Dziko la South Sudan Lalengeza Madera Omwe Akhudzidwa ndi Njala
Dziko la South Sudan lalengeza kuti mmadera ena a mdzikolo anthu akuvutika ndi njala. Malinga ndi boma la dzikolo komanso bungwe lowona za mgwirizano wa maiko a pa dziko lonse la United Nations UNanthu...
View ArticleAfa Atawombedwa ndi Galimoto ku Ntchisi
Bambo wina wafa ataombedwa ndi njinga ya moto m’boma la Ntchisi. Wofalitsa nkhani za apolisi m’bomalo, Sergeant Gladson Mbumpha wati a Bruno Malithano a zaka 38zakubadwa anakwezana njingayo yomwe ndi...
View ArticleAtolankhani Atenge Mbali Poteteza Anthu Achikulire
Bungwe lomenyera ma ufulu a anthu achikulire, la Malawi Network of Older People (MANEPO) lati atolankhani ndi ofunika pa ntchito yoteteza maufulu a anthu achikulire mdziko muno. Mkulu wa bungweri a...
View ArticleBwanamkubwa wa Balaka Apempha Mgwirizano
Khonsolo ya boma la Balaka yapempha kuti pakhale ubale wabwino pakati pa adindo ndi makomiti a za chitukuko m’bomalo. Bwanamkubwa wa bomalo, Rodrick Mateauma ndi yemwe wanena izi potsatira mphekesera...
View ArticleAnthu 70 Afa pa Nyanja ya Atlabtic
Matupi oposera 70 a anthu akufa akuti apezeka akuyandama kudera lina mu nyanya yayikulu ya Atlantic m’dziko la Lybia. Akatswiri pa ntchito zopulumutsa anthu pa ngozi zochitika pamadzi akuti ndi amene...
View ArticleAmayi Awiri Akayankha Mlandu Wopha Kim Jong-Nam
Amayi ena awiri akuyembekezeka kukawonekera ku bwalo la milandu mawa ndi kukayankha mlandu wokhudzana ndi kuphedwa kwa mchimwene wake wa mtsogoleri wa dziko la North Korea,Kim Jong-Nam. Malipoti a...
View ArticleAnthu Atatu Amangidwa Kamba Koba Katundu ku CADECOM
Apolisi m’boma la Balaka agwira anthu atatu omwe akuwaganizira kuti ndi amene akukhudzidwa ndi mulandu wakuba ku malo a mpingo wakatolika a CADECOM ku Ulongwe ndi ku malo a zaulimi wa nthilira a...
View ArticleChipani cha MCP Sichikudziwapo Kanthu pa “Antchito”
Chipani cha Malawi Congress(MCP) chati sichikudziwapo kanthu kwa achinyamata omwe akuti anabwera ku likulu la chipanichi m’chigawo cha ku m’mwera kudzafuna malipiro awo a ntchito. Wapampando wa chipani...
View ArticleMACRA Ikondwelera Tsiku Lokumbukira Wailesi pa Dziko Lonse
Dziko laMalawimawa ligwilizana ndi mayiko pa dziko lonse pochita mwambo wa tsiku loganizira nyumba zoulutsira mawu padziko lonse (World Radio Day). Mwambo wa ukulu woganizira tsikuli unachitikira ku...
View ArticleAnthu 26,000 Athawa Mu Mzinda Wa Mosul
Anthu okwana 26 sauzande a m’dziko la Iraq athawa kum’mvuma kwa mzinda wa Mosul pa masiku okwana khumi 10 potsatira kumenyana komwe kunabuka pakati pa asilikali a dzikolo ndi zigawenga za Islamic State...
View ArticleGogo Afa Khoma la Nyumba Litamugwera
Mayi wina wafa khoma la nyumba litamugwera m’boma laNtchisi. Malingana ndi ofalitsa nkhani za apolisi m’bomaloSergeantGladson Mbumpha,malemu mayiMelina Felix akuti khudzidwa ndi imfayi pa nthawi imene...
View ArticleTsvangirai Wamwalira
Mtsogoleri wa zipani zotsutsa boma ku nyumba ya malamulo mdziko la Zimbabwe, Morgan Tsvangirai wamwalira. Malipoti a wailesi ya BBC ati Tsvangirai wamwalira pa chipatala china cha mdziko la South...
View ArticleSam Mpasu Wamwalira
Mtsogoleri wa chipani cha New Labour, a Sam Mpasu apezeka atafa ku nyumba kwawo. Mneneri wa ku banja a Stanly Wasi, ati akukhulupilira kuti a Mpasu omwe anakhalaponso sipikala wa nyumba ya malamulo...
View ArticleZuma Atula Pansi Udindo
Mtsogoleri wa dziko la South Africa, Jacob Zuma watula pansi udindo wake. Malinga ndi malipoti a wailesi ya BBC, Zuma wati akuchoka pa udindowu mwa kufuna kwake osati kaamba kokakamizidwa ndi chipani...
View ArticleApha Msuweni Kaamba Kogona ndi Mkazi Wake
Apolisi m’boma la Mchinji amanga mamuna wina kaamba komuganizira kuti anapha msuweni wake atamugwira akuchita zadama ndi mkazi wake. Malinga ndi wofalitsa nkhani za apolisi m’bomalo, Inpector Kaitano...
View Article