Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

ANTHU AWIRI AMWALIRA PA NGOZI KU NENO

Anthu awiri amwalira lolemba pa ngozi ziwiri zogundidwa ndi galimoto mboma la Neno. Malinga ndi mneneri wa apolisi mbomalo a Raphael Kaliati, ngozi yoyamba inachitikira pa msika wa Kanono koma  bambo...

View Article


BAMBO MATTIAS CHIWANDA AMWALIRA

M’modzi mwa amsembe ampingo wakatolika mu dayosizi ya Chikwawa bambo Mattias George Chiwanda amwalira lachiwiri madzulo atadwala kwa nthawi yochepa. Malinga ndi akulikulu la mpingo wakatolika kuno ku...

View Article


MONSINYO VAN MEGEN NDI NDUNA YATSOPANO YA PAPA KU SUDAN

Mtsogoleri wampingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco wasankha yemwe anali oyimilira Papa kuno ku Malawi  Mosinyo Hubertus Matheus Maria van Megen kukhala nduna yatsopano ya Papa mdziko la...

View Article

MPINGO WAKATOLIKA WATI OYAMBITSA ZIWAWA ALANDIRE CHILANGO

Bungwe la Catholic Commission for Justice and Peace [CCJP] lomwe ndi nthambi ya bungwe la ma episkopi ampingo wakatolika kuno ku Malawi lapempha bungwe loona za chisankho la Malawi Electoral Commission...

View Article

ULALIKI

Ine nkulu uyu ndatopa naye by James Kastome

View Article


Adampachika pa mtandapo

Adampachika pa mtandapo by st marys catholic choir kamuzu barracks

View Article

Mdima unadetsa dziko

Mdima unadetsa dziko by St Stephen Bwanje Parish Dedza Diocese

View Article

Kodi tidikira

View Article


BAMBO CHIWANDA ALOWA M’MANDA

Ma episkopi atatu ampingo wakatolika kuno ku Malawi lachinayi pa 20 march anatsogolera anthu zikwizikwi pa mwambo woyika m’manda thupi la bambo Matthias Chiwanda amu dayosizi ya Chikwawa omwe...

View Article


ULALIKI

Sitima imaphweka akamayendetsa wina by Kalongonda 

View Article

ANTHU ATATU AMWALIRA PA NGOZI KU MZUZU

Anthu atatu kuphatikizapo msungwana wa zaka khumi ndi zitatu amwalira atawombedwa ndi galimoto pa mtsinje wa Lunyangwa mumsewu wa Mzuzu-Karonga loweruka. Malinga ndi mneneri wa apolisi mumzinda wa...

View Article

AKHRISTU 23 APITA KU MALO OYERA KU ROME MWEZI WA MAWA

Akulu akulu omwe akuyendetsa zokonzekela za ulendo wa akhristu a ku Malawi opita kumalo oyera ku Rome mdziko la Italy pa 16 April chaka chino ati zokonzekera za ulendowo zili mkati ndipo zikuyenda...

View Article

PULEZIDENTI BANDA WATI A MUTHARIKA ANAYAMBITSA ZIWAWA KU THYOLO

Pulezidenti Dr Joyce Banda wati ziwawa zomwe zinachitika kwa Goliati mboma la Thyolo sabata yatha zomwe zinazetsa imfa ya wapolisi ndi munthu wamba m’modzi zinakonzedwa ndi pulezidenti wachipani cha...

View Article


ULALIKI

kodi izo izozo zililiko? by Kalongonda

View Article

A MALAWI ALEMBA NAWO BAIBULO LA CHICHEWA PA MANJA

A Malawi akhala ndi mwayi olemba nawo Baibulo la Chichewa pa manja lomwe likasiyidwe ku malo omwe amasungirako ma Baibulo mdziko la Israel. Malinga ndi mkulu yemwe akuyendetsa ntchitoyi mdziko muno...

View Article


PULEZIDENTI BANDA WAKHUTIRA NDI MMENE MALONDA A FODYA AYAMBIRA

Pulezidenti Dr Joyce Banda wati ndi okondwa ndi mitengo yomwe alimi anagulitsira fodya wawo lolemba pamene amatsekulira msika wambewuyi chaka chino ponena kuti akukhulupirira kuti chaka cha 2014...

View Article

MABUNGWE AKWIYA NDI KUYIMITSIDWA KWA NTCHITO YOWUNIKA MAYINA MKAWUNDULA

Anthu komanso mabungwe omwe sia boma ati sakugwirizana ndi zomwe bungwe la za chisankho la MEC lachita poyimitsa ntchito ya mugawo loyamba lowunika mayina mukawundula wa voti yomwe inayamba lolemba...

View Article


A PAYONIYA AKUFUNA CHILUNGAMO KUCHOKERA KU BOMA

Mamembala a gulu lakale la boma la Malawi Young Pioneers [MYP] lachiwiri anakatula chikalata kwa pulezidenti Joyce Banda kudzera ku ofesi ya bwanamkubwa wa mboma la Lilongwe chopempha kuti alowererepo...

View Article

MA BISHOPU AMPINGO WA ANGLICAN APEMPHA KAMPENI YA BATA

Pomwe mabungwe ndi zipembezo zikupitiriza kudzudzula mchitidwe wa ziwawa womwe unaphetsa wapolisi ndi munthu wamba m’modzi kwa Goliati mboma la Thyolo mpingo wa Anglican wapempha boma kuti lionetsetse...

View Article

DAYOSIZI YA MANGOCHI IKUZINDIKIRITSA ACHINYAMATA ZOPEWA ZIWAWA

Pamene kwangotsala sabata zowerengeka kuti anthu adzaponye voti pa chisankho cha patatu pa 20 May, Dayosizi ya Mangochi yampingo wakatolika yati ikudzipereka powonetsetsa kuti chisankhochi...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>