Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Papa Francisco Apereka Mwayi woti Anthu Azawone Thupi la Malemu Padre Pio

Likulu lampingo wakatolika lalengeza kuti thupi la malemu Pio oyera yemwe amadziwika bwino ndi dzina loti Padre Pio  adzalitulutsa mmanda kuti anthu adzakhale ndi mwai opereka ulemu kwa iye kuyambira...

View Article


Mwambo okondwelera kuti Ambuye Emanuel Kanyama ndi Ansembe awiri akwanitsa...

Mwambo okondwelera kuti Episkopi wa Dayosizi ya Dedza olemekezeka Ambuye Emmanuel Kanyama ndi ansembe ena awiri akwanitsa zaka 25 ali muunsembe uchitika  Loweruka pa 8 ku parishi ya St Martin De-Poris...

View Article


Papa Francisco Apempha Maiko Achitepo Kanthu Polimbana ndi Nkhaza.

Mtsogoleri wampingo wakatolika padziko lonse Papa Francisco wabwerezanso kupempha maiko padziko lonse kuti achitepo kanthu polimbana ndi nkhanza zomwe akhiristu ndi magulu ena azipembedzo...

View Article

Dziko la Philippines Likhazikitsa Masiku a Tchuthi Pamene Papa Francisco...

Pamene mtsogoleri wampingo wakatolika padziko lonse Papa Francisco akuyembekezeka kukacheza mdziko la Philippines mwezi wa mawa, meya wa mzinda wa Manila mdzikolo walamula kuti anthu mu mzindawo...

View Article

A Quest for a Better and Descent Malawi”

                        “A Quest for a Better and Descent Malawi” The Catholic Commission for Justice and Peace Media and Advocacy Statement on the Contemporary Socio-Economic and Political Context....

View Article


Anthu omwe Ali ndi Zilema Zosiyanasiyana Ali ndi Mwayi wa Maphunziro a Luso

Unduna owona kuti pasamakhale kusiyana pakati pa akazi ndi amuna, ana ndi chisamaliro cha anthu olumala wapempha anthu omwe ali ndi abale omwe ali ndi zilema zosiyanasiyana kuti apite kumaofesi a...

View Article

Bwalo Lamilandu la ICC Siligwira Ntchito Mokondera

Mmodzi mwa akaswiri owona za malamulo komanso mkulu oweruza milandu   mdziko muno wati samagwirizana ndi maganizo a anthu omwe amadzudzula bwalo la milandu la padziko lonse la International Criminal...

View Article

Papa Francisco Wakhazikitsa Tsiku la 1 September Kukhala Lopemphelera...

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco wakhazikitsa tsiku la pa 1 September chaka chino kuti likhale lopemphelera chisamaliro cha chilengedwe. Papa Francisco wakhazikitsa tsikuli...

View Article


Anthu 22 Asowa Mdziko la China

Anthu oposa makumi awiri akusowa nthaka itagumuka mdera la kumpoto chakumvuma mdziko la  China. Malipoti a BBC ati nyumba zankhaninkhani zomwe anthu ogwira ntchito pa kampani ina ya migodi mderalo...

View Article


Mabungwe Atenge Nawo Mbali pa Nkhani ya Magetsi

Kupereka mwayi ku mabungwe osiyanasiyana omwe  siaboma kutenga nawo gawo pa ntchito zokhudza magetsi mdziko muno ati kungathandize kuti  mitengo yamagetsiwa ikhale yotsikirapo. Wofalitsa nkhani ku...

View Article

Mfumu Zwelithini Ikuyembekezeka Kufika Mdziko la Zimbabwe

Mfumu yayikulu ya Angoni mdziko la South Africa Goodwill Zwelithini ikuyembekezeka kufika mdziko la Zimbabwe masiku akudzawa. Magulu osiyanasiyana omenyelera ufulu wa anthu mdziko la Zimbabwe ati mfumu...

View Article

Bambo Kamalo a mu Dayosizi ya Zomba Amwalira

Bambo Denis Kamalo omwe amatumikira  mu dayosizi ya Zomba yampingo wakatolika amwalira. Malinga ndi mkulu wamuofesi yofalitsa nkhani za dayosiziyi Bambo Steven Likhutcha,Bambo Kamalo a mwalira...

View Article

Bungwe la UN Liwulura Mayiko Omwe Akuzunza Anthu

Bungwe la mgwirizano wa mayiko la United Nations UN lati liwulula  mayiko omwe akulephera kupereka zilango kwa asilikali awo omwe akukhudzidwa ndi mchitidwe ozunza anthu osalakwa mmayiko omwe bungweli...

View Article


Bambo Kamalo Ayikidwa Mmanda

Mwambo oyika mmanda thupi la malemu Bambo Dennis Kamalo omwe amatumikira mudayosizi ya Zomba ngati wansembe mumpingo wakatolika wachitika lolemba ku Zomba Cathedral mu dayosiziyo. Bambo Kamalo amwalira...

View Article

Anthu 40 Afa ndi Bwato

Anthu pafupifupi makumi anayi afa bwato lomwe anakwera litamira chifukwa chonyamula  mopitilira muyeso mkatikati mwa nyanja ya Mediterranean mdziko la Libya. Malipoti a wailesi ya BBC ati anthu oposa...

View Article


ASisteri a Chipani cha Presentation Alimbikitsidwa mu Utumiki

M’bindikiro wa masiku asanu ndi atatu wa asisiteri a chipani cha Presentation for the Blessed Mary mu dayosizi ya Dedza watha lamulungu mudayosiziyo. M’bindikirowu omwe unachitika ndi mutu oti Mayi...

View Article

Ma episkopi Mdziko la America Adzudzula Apolisi

Maepisikopi a mdziko la America adzudzula apolisi ku mchitidwe omawopseza anthu oganiziridwa milandu omwe akuti wakula  kwambiri  mdzikolo. Ma episikopiwa adzudzula apolisiwo zitamveka kuti iwo...

View Article


Makolo M’boma la Nsanje Apitiriza Kutsatira Myambo ina Yoyipa.

Makolo ena ku nsanje  akupitirizabe kuchita miyambo ina yoipa monga kukwatiwitsa ana akadali achichepere  komanso kuwagwiritsa ntchito zokhwima zomwe ati zikumakolezera ana ambiri kusiya sukulu. Mkulu...

View Article

Hostel ya Atsikana Imangidwa pa Secondary ya Liwonde M’boma la Machinga.

Kumangidwa kwa hostel ya atsikana pa sukulu ya Secondary ya Liwonde m’boma la Machinga kuthandiza kuti atsikana ambiri ayambe kuchita bwino pa maphunziro awo. Mphunzitsi wa mkulu pa sukuluyi a Welson...

View Article

Pulezidenti Kiir Wakana Kusayinira Mgwirizano Wodzetsa Mtendere

Mtsogoleri wa dziko la South Sudan Salva Kiir wakana kusayinira mgwirizano odzetsa mtendere pakati pa iye ndi magulu owukira boma mdzikolo. Pulezidenti Kiir wakana kusayinira panganoli posachedwapa...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>