Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Papa Apepesa Okhudzidwa pa Ngozi ya Ndege Mdziko la Hong-Kong

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonsePapa Franciscowapereka uthenga wa chipepeso kwa anthu amene akhudzidwa pa ngozi ya ndege yomwe yagwa mu mzinda waKyrgyzstanmdziko laHong-Kong. Malipoti a...

View Article


Ntchito Yofufuza MH370 Yaimitsidwa

Ntchito yofufuza ndege ya MH370 ya mdziko la Malaysia yomwe inasowa zaka zitatu zapitazo ati ayamba ayiyimitsa. Malinga ndi malipoti a wailesi ya BBC, mayiko a Australia, Malaysia komanso China aganiza...

View Article


Apempha Anthu Apitirize Kugwirana Manja ndi Apolisi

Anthu okhala mdera la mfumu yayikulu Bvumbwe m’boma la Thyolo awapempha kuti apitirize kugwirana manja ndi apolisi pa ntchito yolimbikitsa chitetezo cha ku madera. Mkulu wa apolisi ya m’delari a...

View Article

Papa Wati Ndi Udindo Wa Aliyense Kusamalira Ndi Kuteteza Ana

M'tsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse PapaFrancisko wati ndi udindo wa munthu aliyense kuwonenetsetsa kuti ana akulandira chisamaliro ndi chitetezo chabwino. Papa walankhula izi lachitatu...

View Article

Asilikali Apulumutsa Ana 53 Omwe Anabedwa Ku Ethiopia

Asilikali m’dziko la Ethiopia ati akwananitsa kupulumutsa ana makumi asanu ndi atatu 53 omwe anabedwa ndi gulu lina la zigawenga m’dzikomo. Malingana ndi malipoti a wailesi ya BBC anawa akuti anagwidwa...

View Article


Jammeh Watuluka Mdziko la Gambia

Mtsogoleri wakale wa dziko la Gambia, Yahya Jammeh wachoka mdzikolo atavomereza kugonja kwake pa chisankho atalamulira dzikolo kwa zaka 22. Malipoti a wailesi ya BBC ati Jammeh pakadali pano ali mdziko...

View Article

Papa Apempha Akhristu Alimbikitse Umodzi, Apemphelera Okhudzidwa Ndi Zivomerezi

Mtsogoleri wa mpingo wa katolika pa dziko lonse papa Francisco wapempha akhristu kuti agwirane manja popemphelera umodzi  pakati pawo. Malinga ndi malipoti a wailesi ya Vatican ati papa wanena izi...

View Article

Radio Maria Malawi Yakonzeka Kutumikira Omvera Ake Mchaka Cha 2017

Radio Maria Malawiati yakonza ndondomeko zosiyanasiyana pofuna kupititsa patsogolo ntchito za wailesiyi ndi cholinga choti itumikire bwino omvera ake mchaka cha 2017. Mkulu woyendetsa mapologalamuku...

View Article


Anthu 18 Afa Kamba ka Nyengo Yoipa Mdziko la America

Anthu pafupifupi 18 afa ndipo ena ambiri avulala kutsatira nyengo yoipa kum’mwera kwa dziko la America. Malipoti a wailesi ya BBC ati gavanala wa ku Georgia walengeza kuti madera asanu ndi awiri 7...

View Article


11 Million Dollars Zasowa Mdziko la Gambia

Ndalama zoposa 11 million za America akuti zasowa mdziko la Gambia kutsatira kuchoka kwa mtsogoleri wa kale wa dzikolo a Yahya Jammeh. Malipoti a wailesi ya BBC ati pali chisonyezo chakuti a Jammeh aba...

View Article

Bungwe la CCJP Lati Ntchito ya Chilungamo cha Mmudzi Ikupindulira Anthu

Bungwe la chilungamo ndi mtendere CCJP mu Arch dayosizi ya Blantyre ya mpingo wakatolika lati ndi lokhutira ndi momwe ntchito yothandiza anthu kumvetsa ma ufulu awo ndi kupereka uphungu pa milandu...

View Article

Papa wati Mauthenga Azibweretsa Kusintha

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco walimbikitsa anthu kuti akhale ndi kuthekera kwabwino kopereka mauthenga ndi cholinga chofuna kuti dziko lonse liziyenda mu chowona komanso...

View Article

Maepiskopi a Mdziko la America Sakugwirizana ndi Maganizo a Trump

Maepiskopi a Mdziko la America Sakugwirizana ndi Maganizo a Trump Bungwe la maepiskopi a mpingo wakatolika mdziko la America la United States Conference of Catholic Bishops latsutsa maganizo a...

View Article


Mipingo ya M’dera la Chimwala Ichita Mwambo wa Umodzi wa Akhristu

Mipingo ya chikhristu yopezeka m’dera la aSenior Chief Chimwalam’boma laMangochiayiyamikira kamba kodzipeleka pa ntchito zolimbikitsa umodzi pakati pawo. Mkulu woyendetsa ntchito za umodzi wa mipingo...

View Article

Dziko la Columbia Likufuna Kuthetsa Kulima Mbewu ya Coca

Dziko la Columbia lalengeza za mapulani ofuna kuthetsa kulima mbewu ya Coca yomwe amapangira mankhwala ozunguza bongo a Cocaine. Malipoti a wailesi ya BBC ati alimi amene  achotse mbewu zawo okha...

View Article


Trump Aletsa Mzika za Syria Kulowa Mdziko la America

Mtsogoleri wa dziko la America, Donald Trump wayimitsa ndondomeko ya anthu othawa kwawo ya dzikolo ndipo waletsa anthu a mdziko la Syria kulowa mdziko la America. Malipoti a wailesi ya BBC ati...

View Article

Papa Apereka Uthenga wa Chipepeso ku Dziko la Chile

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco ati wapereka uthenga wa chipepeso kwa anthu onse omwe ataya abale awo komanso omwe akhudzidwa pa  ngozi ya moto wachilengedwe mchigawo...

View Article


Papa Ayamikira Ziwonetsero Zoteteza Moyo Mdziko La America

Mtsogoleri wa mpingo wa katolika pa dziko lonse Papa Francisco wayamikira onse omwe anatenga nawo mbali pa ulendo wa ndawala woteteza ufulu wa moyo womwe wachitika dzulo lachisanu mu mzinda wa...

View Article

CADECOM Iwonetsetsa Kuti Anthu Akukhala ndi Chakudya Chokwanira

Bungwe la CADECOM mu dayosizi ya Zombalati liwonetsetsa kuti anthu mu dayosiziyo akukhala ndi chakudya chokwanira ngakhale nyengo ikusintha. Mkulu wa bungwe la CADECOM mu dayosizi yo bambo Patrick...

View Article

Dr. Kumpalume Achenjeza Anthu Ochita Chinyengo Mzipatala za Boma

Unduna wa zaumoyo wati uthana ndi anthu onse ochita zachinyengo mu ntchito ya zaumoyo mdziko muno. Nduna mu undunawu Dr. Peter Kumpalume ndi omwe anena izi pa mwambo omwe bungwe la Clinton Health...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>