Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Nyumba zofalitsa nkhani mdziko muno azipempha kuti zizilemba zoona zokhudza...

Nyumba zofalitsa nkhani m`dziko muno azipempha kuti zizilemba nkhani zoona zokhazokha zokhudza matenda a EDZI. Mkulu wogwilizira udindo woona za mapologalamu ku bungwe la National Aids Commission (NAC)...

View Article


Mpingo wakatolika mdziko la South Sudan udzudzula za mchitidwe wakupha

Mpingo wakatolika mdziko la South Sudan wadzudzula achiwembu omwe apha meya wa mzinda wa Yei womwenso ndi likulu la dayosizi ya mpingowu mdzikolo. Mai Cecelia Tito anasankhidwa kukhala meya wa mzindawo...

View Article


Akuluakulu a Bungwe la Utumiki wa Apapa Ayamikira Akhristu a Mpingo...

Akuluakulu a bungwe la utumiki wa apapa la Pontifical Missionary Societies PMS mmaiko a Britain ndi Ireland ayamikira akhristu a mpingo wakatolika mdziko muno kamba ka chidwi chawo pankhani...

View Article

Mutharika Awonetsetsa kuti Ndalama ya Kwacha Isapitilire Kugwa

Pulezident wa dziko lino Professor Arthur Peter Mutharika wati boma lake lichita chotheka  powonetsetsa kuti mphamvu ya ndalama ya kwacha isapitilire kugwa. Mtsogoleriyu amalankhula izi lachitatu pa...

View Article

Asilikali Achita Ziwonetsero Mdziko la Ivory Coast

Nduna ya zachitetezo mdziko la Ivory Coast a Paul Koffi Koffi alamula asilikali mdzikolo kuti abwelere mmalo awo ogwilira ntchito kamba koti  achitapo kanthu pa zomwe asilikaliwo akudandaula....

View Article


Dotolo Amwalira Atadwala Matenda a Ebola

Dotolo wina wa mpingo wakatolika amene wakhala akudzipeleka kwambiri pothandiza anthu odwala matenda a Ebola mdziko la Siera Lione akuti wamwalira atapezeka ndi matendawa. Dotoloyo Martin Saliya yemwe...

View Article

Kusamvana Kwakula Pakati pa Dziko la Israel ndi Palestine

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika padziko lonse Papa Francisco wapempha atsogoleri a mayiko a Israel ndi Palestine kuti athetse kusamvana komwe kwakhala kukuchitika pakati pa mayiko awiriwa. Kusamvana...

View Article

Beam Trust Yakonzeka Kulimbikitsa Amayi pa Chuma

Bungwe la Beautify Malawi (BEAM) TRUST lati posachedwapa liyamba kulimbikitsa amayi komanso asungwana kukhala odzidalira pachuma pamwamba pa ntchito zake zowonetsetsa kuti mdziko muno muli ukhondo....

View Article


UKALISTIYA

UKALISTIYA BY ST ANDREWS CATH. CHOIR MUA PARISH DIOCESE OF DEDZA

View Article


NDANI ANKADZIAWA

NDANI ANKADZIWA BY LISANJALA PARISH

View Article

LERO NDAKONDWA BY LIMBE CATHEDRAL

LERO NDAKONDWA BY LIMBE CATHEDRAL

View Article

St Patricks Mangochi Cathedral Itenga Chikho cha Radio Maria Malawi Choir...

Kwaya ya St Patricks yochokera ku Mangochi Cathedral mu dayosizi ya Mangochi, ndi yomwe yatenga chikho cha chaka chino cha chikondwerero cha mayimbidwe cha Radio Maria Malawi Choir Festival 2014....

View Article

Bungwe la CADECOM Lilimbikitsa Alimi Kukhala Odzidalira

Bungwe lowona za chitukuko mumpingo wa katolika la Catholic Development Commission in Malawi (CADECOM)  m`boma la  Dedza lakhazikitsa ntchito ya zaka zitatu yotchedwa Zuze Intergrated Food Security...

View Article


Chipani cha Patriotic Front Chayimika Pulezidenti Scott Kukhala Membala wa...

Chipani cholamula mdziko la Zambia  cha Patriotic Front  chayimika Pulezidenti wadzikolo  Guy Scott kukhala membala wachipanicho kwa miyezi iwiri. Chipanicho chayimika Pulezidenti Scott yemwe...

View Article

Monsinyo Tamani Ayamikira Akhristu a ku St Cecilia Sigerege

Akhristu a ku St Cecilia ku St James Catholic Parish ku Chilomoni a mpingo wakatolika mu Akidayosizi ya Blantyre awayamikira kamba kochitapo kathu pomanga tchalitchi lawo modzidalira. A Vicar General...

View Article


Mafumu Apemphedwa Kuchitapo Kanthu pa Ngozi Zogwa Mwadzidzidzi

Bungwe la zachitukuko mu mpingo wakatolika la Cadecom mu Dayosizi ya Chikwawa lapempha mafumu onse opezeka mu dayosiziyo kuti  achite zomwe angathe kuti ateteze anthu awo ku ngozi zogwa mwadzidzi zomwe...

View Article

Mnyamata Wina Aphedwa ndi Mfuti Yosema

Bambo wina wa zaka 61 zakubadwa ali m’manja mwa apolisi m’boma la Neno kamba komuganizira kuti wapha m’bale wake pomuwombera ndi mfuti yochita kusema. Ofalitsa nkhani za apolisi m’bomalo a Raphael...

View Article


Achinyamata Apemphedwa Kukhala Odzisunga

Dayosizi ya Mangochi ya mpingo wakatolika yapempha achinyamata mudayosiziyo kuti adzisunge pofuna kuti adzathe kukwaniritsa utumiki wawo mtsogolo. Mlembi wamkulu wowona za chiyitanidwe mu dayosiziyi...

View Article

Nthumwi za Bungwe la Utumiki wa Apapa Ziyamikira Mpingo wa Katolika ku Malawi

Nthumwi zoyimilira mabungwe a utumiki wa a papa la Pontifical Missionary Soceties (PMS) zochokera m’mayiko a Ireland ndi England zati zakhutira ndi momwe mpingo wakatolika mu Diocese ya Zomba...

View Article

Malawi Angatukuke ndi Miyala ya Mtengo Wapatali

Boma lati lili ndi chikhulupiriro chakuti mdziko muno muli miyala yambiri ya mtengo wapatali yomwe ingathe kugwiritsidwa ntchito potukulira chuma cha dziko lino. Wachiwiri kwa mkulu wowona...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live