Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

TIGWILANE MANJA POTHETSA UMBAVA-MASAUKO MEDI

  Apolisi owona za chitetezo ku likulu la apolisi mu mzinda wa Lilongwe ati ayesetsa kugwira ntchito  modzipereka ndi anthu a m’midzi pofuna kuthetsa m’chitidwe wa umbava ndi umbanda. Mkulu wa apolisi...

View Article


AMBUYE STE MARIE APEMPHA AKHRISTU KUTI AZAMITSE CHIKHULUPILIRO

  Arkiepiskopi wa Arkidayosizi ya Lilongwe ya Mpingo wa Katolika Ambuye Remi Ste Marie  apempha akhristu a Mpingowu mu arkidayosiziyo kuti alimbitse chikhulupiliro chawo pomwenso akhristu a Mpingowu pa...

View Article


BUNGWE LA MEC LAYIMITSA GANIZO LOGWILITSA NTCHITO MAKINA ATSOPANO PA CHISANKHO

  Bungwe loyendetsa zisankho m’dziko muno la Malawi Electoral Commission (MEC) lati layimitsa ganizo lake lofuna kugwiritsa ntchito makina atsopano pa kalembera wa voti pokonzekera chisankho cha...

View Article

WAYILESI ZA MARIA ZIKUFUNA KUTHANDIZA KUTI MAWAYILESI ENA AKHAZIKITSIDWENSO...

  Wailesi za Maria  zomwe zidakhazikitsidwa kale pa dziko la pansi zakonza dongosolo lofuna kuthandiza  kukhazikitsa  wayilesi zina  m’mayiko momwe akufuna kukhalanso  ndi wayilesi za amayi  Maria pa...

View Article

PAPA FRANCIS ACHEZA NDI MTSOGOLERI WOPUMA PAPA BENEDIKITO WA 16

Mtsogoleri wa Mpingo wa Katolika padziko lonse Papa Francis  anakayendera ndikudya nkhomaliro ndi mtsogoleri  opuma wa Mpingowu  Papa Benedikito wa 16 loweruka pa 23 March 2013. Papa Francis...

View Article


"IKANI MAPEMPHERO PATSOGOLO MU NYENGO YA PA PASAKA"-PRESIDENT JOYCE BANDA

  Mtsogoleri wa dziko lino Dr Joyce Banda wapempha akhristu kuti akondwelere kuwuka kwa Yesu khristu poika mapemphero patsogolo mu chikondwelero cha Pasaka. President Joyce Banda walangizanso anthu...

View Article

BAMBO STEVEN SAULOSI MKATA ALOWA M'MANDA PA 2 APRIL 2013

  Bambo Steven Saulosi Mkata omwe amwalira pa 30 March 2013 akuyembekezeka kuikidwa m’manda mwa ulemu lachiwiri likudzali  pa 2 April 2013. Monsignor Mkata adamwalira  ku pachipatala cha St Joseph ku...

View Article

NDUNA IYAMIKIRA MGWIRIZANO PAKATI PA MIPINGO YA MU MZINDA WA MZUZU

  Nduna ya za malimidwe ndi kuonetsetsa kuti m'dziko muno muli chakudya chokwanira Wolemekezeka a Peter Mwanza ayamikira mgwilizano wabwino omwe ulipo pakati pa Mipingo yozungulira  mzinda wa Mzuzu. A...

View Article


ZITSEKO MU MPINGO

Ulaliki titled Zitseko  Mu Mpingo by Mai Senia Kaunda

View Article


KUSUNGA CHIKHULUPILIRO

Ulaliki titled Kusunga Chikhulupiliro by Mai Senia Kaunda

View Article

BOMA LIDZIPEREKA MALIPIRO ABWINO KWA OGWIRA NTCHITOZA CHIPATALA-DAVID KANKWAMBA

  Mkulu wa bungwe la atolankhani omwe anapezeka ndi Kachilombo ka HIV komwe kamayambitsa matenda a Edzi la Journalists living with HIV and AIDS a David Kamkwamba apempha boma kuti lithandize pa nkhani...

View Article

APOLISI AGWIRA MWAMUNA OPEZEKA NDI MFUTI POPANDA CHILOLEZO

  A polisi ku Mzuzu agwira ndi kutsekera m'chitolokosi mwamuna wina yemwe amasunga mfuti ziwiri za mtundu wa Green nala m’boma la Karonga .  Mneneri wa a Polisi ku Mzuzu Sergeant Morris Chapola wati...

View Article

CHIPANI CHA AFORD CHAKANA KUGWIRA NTCHITO CHIPANI CHOLAMULA

  Mmodzi wa akuluakulu a chipani cha Alliance For Democracy (AFORD) watsutsa zomwe  wayankhula wapampando wachipanichi  a Enock Chakufwa Chihana kuti chipani cha AFORD  chigwira ntchito ndi cha...

View Article


KODI CHIZINDIKIRO CHANU NCHANI?

Ulaliki titled Kodi Chizindikiro Chanu Nchani? by Mayi Marita Senia Kaunda.

View Article

Mariathon Jingle

View Article


AFITI OPEMPHERA

Ulaliki titled Afiti Opemphera by Father E Nthalika

View Article

Dimu Pamsewu

Ulaliki titled Dimu Pamsewu by Senia Kaunda

View Article


Nkhondo Ili Dzenjemu

Ulaliki titled Nkhondo ili  dzenjemu

View Article

Fanizo La Ana Awiri

Ulaliki titled Fanizo La Ana Awiri

View Article

Za Chuma cha Kumwamba

Ulaliki titled Zachuma Cha Kumwamba by Father James Chizuma

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>