Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Anthu omwe Ali Paulendo waku Yerusalemu Apite ndi Cholinga Chimodzi

Akhristu omwe ali paulendo okamphera ku malo oyera ku Yerusalemu chaka chino awapempha kuti adzapite ku malowa ndi cholinga chimodzi chokapemphera kuti ayambe moyo watsopano. Mtsogoleri waulendowu...

View Article


Ntchito Yotolela Thandizo la Radio Maria Itha Lolemba

Ntchito yotolera thandizo la Radio Maria yotchedwa Mariatona yomwe imachitika m`masiku  atatu ati itha lolemba pa 17 May 2015. Malinga ndi  mkulu owona za maporogaramu ku wailesiyi Bambo Josephy Kimu...

View Article


Ambuye Msusa Asankhidwa Kukhala Apostolic Administrator wa Dayosizi ya Zomba

Mtsogoleri wa mpingo wa katolika padziko lonse Papa Francisco wasankha  Olemekezeka Ambuye Thomas Luke Msusa,omwe ndi arkepiskopi wa arkdayosizi ya Blantyre kukhala woyendetsa dayosizi ya Zomba ngati...

View Article

Anthu Pafupifupi 9 Sauzande Afa pa Ngozi ya Chivomerezi Mdziko la Nepal

Anthu oposa 8 sauzande 500 ndi omwe afa pangozi ziwiri za chivomerezi zomwe zagwedeza dziko la Nepal masiku apitawa. Malipoti a wailesi  yakatolika ku likulu la mpingowu ku Vatican ati padakali pano...

View Article

Dziko la South Africa Labwenza Mzika za Mdziko la Mozambique Kwao

Dziko la South Africa labweza anthu oposa mazana anayi 400 a mdziko la Mozambique omwe amakhala mdzikolo alibe zitupa zowayenereza. Dzikolo lachita izi pambuyo pa ziwembu  zomwe mzika za dzikolo...

View Article


Malemu Sister Mzaza Ayikidwa Mmanda

Mwambo woyika mmanda thupi la malemu Sister Anastazia Mzaza a chipani cha Charity of Ottawa wachitika lolemba ku parish ya Ludzi m’boma la Mchinji. Sister Anastazia Mzaza,anabadwa pa 10 November mchaka...

View Article

Kusamvana Kukupitilira Mdziko La Burundi pa Chisankho chomwe Chichitike Mdzikolo

Boma la dziko la Burundi lati silibwenzera anthu omwe akukhudzidwa mugulu lomwe lakhazikitsidwa lofuna kuchotsa pampando Pulezidenti Pierre Nkuruzinza kuti asayimenso pa chisankho chomwe...

View Article

Bomba Lapha Anthu Asanu Ndi Awiri Mdziko La Nigeria.

Anthu asanu ndi awiri afa pa msika wina mdziko la Nigeria ndi bomba lomwe linaphulitsidwa pa msikawo. Malinga ndi malipoti a BBC aka ndi kachiwiri sabata ino izi kuchitika ku mpoto kwa dzikoli pomwenso...

View Article


Ark Episkopi Gabriel Anokye Wasankhidwa Kukhala Mkulu Wa Caritas...

Ark Episkopi wa mdziko la Ghana Gabriel Justice Yaw Anokye wasankhidwa kuti akhale mtsogoleri watsopano wa bungwe la Caritas International wa mmayiko a kuno Africa. Malinga ndi malipoti a wailesi ya...

View Article


Asilikali a Mdziko la Nigeria Apulumutsa Amayi ndi Ana ku Zigawenga za Boko...

Dziko la Nigeria likusunga amayi ndi ana omwe apulumutsidwa mmanja mwa zigawenga za Boko Haram ku malo ena a asilikali pofuna kuti liziwasamalira mwanjira zosiyanasiyana. Kumalo a asilikaliwo,amayiwo...

View Article

Mutharika Atsekulira Chiwonetsero cha Malonda

Pulezidenti wadziko lino Proffesor Arthur Peter Mutharika wapempha a Malawi onse kuti agwirane manja pofuna kupititsa patsogolo chitukuko cha dziko lino. Proffesor Mutharika wanena izi lachisanu pa...

View Article

Sister Stefani Akhazikitsidwa Kukhala Odala

Mwambo okhazikitsa malemu  Sister Ireen Stefani kukhala odala wachitika loweruka lapitali mu ark dayosizi ya Nairobi mdziko la Kenya. Kadinala Polycarp Pengo yemwenso ndi arkepiskopi wa dayosizi ya Dar...

View Article

Sister Chikwawa a Chipani cha SBVM Amwalira

Sister Ellen Chikwawa a chipani asisteri cha Sisters of the Blessed Virgin Mary SBVM, amwalira. Sister Chikwawa,omwe amwalira la Mulungu madzulo, anabadwa mchaka cha 1940 mmudzi mwa Chimatila mdera la...

View Article


Pulezidenti Jonathan Akuyembekezeka Kutula Udindo Wake Lachisanu

Mtsogoleri wa dziko la Nigeria GoodLuck Jonathan,akuyembekezeka kupereka udindowu kwa mtsogoleri watsopano Muhamad Buhari lachisanu likudzali atalephera pachisankho cha pulezidenti chomwe chidachitika...

View Article

Nthambi ya CCJP ku Vatican Yati Chaka cha 2015 ndi Chofunika

Nthambi yowona za chilungamo ndi mtendere kulikulu la mpingo wakatolika ku Vatican lati chaka cha 2015 ndi chofunikira kwambiri pachitukuko cha mayiko. Mtsogoleri wa nthambiyi kulikululo Kadinala Peter...

View Article


Akhristu akhale Olimba pa Chikhulupiliro Chawo Potsata Mphatso za Mzimu Woyera

Akhristu awapempha kuti akhale olimba pa chikhulupiliro chawo posiya  makhalidwe omwe ndi osiyana ndi mphatso zomwe  Mzimu Woyera umapereka .   Nduna ya episkopi wa Arkidayosizi ya Blantyre Monsinyo...

View Article

Sister Chikwawa Ayikidwa Mmanda

Mwambo oyika m'manda thupi la malemu Sister Ellen Chikwawa wachitika lachiwiri ku likulu la chipani cha Atumiki a Maria Virgo  ku Mary View ku Nguludi m'boma la Chiradzulu. Episkopi wa Dayosizi ya...

View Article


Mpingo wa Katolika Mdziko la Burundi ndi Wokhudzidwa

Mpingo wakatolika m’dziko la Burundi wati ndi wokhudzidwa ndi momwe zinthu zilili pa ntchito yokonzekera chisankho cha Pulezidenti chomwe dzikolo likuyembekezeka kukhala nacho mwezi wa mawa. Mpingowu...

View Article

Dayosizi ya Mangochi Yakhazikitsa Ntchito Yothandiza Anthu omwe Anakhudzidwa...

Dayosizi ya Mangochi yakhadzikitsa ntchito yopereka thandizo kwa anthu amene anakhudzidwa ndi ngozi za kusefukira kwa madzi Mwambo wokhazikitsa ntchitoyi wachitikira pa msasa umene anthuwa akukhala...

View Article

Dziko la Burundi Lapempha Mzika zake Kupeleka Ndalama Zothandizira Chisankho

Dziko la Burundi  lapempha mzika za dzikolo  kuti zipereke ndalama zothandizira  pa  chisankho chomwe chikuyembekezeka kuchitika mdzikolo mwezi wa mawa.   Izi zadza pomwe bungwe la mgwirizano wa maiko...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>