Quantcast
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Ophunzira a YCS Akhale Owonetsa Makhalidwe Abwino-Bambo Mwakhwawa

Ophunzira a mpingo wa katolika msukulu za sekondale mdziko muno awapempha kuti akhale owonetsa makhalidwe abwino. Mkulu wa ku ofesi yoona za utumiki wa apapa ya Pontifical Missionary Societies (PMS) ku...

View Article


Ntchembere Zandonda Zawononga Kwambiri Mbewu mu Machinga ADD

Ofesi yoyang’anira ntchito za ulimi m’maboma a m’chigawo cha ku m’mawa cha dziko lino ya MachingaADDyadandaula kaamba ka zilombo zina zomwe zikuwoneka ngati ntchembere zandonda zomwe ati zakhudza mbewu...

View Article


Anthu Khumi Afa pa Ngozi ya pa Nyanja ya Indian

Anthu khumi afa ndipo ena asanu ndi awiri apulumutsidwa boti lomwe anakwera litagubuduzika pa Nyanja ya Indian mdziko la Sri Lanka. Anthu omwe anali mu botili ati anakachita nawo chikondwelero cha...

View Article

Achinyamata Alimbikitsidwe pa Moyo wa Uzimu-Bambo Kalasi

Achinyamata ati akuyenera kulimbikitsidwa pa umoyo wao wachikhristu kaamba koti amakhala akukumana ndi zinthu zambiri zowabweza mmbuyo pa nkhani ya chikhulupiliro. Mkulu woyang’anira bungwe la...

View Article

Bungwe la FAWO Lati Amayi Amasiye Akhale Odzidalira

Bungwe lomenyela ufulu wa amayi ndi ana amasiye mdziko muno la Foundation for Widows and Orphans (FAWO) lati nthawi yakwana yoti amayi amasiye akhale odziyimira pawokha pa nkhani za chuma. Polankhula...

View Article


Papa Alimbikitsa Ubale wa Mpingo wa Katolika ndi Anglican

M’tsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse papa Francisco waonetsa chitsanzo cha ubale wabwino pakati pa mpingo wakatolika ndi wa Anglican. Papa wachita izi atakayendera akhristu a mpingo wa...

View Article

Bwanamkubwa Ayamikira Sukulu ya Ukachenjede ya DMI

Bwana-mkubwa wa boma la Mangochi a James Manyetera ayamikira sukulu ya ukachenjede ya DMI yomwe imayendetsedwa ndi amsembe a mpingo wakatolika mu chipani cha Missionaries of Mary Immaculate(MMI) kamba...

View Article

Apempha Akhristu Azipemphelera a Sisteri

Ophunzira a mpingo wa katolika msukulu za sekondale mdziko muno awapempha kuti akhale owonetsa makhalidwe abwino. Mkulu wa ku ofesi yoona za utumiki wa apapa ya Pontifical Missionary Societies (PMS) ku...

View Article


Dziko la South Sudan Lalengeza Madera Omwe Akhudzidwa ndi Njala

Dziko la South Sudan lalengeza kuti mmadera ena a mdzikolo anthu akuvutika ndi njala. Malinga ndi boma la dzikolo komanso bungwe lowona za mgwirizano wa maiko a pa dziko lonse la United Nations UNanthu...

View Article


Nyumba Zosindikiza Ndi Kuwulutsa Nkhani Zizilemba Mwaukadaulo Nkhani Zokhudza...

Nyumba zotsindikiza ndi kuwulutsa nkhani mdziko muno azilimbikitsa kuti zizifufuza mokwanira komanso kulemba mwaukadaulo nkhani zokhudza anthu olumala. Wachiwiri kwa mkulu wa nthambi yophunzitsa...

View Article

Bungwe la PACHI Likulimbikitsa Uchembere Wabwino

Bungwe la Parent and Child Health Initiative (PACHI) lapempha amayi kuti azipita ku chipatala msanga akakhala oyembekezera pofuna kuchepetsa  imfa zokudza kaamba ka uchembere. Mkulu woona za ma...

View Article

Anthu Atatu Amangidwa Kamba Koba Katundu ku CADECOM

Apolisi m’boma la Balaka agwira anthu atatu omwe akuwaganizira kuti ndi amene akukhudzidwa ndi mulandu wakuba ku malo a mpingo wakatolika a CADECOM ku Ulongwe ndi ku malo a zaulimi wa nthilira a...

View Article

Mpingo Wakatolika Wati Pasakhale Lamulo Lakupha Munthu Wopha ma Alubino

Mpingo wa katolika mdziko muno wati ukugwirizana ndi ganizo la boma loti pasakhale lamulo lakupha  munthu wopezeka olakwa pa mlandu wosowetsa komanso kupha anthu a mtundu wa chialubino. Mlembi wa mkulu...

View Article


Anthu 70 Afa pa Nyanja ya Atlabtic

Matupi oposera 70 a anthu akufa akuti apezeka akuyandama kudera lina mu nyanya yayikulu ya Atlantic m’dziko la Lybia. Akatswiri pa ntchito zopulumutsa anthu pa ngozi zochitika  pamadzi akuti ndi amene...

View Article

Mpingo Wakatolika Wati Pasakhale Lamulo Lakupha Munthu Wopha ma Alubino

Mpingo wa katolika mdziko muno wati ukugwirizana ndi ganizo la boma loti pasakhale lamulo lakupha  munthu wopezeka olakwa pa mlandu wosowetsa komanso kupha anthu a mtundu wa chialubino. Mlembi wa mkulu...

View Article


YCW Ikutolera Thandizo la Seminale Ya St. Peters

Bungwe la achinyamata mu mpingo wakatolika m’dziko muno la Young Christian Workers (YCW) lati likutolera thandizo pofuna kuthandiza seminale yaikulu ya St. Peters mu dayosizi ya Zomba yomwe padakali...

View Article

PRO-LIFE Yati Kupha ma Alubino ndi Kutsutsana ndi Cholinga cha Mulungu

Bungwe loteteza miyoyo ya anthu la mpingo wa katolika la PRO-LIFE lati kupha anthu a mtundu wa chialubino ndi kutsutsana ndi cholinga cha Mulungu kaamba koti iye analenga munthu aliyense m’chifaniziro...

View Article


Amayi Awiri Akayankha Mlandu Wopha Kim Jong-Nam

Amayi ena awiri akuyembekezeka kukawonekera ku bwalo la milandu mawa ndi kukayankha mlandu wokhudzana ndi kuphedwa kwa mchimwene wake wa mtsogoleri wa dziko la North Korea,Kim Jong-Nam. Malipoti a...

View Article

Ana Ochoka Mdziko la Libya Kupita Italy Ali pa Chiopsezo- UN

Bungwe lowona za mgwirizano wa maiko a pa dziko lonse la United Nations UNlachenjeza  kuti ana ochuluka othawa kwao ochoka mdziko la Libya kupita mdziko la Italy ali pa chiopsezo. Malinga ndi malipoti...

View Article

Ma Episkopi Apempha Mayiko Athandize Anthu a Njala Mdziko la South Sudan

Ma episkopi a mpingo wa katolika mdziko la South Sudan apempha maiko akufuna kwabwino kuti athandize anthu amene akuvutika ndi njala mdzikolo. Malinga ndi chikalata chomwe ma episkopiwa alemba,...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>