Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Za Chuma cha Kumwamba

Ulaliki titled Zachuma Cha Kumwamba by Father James Chizuma

View Article


Ndewu Pakati Pa Njoka ndi Chule

Ulaliki titled Ndewu Pakati Pa Njoka ndi Chule by Father James Chizuma

View Article


NZIKA ZILI NDI UDINDO PA ZISANKHO ZA 2014-MEC

Bungwe la Malawi Electoral Commission (MEC), lati nzika za m’dziko lino zikuyenera kuonetsa udindo wawo potenga mbali pazisankho zachaka cha mawa polembetsa m’nkaundula wa mavoti. Wapampando wa bugweli...

View Article

A CCJP media statement in total condemnation of the resurgence of the...

1.0.            Preamble The Catholic Commission for Justice and Peace (CCJP) of the Episcopal Conference of Malawi is a social justice and advocacy arm of the Catholic Church in Malawi that is...

View Article

Mfumu Zwelithini ya Mdziko la South Africa Ikuyembekezeka Kudzudzula Anthu...

Mfumu yachizulu Good-will Zwelithini ya mdziko la South Africa ikuyembekezeka kulankhulapo popempha mzika za dzikolo kuti zisiye kuchitira mtopola mzika za mmayiko ena zomwe zikukhala mdzikolo pa...

View Article


Anthu Achitepo Kanthu Pofuna Kuchepetsa Imfa za pa Nyanja

Mtsogoleri wampingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco wapempha mayiko padziko lonse kuti achitepo kanthu pofuna kuchepetsa imfa za anthu omwe akumwalira panyanja, paulendo opita mmayiko a ku...

View Article

Bungwe la Law Society ndi lokhudzidwa ndi Mavuto omwe Dziko Lino Likukumana Nawo

Bungwe lowona za malamulo mdziko muno la Law  Society lati ndi lokhudzidwa kwambiri ndi mavuto omwe dziko lino layamba kukumana nawo posachedwapa pankhani zosiyanasiyana. Ena mwa mavuto omwe bungweli...

View Article

MESSAGE FOR VOCATION SUNDAY – 26 APRIL 2015

  Theme: Do not be afraid, God does not abandon us   Dear Brothers and Sisters in the Lord, The Fourth Sunday of Easter, which is the Good Shepherd Sunday, 26thApril 2015 is Vocation Sunday. It is a...

View Article


Apereka nthandizo kwa Amayi Oyembekezera

Wapampando wa bungwe la achinyamata ku mphakati wa St Teleza ku parish ya St Francis mu Archdiocese ya Lilongwe a Kodwani Cornelius Zalimba, wati achinyamata m’dziko muno akuyenera kusintha makhalidwe...

View Article


Dziko la Malawi Lisainira Mgwirizano wa Za Malonda

Mgwirizano wa malonda omwe wachitika pakati dziko lino ndi dziko la Tanzania, akuti uthandiza kwambiri pa chitukuko cha za malonda m’dziko muno. Nduna ya za malonda ndi mafakitale olemekezeka a Joseph...

View Article

Dayosizi ya Mangochi Iyamikira Akhristu

Dayosizi ya Mangochi ya mpingo wa Katolika yayamikira akhristu a mpingowu komanso anthu akufuna kwabwino a mu dayosizi ya Zomba ndi Dedza, kamba kopereka thandizo la chakudya ndi zovala kwa anthu omwe...

View Article

Morsi Amulamula kuti Akakhale ku Ndende Zaka 20

Yemwe kale adali m’tsogoleri wa dziko la Egypt a Mohamed Morsi  amulamula kuti akakhale kundende ndi kukagwira ntchito yakalavulagaga kwa zaka makumi awiri 20 kamba komupeza wolakwa pa milandu...

View Article

Likulu la Mpingo Wa Katolika Lasayinirana Mgwirizano ndi Bungwe la United...

Likulu la mpingo wa Katolika pa dziko lonse ndi nthambi ya bungwe ya United Nations yosamalira ana asayinirana pangano logwilira ntchito limodzi pofuna kuthandiza achinyamata osowa pa dziko lonse....

View Article


Bungwe la Save the Children Lapempha Mayiko kuti Ateteze Anthu omwe Akumafa...

Bungwe lowona za chisamaliro cha ana la Save the Children lati ana pafupifupi 2, 500 amwalira pomafika kumapeto a chaka chino, ngati mayiko aku Ulaya sadzipereka poteteza anthu omwe akumafa pa ngozi za...

View Article

Bungwe la Prison Fellowship of Malawi Lasayinila Pangano ndi Malawi Prison...

Bungwe lomwe limapereka luso losiyanasiyana kwa anthu omwe atuluka kundende la Prison Fellowship of Malawi la m’boma la Balaka, lachisanu lasayinirana pangano ndi nthambi yoyendetsa ndende za mdziko...

View Article


Apolisi Mdziko la France Akhwimitsa Chitetezo Mmatchalitchi Akatolika

Malo 178 a mpingo wa Katolika mdziko la France kuphatikizapo matchalitchi, akuyembekezeka kutetezedwa ndi apolisi zitadziwika kuti gulu lazauchifwamba la mdziko la Syria limakonza zochita zamtopola...

View Article

Mayiko aku Ulaya Awonjezera Thandizo Lolimbana ndi Anthu Olowa Mmayiko ena...

Atsogoleri a mayiko akuulaya amvana zowonjezera thandizo lomwe amapereka pa ntchito yolimbana ndi anthu a mmayiko ena omwe amalowa mayikowo mosavomerezeka pogwiritsa ntchito mabwato. Atsogoleriwa...

View Article


OPHUNZIRA MSUKULU ZOSIYANASIYANA APHUNZITSIDWE ZA CHILENGEDWE

Unduna woona zachilengedwe ndi kusintha kwa nyengo wati ugwira ntchito ndi unduna wa zamaphunziro ndi cholinga choti ophunzira m’sukulu zosiyanasiyana aziphuzitsidwa mokwanira momwe angamasamalire...

View Article

Mutharika wati Amalawi Safa ndi Njala

Mtsogoleri wa dziko lino Proffessor Arthur Peter Mutharika walonjeza amalawi kuti palibe amene akumane ndi vuto la kusowa kwa chakudya  chaka chino. Mtsogoleriyu walankhula izi lachiwiri pa msonkhano...

View Article

Asilikali a Dziko la Nigeria Apulumutsa Anthu 300 ku Zigawenga za Boko Haram

Asilikali a mdziko la Nigeria apulumutsa anthu pafupifupi mazana atatu  omwe amasungidwa mu nkhalango ina ndi zigawenga za chisilamu za Boko Haram m’dzikomo. Anthuwa omwe  mazana awiri ndi atsikana...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>