Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Kaliati Wayamikira Mpingo Wakatolika Podzipereka Kufalitsa Uthenga Wabwino

Mpingo wakatolika m’dziko muno awuyamikira kamba kodzipereka pa ntchito zofalitsa uthenga wabwino. Nduna ya zofalitsa nkhani ndi kuphunzitsa anthu zinthu zosiyanasiyana mayiPatricia Kaliati ndi omwe...

View Article


Ntchito Yolumikiza Magetsi Mmidzi Idya 8 Billion Kwacha

Boma lati ntchito yolumikiza magetsi m’madera akumidzi ikuyembekezeka kudya ndalama zokwana 8 Billion kwacha. Nduna yoona za chilengedwe komanso mphamvu za magetsi a Bright Nsaka ati gawoli ndi la...

View Article


Mphamvu za Mpingo Wakatolika Zili pa Akhristu Ovutika Mchikhulupiliro-Papa

Mtsogoleri wa mpingo wa Katolika pa dziko lonse Papa Fransisko wati mphamvu za mpingo wa Katolika zatsamira kwambiri pa akhristu ochepa omwe akuvutikabe kaamba ka chikhulupiliro chawo. Iye amalankhula...

View Article

Dayosizi ya Mangochi Ilimbikitsa Achinyamata Kutenga Mbali mu Mpingo

Dayosizi ya mpingo wa katolika ya Mangochi yati iwonetsetsa kuti achinyamata akutenga nawo mbali pa zochitika zonse za mpingo. Mlembi wa episkopi wa dayosiziyi bambo Steven Kamanga anena izi pa...

View Article

Dziko La Indonesia Lidzudzula President Trump

Wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko la Indonesia a Jusuf Kalla wati ndondomeko yomwe dziko la America lokonza poletsa anthu ochokera ku Mayiko a chisilamu kulowa mdziko la America, kukupereka chikayiko...

View Article


Trump wati Sakudana ndi Chipembedzo cha Chisilamu

Mtsogoleri wa dziko la America Donald Trump wati ganizo lake loletsa nzika zina zochokera ku mayiko ena achisilamu kulowa mdzikolo sikukutanthauza kuti akudana ndi chipembedzo chachisilamu. A Trump...

View Article

Papa wati Chipulumutso Chikuyenera Kuvalidwa Ngati Chipewa

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco wapempha akhristu kuti avale chiyembekezo cha chipulumutso ngati chipewa chodzitetezera pa ngozi ya njinga  pozindikira kuti kuwuka kwa...

View Article

Mamuna Wina Wamira M’boma la Ntchisi

Mamuna wina m’boma la Ntchisi ati wafa atamira mu mtsinje wa Bua komwe anapita kukawedza nsomba. Wofalitsa nkhani za apolisi mbomali Sergent Gladson M’bumpha watsimikiza za nkhaniyi. Sergent M’bumpha...

View Article


Papa Francisko Wakhazikitsa Stanislaus ndi Maria Elizabeti Kukhala Oyera

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisko wakhazikitsa Stanislaus wa Yosefe ndi Maria komanso Maria Elizabeti Hesselblad kukhala oyera. Papa wakhazikitsa awiriwa kukhala oyera...

View Article


Anthu Asanu Ochita Masewero Opalasa Njinga Afa Atagundidwa Ndi Galimoto

Anthu asanu ochita masewero opalasa njinga afa ndipo ena anayi avulala galimoto lina litawaomba ku Michigan m’dziko la America. Anthu-wa ati agundidwa ndi galimoto la mtundu wa Pick Up lomwe pa...

View Article

Papa Apempha Akhristu Azipemphelera Atumiki a Mulungu

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco wapempha anthu kuti azipemphelera atumiki a Mulungu omwe anayitanidwa kuti atumikire Mulungu. Papa amalankhula izi ku likulu la mpingowu ku...

View Article

Ambuye Msusa Adandaula Kamba ka Kusagwiritsa Ntchito Bwino Chilengedwe

Arkiepiskopi wa arkidayosizi ya Blantyre ya mpingo wakatolika Ambuye Thomas Luke Msusa wadandaula kuti dziko la Malawi likulephera kugwiritsa  ntchito moyenera zachilengedwe zomwe lili nazo. Ambuye...

View Article

Msilikali Amangidwa Kamba Kobera Anthu Ndalama

Apolisi m’boma la Karonga ati akusunga mchitokosi msilikali wina wa ku Cobbe barracks ku Zomba kaamba komuganizira kuti amalandira ndalama zokwana 80 sauzande kwacha kwa anthu a mmidzi ina ya m’bomalo...

View Article


Apolisi M’dziko la New Guinea Akuwaganizira Kuti Apha Ophunzira Anayi Omwe...

Apolisi m’dziko la New Guinea akuwaganizira kuti apha ophunzira anayi   a pa sukulu ina ya ukachenjede omwe amachita chionetsero chosonyeza kusakondwa ndi zochita za nduna yaikulu ya dzikolo. Malingana...

View Article

Anthu Makumi Atatu Afa Zigawenga za Islamic State Zitaphulitsa Bomba La Timke...

Anthu makumi atatu afa, ndipo ena 80 avulala  gulu la zigawenga la Islamic State litaphulitsa  mabomba awiri atinkenawo  munzinda wa Baghdad  m`dziko la Iraq Malinga ndi malipoti awailesi ya BBC, bomba...

View Article


Anthu Asanu Ochita Masewero Opalasa Njinga Afa Atagundidwa Ndi Galimoto

Anthu asanu ochita masewero opalasa njinga afa ndipo ena anayi avulala galimoto lina litawaomba ku Michigan m’dziko la America. Anthu-wa ati agundidwa ndi galimoto la mtundu wa Pick Up lomwe pa...

View Article

Papa Wati Akhristu Apempherere Mtendere wa Mmaiko Onse

M’tsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Franciskowapempha anthu ndi akhristu a mpingowu kuti lachitatu akumbukire kupemphelera mtendere wa m’mayiko pa dziko lonse. Malinga ndi malipoti a...

View Article


Nthambi Ya Zachilungamo Igwirizana Ndi Lamulo La Trump

Nthambi ya zachilungamo mdziko la America yati ikugwirizana ndi zomwe mtsogoleri wa dzikolo, Donald Trump wachita poletsa  anthu a m’maiko ena a chisilamu kolowa mdzikolo. Malinga ndi malipoti a...

View Article

Mayi Afa pa Ngozi ya pa Nsewu M’boma la Mangochi

Mayi wina wa zaka 52 zakubadwa wafa atawombedwa ndi galimoto m’boma la Mangochi. Wofalitsa nkhani za apolisi m’bomalo Sergeant Amina Tepani Daudi wauza Radio Maria Malawi kuti mayiyu Martha Kuswenje...

View Article

Kanyongolo Wapempha Boma Libwezeretse Maubale Ndi Maiko Ena

Katswiri wa malamulo yemwenso ndi mphunzitsi wa malamulo pa sukulu ya ukachenjende ya Chancellor, Professor Edge Kanyongolo wapempha boma  kuti libwezeretse ubale womwe unasokonekera pakati pa boma la...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>