Likulu la mpingo wa katolika dziko muno ECM,kudzera ku nthambi yake ya zachitukuko ya Social Development Directorate lapereka ndalama zokwana 5 hundred thousand kwacha ku bungwe la atolankhani la MISA Malawi kuti zithandizire zokonzekera tsiku lokumbukira ufulu wofalitsa nkhani.
↧