Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

ANA ATATU AFA KUDOWA PA NGOZI ZOSIYANASIYANA

  Ana awiri ku Mponela m’boma la Dowa afa chipupa cha nyumba yomwe anagona chitawagwera. Mneneli wa apolisi ku Mponela  a Kondwani Kandiado atsimikiza za nkhaniyi ndipo ati ,anawo ndi Angella Hastings...

View Article


MAGANIZO A ANTHU PA ZA KUPUMA UDINDO WA APAPA

  Pamene anthu akupitiliza kuthilirapo ndemanga pa ganizo la mtsogoleri wa Mpingo waKatolika pa dziko lonse, Papa Benedikito wachi 16 lopuma pa udindowu mwezi uno,anthu mdziko muno ayamikira papayu...

View Article


"PAPA AKHONZA KUKHALA WA KU AFILIKA", KADINALA TURKSON

Kadinala Peter Appiah Turkson wa m’dziko la Ghana wati mtsogoleri watsopano wa Mpingo wakatolika pa dziko lonse akhonza kukhala wa ku Afilika. Kadinalayu ndi mmodzi mwa makadinala atatu aku Afilika...

View Article

PAPA APEMPHA MAPEMPHERO KWA AKHRISITU

Mtsogoleri wa Mpingo wa katolika pa dziko lonse Papa Benedikito wachi 16 wapempha akhrisitu kuti amupempherere pamodzi ndi Papa yemwe adzalowe m’malo mwake mtsogolomu. Papayu walankhula izi  kwa...

View Article

MPINGO WA KATOLIKA KOMANSO ANGILIKANI ALOWA M'NYENGO YA LENT

  Akhrisitu a Mpingo wa Katolika komanso Angilikani pa dziko lonse  lapansi ayamba nyengo yokumbukira masautso a Yesu Khrisitu. Nyengoyi imayamba ndi mwambo wa nsembe ya misa ya phulusa, pomwe...

View Article


DONGOSOLO LA KUTULA PANSI UDINDO KWA APAPA

Mneneli wa Mpingo wa katolika ku VatiKani  Bambo Federico Lombardi apereka dongosolo la momwe zikhalire pomwe mtsogoleri wa Mpingowu akhale akupuma komanso mmene asankhire papa  wina kumapeto a mwezi...

View Article

PAPA BENEDIKITO WA CHI 16 ATHOKONZA BUNGWE LA PRO-PETRI-SEDE ASSOCIATION OF...

Mtsogoleri wa Mpingo wa Katolika pa dziko lonse Papa Benedikito wachi 16, wayamikira bungwe lina la m’dziko la Belgium, chifukwa cha thandizo landalama lomwe limapereka ku likulu la Mpingowu. Papa...

View Article

APEMPHA BOMA KUTI LICHITEPO KANTHU PA ZAVUTO LA NJALA

Anthu a m’dera la mfumu yaikulu Katuli m’boma la Mangochi apempha boma kuti liwathandize msanga pobweretsa chimanga ku Admarc ya Katuli komwe chinatha kalekale. Pempho la anthuwo, ladza pomwenso misika...

View Article


ALAMULIDWA KUKAKHALA KU NDENDE ZAKA ZINAYI KAMBA KOBAYA MUNTHU

  Bwalo la milandu la magistrate m’boma la Dowa lalamula mwamuna wina kuti wa kumalo osungira anthu othawa kwawo a Dzaleka kuti akakhale kundende zaka zinayi kamba kovulaza mnyamata wina wa zaka 16...

View Article


M'BUSA AGWIDWA KAMBA KOGWILIRA MZIMAYI WA MISALA

Apolisi ku Dowa amanga m`busa wina yemwe ndi mzika ya dziko la Democratic Republic of Congo wa kumalo osungirako anthu othawa kwawo a Dzaleka  m’bomalo kamba komuganizira kuti adagwirila mzimayi...

View Article

AKHRISTU ATSANZIKANA NDI PAPA BENEDIKITO WA 16

Akhristu pafupifupi 100 sauzande anasonkhana kunja kwa tchalitchi la likulu la St Peters Square pofuna kuona komanso kutsanzikana ndi Papa Benedicto wa 16 yemwe akhale akutula pansi udindo wake...

View Article

AKHRISTU ALANDIRA MADALITSO KUCHOKERA KWA PAPA

Akhristu zikwizikwi anakhamukira ku likulu la Mpingo wakatolika ku Vatikani kukalandira madalitso ochokera kwa mtsogoleri wa Mpingowu pa dziko lonse Papa Benedikito wachi 16 pa umodzi mwa miyambo yake...

View Article

MSONKHANO WOSAKHA PAPA WATSOPANO UCHITIKA MWEZI WA MARCH

  Likulu la Mpingo wakatolika ku Vatikani lati msonkhano wapadera wosankha Papa watsopano udzayamba pa 15 kapena pa 19 mwezi  wa March.  Mneneli wa Mpindo wa Katolika ku Vatikani Bambo Federico Lombard...

View Article


CHANJELANI NDI BODZA LA A DEMONI

Ulaliki titled Chenjelani ndi Bodza la  a Demoni by Fr.E. Mwinganyama

View Article

ANTHU 1 SAUZANDE AKUMATENGA MATENDA A EDZI PASABATA

  Mlembi wamkulu mu ofesi yoona  za madyedwe ndi matenda a  Edzi Mai Edith  Mkawa  ati ndiwokhudzidwa ndi kufala kwa kachilombo ka matenda oyambitsa Edzi ka HIV ngakhale Boma likuyesetsa  kupeza njira...

View Article


BOMA LIFUFUZA ANTHU OMWE ANATUMA ANA KUTI ACHITE ZIONETSERO

  Boma la Malawi lati lifufufuza ndi kumanga anthu omwe adatsogolera ana a sukulu omwe adachita ziwonetsero zokwiya ndi kuima kwa maphunziro pamene aphunzitsi mumzinda wa Blantyre amachita nawo...

View Article

"MUKHALE ZITSANZO ZABWINO", BAMBO MULAVA

Abwenzi a Radio Maria awapempha kukhala zitsanzo zabwino pokondana ndi kulimbikapogwira ntchito zothandiza wayilesiyi. Wachiwiri kwa wamkulu owona za ma Pulogalamu ku wayilesiyi, Bambo Medrick Mulava...

View Article


DZIKO LA TANZANIA LIFUFUZA ZA KUPHEDWA KWA WAMSEMBE

Pulezidenti wa dziko la Tanzania a Jakaya Kikwete walamula apolisi m’dzikolo kuti afufuze mwansanga  za kuphedwa kwa wamsembe wina wa Mpingo  wa Katolika m’dzikolo. Pulezidenti Kikwete walamula izi...

View Article

OPHWANYA LAMULO, LAMULO LIDZAMUPWANYA

Ulaliki titled Ophwanya Lamulo, Lamulo lidzamuphwanya

View Article

KUTUMIKIRA MULUNGU KUMASOWA CHIKONDI

Ulaliki titled Kutumikira Mulungu Kumasowa Chikondi by Father Mwinganyama

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>