Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Khansa ya Khomo la Chiberekero, Chiwopsezo Cha Miyoyo ya Amayi

Nthenda ya khansa ya mchiberekero akuti ndi imodzi mwa matenda omwe akupitilira kutenga miyoyo ya amayi kamba koti amayi ambiri samapita kukayezetsa kuti adziwe ngati ali ndi matendawa kapena ayi....

View Article


Mzimayi Afa ndi Nthaka Yogumuka

Mayi wa zaka 62 wamwalira ndipo ena awiri awagoneka pachipatala cha Dowa atavulala kwambiri nthaka itawagumukira m’boma la Dowa. Mneneri wa   apolisi m’bomalo Sergent Richard Kaponda watsimikiza za...

View Article


Dziko la Zimbabwe lati Libweza Malo omwe Lidalanda kwa Azungu

Dziko la Zimbabwe lati libweza  malo omwe lidalanda azungu zaka khumi ndi zisanu zapitazo pofuna kubwezeretsa phindu lomwe dzikolo limapeza paulimi omwe azungu amachita mmalowo. Malipoti a News24 ati...

View Article

Pulezidenti Museveni Adzetsa Mtendere Mdziko la Burundi

Mtsogoleri wa dziko la Uganda Yoweri Museveni wayamba zokambirana zofuna  kudzetsa mtendere pakati pa boma ndi magulu otsutsa mdziko la Burundi pomwe magulu otsutsawo sakugwirizana ndi mfundo yoti...

View Article

Papa Benedicto Abwelera ku Vatican

Mtsogoleri wopuma wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Benedicto wa 16 wabwelera ku likulu la mpingowu ku Vatican atakhala sabata ziwiri ku nyumba ya a Papa ya Castel Gandolfo mdziko la Italy....

View Article


Vuto la Madzi Lakula Mdera la Mchesi

Anthu okhala ku Mchesi m’boma la Lilongwe apempha boma kuti liyambe msanga kupereka madzi awukhondo pogwiritsa ntchito mipopi yomwe idamangidwa kale mderalo. Malinga ndi m’modzi mwa anthu okhudzidwa...

View Article

Atsogoleri Mmadera Akhale Patsogolo Pokhwimitsa Chitetezo

Apolisi m’boma la Balaka apempha atsogoleri a mmagulu osiyanasiyana kuti atengepo gawo lalikulu pantchito yokhwimitsa chitetezo m’bomalo. Mkulu owona ntchito za apolisi akumidzi m’bomalo Sub-Ispector...

View Article

Papa Francisco wati Ntchito za Migodi Zikomere Anthu Okhala Moyandikana ndi...

Mtsogoleri wampingo wakatolika padziko lonse Papa Francisco,wapempha mayiko kuti adziwonetsetsa kuti ntchito za migodi zomwe zikuchitika mmayiko awo zikuchitika mokomera anthu  onse maka oyandikana ndi...

View Article


Atsogoleri a Zipani Zotsutsa Sapikisana Nawo pa Chisankho cha Pulezidenti...

Pamene chisankho cha pulezidenti mdziko la Burundi chikuyembekezeka kuchitika lachiwiri, mtsogoleri wa dzikolo Pierre Nkurunziza ati akuyembekezeka kupambana pa chisankhochi zomwe zichititse kuti...

View Article


Mutharika Wati Boma Lake Silatsankho

Mtsogoleri wadziko lino Professor Arthur Peter Mutharika  wati sizowona zomwe anthu ena akumanena zoti  boma lake limapanga tsankho posankha anthu m'maudindo. Mutharika amayankhula izi lamulungu...

View Article

Mayi Banda ndi Okhudzidwa ndi Imfa ya a Nyondo

Pamene atsogoleri osiyanasiyana pandale akupitiliza kusonyeza kukhudzidwa kwawo ndi imfa ya mtsogoleri  wachipani cha National Salvation Front NASAF a James Nyondo, mtsogoleri wakale wa dziko lino mayi...

View Article

Anthu 15 Afa ndipo 10 Avulala Atawomberedwa

Anthu khumi ndi asanu aphedwa ndinso ena khumi avulala atawomberedwa ndi anthu ena omwe anakwera ngamila mdziko la Sudan. Mmodzi mwa anthu omwe avulala pachiwembucho wawuza atolankhani kuchipatala...

View Article

Nthambi za Chitetezo Zidzudzula za Imfa ya Msilikali

Nthambi za chitetezo mdziko muno za Polisi ndi Army zadzudzula imfa ya msilikali wa Army yemwe anaphedwa ndi apolisi loweruka pa 22 November nthawi ya 11 koloko usiku mumzinda wa Zomba. Akuluakulu...

View Article


Papa Frascisco Asayina Mgwirizano Woteteza Chilengedwe ndi Kuthetsa Mchitidwe...

M’tsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francis wasayinirana mgwirizano ndi akuluakulu a m’mizinda ochokera mmaiko osiyanasiyana wofuna kuteteza chilengedwe komanso kuthetsa mchitidwe...

View Article

Banki Yaikulu pa Dziko lonse Ithandiza Dziko la Nigeria

Banki yaikulu pa dziko lonse ya  World Bank,  yalonjeza kuti ipereka ngongole ya  ndalama zokwana 2.1 biliyoni za America zothandiza kukonzera madera ena omwe gulu la zauchifwamba la Boko Haram...

View Article


Anthu 40 Afa pa Nyanja ya Mediterranean

Anthu pafupifupi makumi anayi amila mu nyanja ya Mediterranean mdera lina lomwe lili kufupi ndi dziko la Libya bwato lomwe anakwera litamila. Panthawiyi anthuwo ati anali paulendo opita mmayiko...

View Article

Dayosizi ya Mangochi Ichita Chikondwelero cha Nkhoswe Yake

Ntchito yokonzekera mwambo wokondwelera nkhoswe ya Dayosizi ya Mangochi yomwe ndi Augustino woyera ikupitilira. Polankhula ndi Radio Maria Malawi mkulu woona zautumiki mu dayosiziyi Bambo Raphael Nkuzi...

View Article


Pulezidenti Obama Ayendera Dziko la Kwawo

Mtsogoleri wadziko la America Barrack Obama wafika  mdziko la Kenya paulendo wake ocheza mdzikolo, pomwenso akuyembekezeka kukambirana ndi atsogoleri a dzikolo pa nkhani zosiyanasiyana. Paulendowu...

View Article

A ku Banja Adzudzula Madonna Polephera Kusunga Lonjezo

Katswiri woyimba nyimbo za chamba cha POP wa mdziko la America Madonna, amudzudzula kamba kolephera kusunga lonjezo lomwe anapereka kwa makolo a mwana yemwe anamutenga mdziko muno kuti akamulere mdziko...

View Article

Buhari Akumana ndi Pulezidenti wa Dziko la Cameroon

Mtsogoleri wa dziko la Nigeria Muhammadu Buhari lachitatu akuyembekezeka kukakumana ndi mtsogoleri wa dziko la Cameroon a Paul Biya kuti akakambirane mfundo zofuna kuthetsa gulu la zauchifwamba la Boko...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>