Ndi KunyentcheraDayosizi Ya Zomba...
Ofesi ya za umoyo mu dayosizi ya mpingo wakatolika ya Zomba yalimbikitsa anthu a mdera la Chingale kuti azidzipeleka polimbana ndi mavuto a kunyentchera pakati pa ana awo. Mlangizi wa sukulu za m’mera...
View ArticleBishop Elect for Mzuzu
KNOW THE BISHOP - ELECT FOR MZUZU DIOCESE ■HIS CURRICULUM VITAE ●Reverend Father John Alphonsus Ryan was born on 27 February, 1952 in Tipperary (Archdiocese of Cashel and Emily - Ireland) ●After his...
View ArticleNew Bishop Of Mzuzu Diocese
26thApril, 2016 His Excellency Archbishop Julio Murat, Apostolic Nuncio to Malawi and Zambia wish to announce that His Holiness Pope Francis has appointed Reverend Father John Alphonsus Ryan of the...
View ArticleEpisikopi Watsopano Wa Diyosizi Ya Mzuzu
Wolemekezeka Ambuye Julio Murat nthumwi ya a Papa m’maiko a Malawi ndi Zambia yalengeza kuti mtsogoleri wa mpingo wa katolika pa dziko lonse Papa Francisko wasankha Reverend Fr. John Alphonsus Ryan...
View ArticleMachar Alumbilitsidwa Kukhala Wachiwiri kwa Pulezidenti
Mkulu wa gulu lowukira boma m’dziko la South Sudan Riek Machar amulumbiritsa kukhala wachiwiri kwa m’tsogoleri wa dzikolo ndi cholinga chofuna kukometsa pangano lodzetsa mtendere ndi m’tsogoleri wa...
View ArticlePapa Alimbikitsa Kufunika kwa Akhristu
Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse PapaFrancisco wauza ansembe kuti akuyenera kutumikira anthu nthawi zonse osati kuti azikhala patsogolo kupanga mfundo zoyendetsera mpingo kaamba koti...
View ArticleMilandu ya Katengale ya Pulezidenti Zuma Iwunikidwenso
Bwalo lamilandu mdziko la South Africa lati ganizo lothetsa milandu 7 hundred 83 ya katangale ya pulezidenti wa dzikolo Jacob Zuma likuyenera kuwunikidwanso. Malipoti a wailesi ya BBC ati milanduyi...
View ArticlePapa Alimbikitsa Anthu Kupereka Chisamaliro kwa Odwala
Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco wati anthu akuyenera kukhala ndi chifundo ndi anthu omwe akudwala matenda osiyanasiya mmadera omwe amakhala. Papa amalankhula izi ku...
View ArticleKusowa kwa Chakudya
Boma lati laika ndondomeko zomwe ati zithandize pothana ndi vuto la chakudya lomwe lili m'dziko muno. Nduna ya zaulimi ,ulimi wa nthirila komanso chitukuko cha madzi Dr.Goerge Chaponda ndiwo anena izi...
View ArticleBungwe la YCW mu Doyosizi Ya Mangochi
Achinyamata abungwe la YCW mu Doyisizi ya Mangochi awapempha kuti adzidzipeleka pomwe apasidwa kuti agwire ntchito m'malo osiyana siyana Avicar General adoyosiziyi bambo Andrew Nkhata ndi omwe anena...
View ArticleDayosizi Ya Zomba Yaphunzitsa Achinyamata Luso Losiyanasiyana Dayosizi Ya...
Achinyamata a kwa Mayaka m’boma la Zomba akuyimba lokoma ndi luso la ntchito zosiyanasiyana zomwe aphunzira kuchokera ku nthambi ya za maphunziro mu mpingo wakatolika mu dayosizi ya Zomba....
View ArticleECM Yapempha Komiti Ya Ophunzira Msukulu Zachikatolika Zaukachenjende...
Komiti yatsopano ya bungwe la ophunzira achikatolika a msukulu za ukachenjede m’dziko muno ayipempha kuti idzipeleke pa ntchito zotukula bungweli m’dziko muno. Mlangizi wa achinyamata ku likulu la...
View ArticleECM Lapereka ndalama ku Bungwe la MISA Malawi
Likulu la mpingo wa katolika dziko muno ECM,kudzera ku nthambi yake ya zachitukuko ya Social Development Directorate lapereka ndalama zokwana 5 hundred thousand kwacha ku bungwe la atolankhani la MISA...
View ArticleMwambo Wotsekulira Mariatona 2016
Mwambo wotsekulira Radio Maria Mariatona 2016 uchitika mawa ku Parish ya St.Louis Montfort ku Balaka mu dayosizi ya Mangochi,pali chikonzero choti akatsogolere misa yotsekulira Mariatona ndi ambuye...
View ArticleBungwe la Maneb Lapempha Magulu kuti Adzipereke
Bungwe lowona za mayeso mdziko muno la National Examinations Board MANEB,lapempha magulu osiyanasiyana kuti adzipereke powonetsetsa kuti vuto lobera mayeso lipitilire kuchepa mdziko muno. Mkulu owona...
View Article