Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Bungwe la Maneb Lapempha Magulu kuti Adzipereke

Bungwe lowona za mayeso mdziko muno la National Examinations Board MANEB,lapempha magulu osiyanasiyana kuti adzipereke powonetsetsa kuti vuto lobera mayeso lipitilire kuchepa mdziko muno. Mkulu owona...

View Article


Zuma wati Dziko Lake ndi la Mtendere

Mtsogoleri wa dziko la South Africa Jacub Zuma wati anthu amene amachitira alendo ziwembu mdzikolo ndi ochepa kwambiri poyerekeza ndi anthu omwe amakonda mtendere. Pulezidenti Zuma wanena izi lachisanu...

View Article


Ma Episkopi Adzipereke pa Ntchito Yophunzitsa Anthu Nkhani Zokhudza Banja

Atsogoleri a mipingo yosiyanasiyana kuphatikizapo maepiskopi a mpingo wakatolika mdziko la America ati apitiliza kudzipereka pa ntchito yophunzitsa anthu nkhani zokhudza banja lapakati pa mwamuna ndi...

View Article

Papa Francisco Ayamikira Asilikali pa Ntchito Yabwino

Mtsogoleri wa mpingo wa katolika pa dziko lonse Papa Francisco wayamikira asilikali omwe amagwira ntchito ya  chitetezo ku likulu la mpingowu ku Vatican pa ntchito yabwino yomwe amagwira. Papa...

View Article

Bungwe la NYD likhazikitsa Pulojekiti ya Chisankho cha Moyo Wanga

Pofuna kuwonetsetsa kuti atsikana ndi amayi akulimbikitsidwa pa ntchito yodziyimira pawokha, bungwe lomwe si laboma la Network for Youth Development likhazikitsa ndondomeko ya ndalama zokwana 25...

View Article


Anthu Pafupifupi 6 Thousand Agwidwa pa Nyanja ya Mediterranean

Anthu oposa 5 sauzande 800,agwidwa mu nyanja ya Mediterranean sabata yapitayi, pamene anthu ogwira ntchito yowona zachitetezo cha anthu pa nyanjayo akhwimitsa chitetezo. Pantchitoyi achitetezowo, apeza...

View Article

Anthu 137 Amila pa Nyanja ya Mediterranean

Malipoti akusonyeza kuti anthu 137 ndi omwe amwalira  munyanja ya Mediterranean bwato lomwe anakwera litamira pa doko la Sicily mdziko la Italy. Malipoti a Wailesi ya BBC ati anthu makumi ndi anayi ndi...

View Article

Apolisi M’boma la Balaka Alangiza Woyendetsa Galimoto Kugwilitsa Tchito...

Apolisi m’boma la Balaka alangiza anthu oyendetsa galimoto kuti adzigwiritsa ntchito zizindikiro zapanseu pofuna kupewa ngozi.   Apolisiwa apereka  langizoli msungwana wazaka khumi ndi zitatu ndi bambo...

View Article


Papa Francisco Akuyembezeka Kukumana ndi Mtsogoleri wa Dziko la Cuba

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco, akuyembekezeka kukumana ndi Pulezidenti wa dziko la Cuba a Raul Castro ku likulu la mpingowu la Mulungu likudzali. Malinga ndi uthenga...

View Article


Anthu Anayi Afa Mdziko la Burundi

Anthu anayi aphedwanso pa ziwawa zomwe zikuchitika mdziko la Burundi pamene anthu akumbali yotsutsa boma akukana kuti mtsogoleri wa dzikolo ayimenso kachitatu pachisankho chomwe chichitike mdzikolo...

View Article

Mzimayi Ataya Mwana Patchire

Apolisi m’boma la Dowa amanga mayi wazaka makumi anayi ndi chimodzi 41, yemwe ndi m’busa wa mpingo wa Assemblies of God ku Mvera m’bomalo chifukwa chotaya mwana wake patchire atangobadwa kumene....

View Article

Papa Francisco Wayamikira Mgwirizano wa Pakati pa Zipembedzo

Mtsogoleri wampingo wakatolika padziko lonse Papa Francisco wayamikira mgwirizano omwe ulipo pakati pa zipembedzo padziko lonse. Papa Francisco,amalankhula izi lachinayi pa msonkhano wa akuluakulu a...

View Article

PRESS RELEASE

  NATIONAL CELEBRATION OF YEAR OF CONSECRATED LIFE: MAULA PARISH   Saturday 16th May 2015   The Catholic Church in Malawi has joined the rest of the Catholic faithful in the world in celebrating the...

View Article


Dayosizi ya Zomba Yapempha Anthu Akufuna Kwabwino kuti Athandize RMM Zomba...

Ofesi yofalitsa nkhani mu dayosizi ya Zomba yapempha anthu akufuna kwabwino kuti athandize dayosiziyi ndi zipangizo zogwilira ntchito ku studio ya Zomba ya Radio Maria ndi cholinga choti dayosiziyi...

View Article

Papa Alimbikitsa ma Episkopi a Mdziko la Mozambique kuti Akhale pa Ubale...

Mtsogoleri wampingo wakatolika padziko lonse Papa Francisco walimbikitsa  maepiskopi a mdziko la Mozambique kuti apitilize kukhala paubale wabwino ndi ansembe awo powathandiza pa zosowa za moyo wawo...

View Article


Bambo wina Apezeka Atafa M’boma la NtchisiBambo wina Apezeka Atafa M’boma la...

Bambo wina m’boma la Ntchisi wapezeka atafa mmudzi mwa Gamba kwa mfumu yayikulu Chilooko. Malinga ndi wofalitsa nkhani za apolisi m’bomali Sergent Gladson M’bumpha bamboyo anapezedwa ndi a Thokozani...

View Article

Good Luck Jonathan Achenjeza Nduna Zake

Pamene dziko la Nigeria likuyembekezeka kulumbilitsa mtsogoleri watsopano kumapeto a mwezi uno, pulezidenti  Good Luck Jonathan yemwe akuchoka paudindowu, wawopseza nduna zake kuti zizunzika kwambiri...

View Article


Mabungwe a Mpingo Wakatolika Ogwila Ntchito za Chifundo Ayamba Msonkhano Wawo...

Mabungwe 164 a mpingo wakatolika omwe amagwira ntchito zachifundo padziko lonse omwe adabwera pamodzi ndikupanga bungwe la Caritas International, lachiwiri ayamba msonkhano wawo wa pachaka pofuna...

View Article

Wogwirizira Kayendetsedwe ka Ntchito mu Dayosizi ya Zomba Wamwalira

Likulu la mpingo wakatolika mdziko muno lati ndi lokhudzidwa kwambiri ndi imfa ya Bambo mfumu a parishi ya Zomba Cathedral mu dayosizi ya Zomba Bambo Henry Kaleso omwe amwalira lachitatu masana....

View Article

Monsignor Henry Kaleso Ayikidwa Mmanda

Mpingo wakatolika mdziko muno wati malemu Bambo Henry Kaleso omwe akhala akugwira ntchito zoyendetsa dayosizi ya Zomba, anali   munthu odzipereka kwambiri pantchito zotumikira mpingo komanso anthu....

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>