Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Dinale Ya Mangochi Idzipereka Pa Utumiki Wa Ana

Dinale ya Mangochi mu mpingo wakatolika yati idzipeleka pa ntchito yolimbikitsa ntchito za utumiki wa ana. Sister Marita Tepelo achipani cha Devine Providence otumikira mu dinaleyi ndi omwe anena izi...

View Article


Zigawenga za IS Zagonjetsedwa

Asilikali a mdziko la Iraq ati ali kumapeto kwa ntchito yogonjetsa zigawenga zachisilamu za Islamic State zomwe zinakhazikika mu mzinda wa Mosul mdzikolo kuyambira mu chaka cha 2014. Malinga ndi...

View Article


Papa Akumbutsa Makadinala Atsopano Ntchito Yawo

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco walimbikitsa makadinala asanu omwe wangowadzoza kumene kuti ntchito yao ndi kutumikira akhristu. Papa amalankhula izi ku likulu la mpingowu...

View Article

Anthu Anayi Afa Pa Ngozi Ya Galimoto

Anthu anayi afa ndipo ena avulala modetsa  nkhawa pa ngozi ya galimoto zomwe zinaombana  m’boma la Dowa. Malinga ndi ofalitsa nkhani za apolisi m’bomalo Sergent Richard Kaponda ngoziyi yachitikira...

View Article

Apempha Akhristu Kupemphelera Mtendere ndi Mgwirizano

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco wapempha akhristu pa dziko lonse kuti apemphelere mtendere ndi mgwirizano m’dziko la Venezuela. Papa amalankhula izi ku likulu la mpingowu...

View Article


Bambo Wina Wapha Mkazi Wake Kaamba Ka Nsanje.

Apolisi ku Kanengo mu m’zinda wa Lilongwe akusunga m’chitolokosi bambo wina wa dzaka 36 zakubadwa kamba komuganizira kuti anamenya ndikupha mkazi wake. Ofalitsa nkhani za apolisi ku delaro Sergeant...

View Article

Akhristu Apemphedwa kutengapo Mbali Mu Mpingo Wa Katolika

Akhristu a mpingo wa katolika awapempha kuti  azilimbikitsa magulu osiyanasiyana amu mpingo-wu ngati njira imodzi yopititsira patsogolo moyo wachipembedzo mu mpingo. Wapampando opuma ku tchalichi la St...

View Article

Boma la Balaka Lichita Tsiku Loganizira Mwana wa ku Africa

Makolo ati ali ndi udindo wolimbikitsa ufulu  wa ana powonetsetsa kuti ufulu wao wa maphunziro ndi maufulu ena akukwaniritsidwa. Bwanamkubwa wa boma la Balaka a Rodrick Mateauma ndi omwe alankhula izi...

View Article


Mnyamata Afa Ndi Ngozi Ya Moto

Mnyamata wina wafa pa ngozi ya moto wa petulo umene unabuka mu golosale yake yomwe inali pa msika wa Chisamba m’boma la Ntchisi. Ofalitsa nkhani za apolisi m’bomali Sergeant Gladson Mbumpha...

View Article


Anthu makumi Asanu Amira pa Nyanja ya Meditteranean

Bwato lomwe linanyamula anthu oposa makumi asanu akuliganizira kuti lamira pa nyanja yaikulu ya Meditteranean mdziko la Morocco. Malinga ndi malipoti a bbc magulu opulumutsa anthu pa ngozi za pa madzi...

View Article

Anthu Apewe Kusankhana Mitundu

M’tsogoleri wa dziko lino Professor Peter Muthalika wapempha anthu m’dziko muno kuti azipewa kusankhana mitundu kamba koti izi sizingathandize pa chitukuko cha dziko lino. President Muthalika wanena...

View Article

Sister Maloya a Chipani cha SBVM Ayikidwa Mmanda

Mwambo woika m’manda thupi la malemu sister Patricia Maloya chipani cha Atumiki a Maria Virigo Woyera uchitika lero ku Maryview ku Nguludi m’boma la Chiradzulu. Malinga ndi a ku likulu la chipani-chi...

View Article

Mafumu Ati Adzigwira Ntchito Limodzi ndi Boma

Mfumu yayikulu Mbenje ya m’boma la Nsanje yalangiza mafumu m’dziko muno kuti adzigwira ntchito limodzi ndi boma lomwe likulamula ndi cholinga chofuna kulimbikitsa ntchito za chitukuko m’dziko lino....

View Article


Apempha Akhristu Kukhala Chitsanzo Chabwino

Akhristu a m’phakati wa St Peters ku parish ya Sacred Heart mu dayosizi ya Zomba awalangiza kuti akhale chitsanzo chabwino komanso olimba pa chikhulupiliro chawo potengera momwe nkhoswe ya mphakati...

View Article

Bambo Simon Nyalugwe Alowa M’manda

Mwambo woyika m’manda thupi la malemu bambo Simon Nyalugwe omwe amatumikira ku dayosizi ya mpingo wakatolika ya Zomba wachitika lolemba pa 22 August 2016ku Zomba Cathedral mu dayosizi ya Zomba. Malinga...

View Article


Mpingo Wakatolika Mdziko Muno ati Udzapindula ndi Msokhano wa WUCWO

Mpingo wakatolika mdziko muno akuti udzapindula kwambiri ndi msonkhano wa bungwe la amayi achikatolika pa dziko lonse waWorld Union of Catholic Women Organisation(WUCWO)umene awukonza kuti uchitikire...

View Article

Alimbikitsa Anthu Kuganizira za Chitukuko cha Dziko Lino

Wachiwiri kwa m’tsogoleri wa dziko lino Dr Saulos Chilima wati nkofunika kuti anthu m’dziko muno ayambe kuganiza mwakuya ndi kupeza njira zabwino zomwe zingathandize pa ntchito zotukula dziko lino....

View Article


Apempha Ansembe Kudzipereka pa Utumiki Wawo

Ansembe mu dayosizi ya Mangochi awapempha kuti akhale odzipereka pa utumuki wawo komanso adzisamalira katundu osiyanasiyana yemwe amagwiritsa ntchito. Polankhula pambuyo pa msulo wa ansembe omwe...

View Article

Migwirizano Ina Ikhumudwitsa Papa

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco wati ndi wokhumudwa ndi migwirizano yomwe imakhalapo pakati pa maiko omwe ndi amphamvu komanso otukuka pa chuma. Papa Francisco wati...

View Article

Ntchito Yolimbana ndi Mbozi ati Ikuyenda Bwino

Boma lati ntchito yolimbikitsa kuthana ndi mbozi zachilendo zofanana ndi ntchembele zandonda zomwe zagwa mdziko muno ikuyenda bwino. Dr. Godfrey Ching’oma omwe ndi mlangizi wamkulu woona za mbewu mu...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>