Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Monsinyo Tamani Apempha a Malawi Azithandizana pa Nkhani ya Njala

Arkidayosizi ya Blantyre ya mpingo wakatolika yalimbikitsa a Malawi kuti azithandizana okhaokha pamene anthu ena akhudzidwa ndi vuto la njala. Vicar General wa Arkidayosiziyi Monsinyo Boniface Tamani...

View Article


Boma Lipempha Anthu Asamalire Nkhalango ya Dzalanyama

Boma lapempha anthu omwe amakhala malo ozungulira nkhalango ya Dzalanyama mu mzinda wa Lilongwe kuti asunge mitengo ya mu nkhalangoyi ndi cholinga chofuna kuchepetsa vuto la kuvuta kwa madzi mu...

View Article


Anthu 26,000 Athawa Mu Mzinda Wa Mosul

Anthu okwana 26 sauzande a m’dziko la Iraq athawa kum’mvuma kwa mzinda wa Mosul pa masiku okwana khumi 10 potsatira kumenyana komwe kunabuka pakati pa asilikali a dzikolo ndi zigawenga za Islamic State...

View Article

Atumiki a Radio Maria Malawi Awapempha Akhale Olimbikira Pofalitsa Uthenga wa...

Anthu omwe amagwira ntchito modzipereka ku Radio Maria Malawi awalimbikitsa kuti asamabwelere m’mbuyo pomwe akukumana ndi zovuta pa nthawi yomwe akutumikira. Bambo Edwin Lambulira alankhula izi...

View Article

President Hosni Mubarak Wapezeka Wosalakwa

Bwalo lalikulu lamilandu la apilo mdziko la Egypt lapeza osalakwa yemwe anali mtsogoleri wakale wa dzikolo a Hosni Mubarak pa mlandu ozunza ndi kupha anthu mazanamazana pa ziwonetsero zomwe zinachitika...

View Article


Papa Alimbikitsa Kubwezeretsa Chilengedwe

M’tsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco wagwirana manja ndi bungwe la ma Episkopi a mpingo wakatolika m’dziko la Brazilpa ntchito yobwezeretsa chilengedwe. Papa wati mpingo...

View Article

Patron Akondwera ndi Bungwe la YCS mu Arkidayosizi ya Lilongwe

Patron wa bungwe la ophunzira a chikatolika msukulu za sekondale la Young Christian Students (YCS) a Phillip Nsinawana Mwale ayamikira momwe ntchito za bungweli zikuyendera mu arkidayosizi ya Lilongwe....

View Article

Wapolisi Wosowa Wapezeka Atafa Atazimangilira

Wapolisi yemwe anasowa ku Police College mu mzinda wa Zomba wapezeka atafa atadzimangilira ku minda ya ku Chancellor College mu mzindawo. Mkulu wofalitsa nkhani mchigawo cha kummawa cha dziko lino...

View Article


Asilikali Apirikitsa Zigawenga za IS mu Mzinda wa Palmyra Mdziko la Syria

Asilikali a mdziko la Syria mogwirizana ndi a mdziko la Russia alanda ndi kupirikitsa zigawenga za chisilamu za Islamic State IS mu mzinda ya Palmyra mdziko la Syria. Malinga ndi malipoti a wayilesi ya...

View Article


Papa Wapempha Ansembe Akhale a Chiyembekezo, Chikhulupiliro

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco wati ansembe akuyenera kukhala a chiyembekezo chabwino mmoyo wao pokumbukira zimene Mulungu anawalonjeza komanso pokhala a chikhulupiliro....

View Article

Asilikali a Iraq Alanda Mlatho wa Tigris ku Zigawenga za IS

Asilikali a mdziko la Iraq ati alanda mlatho wa ufulu wa mtsinje wa Tigris mu mzinda wa Mosul ku zigawenga za chisilamu za Islamic State IS. Malipoti a wailesi ya BBC ati mlathowu ndi wachiwiri pa...

View Article

MBS Itseka Golden Peacock, Pacific Hotel

BungweMalawi Bureau of Standards (MBS) layamba latseka nyumba zogona alendo za Golden Peacock komanso Pacificmu mzinda wa Lilongwe kaamba koti zikusowa zinthu zina zolimbikitsira ntchito za ukhondo....

View Article

Jonathan Watsutsa Kuti Analetsa Boma la America Kugwira Ntchito ndi Boma Lake

Mtsogoleri wakale wa dziko la Nigeria Goodluck Jonathan watsutsa malipoti akuti anakana kuti asilikali a mdziko la America athandize pa ntchito yopulumutsa atsikana oposera 200 omwe anagwidwa ndi...

View Article


Asisteri Anayi Afa pa Ngozi mdziko la Ethiopia

Asisiteli anayi afa ndipo ena atatu avulala modetsa nkhawa pa ngozi ya galimoto mdziko la Ethiopia. Malingana ndi malipoti a Catholic News Agency (CNA), a sisiteliwa omwe ndi achipani cha Daughters of...

View Article

Anthu 20,000 a Mdziko la Myanmar Athawira Mdziko la China

Anthu othawa kwawo oposa 20 thousand a mdziko la Myanmar ati alowa mdziko la China pothawa zamtopola zomwe zinabuka kummwera cha kummawa kwa maiko a mchigawo cha Asia. Malinga ndi malipoti padakali...

View Article


Papa wati Munthu Akuyenera Kukumana ndi Zovuta pa Moyo wake

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco wati munthu sangakule popanda kukumana ndi zovuta zosiyanasiyana mu chikhulupiliro chomwe ali nacho mwa Mulungu. Papa amalankhula izi ndi...

View Article

Dziko la Guatemala Litaya Atsikana Makumi Awiri pa Ngozi ya Moto

Dziko la Guatemala lakhazikitsa masiku atatu okhudza maliro a atsikana makumi awiri omwe amwalira kaamba ka moto omwe unabuka pa malo ena osungirapo ana mdzikolo. Malipoti ati atsikana omwe amwalirawa...

View Article


Dziko La Japan Lipereka 112 Sauzande Dollars Zomangira Sukulu M’boma La...

Boma la dziko la Japan lapereka ndalama zokwana 112 thousand 984 za America ku boma la dziko lino zothandizira kumangira sukulu ya sekondale yoyendera ya Chikangulu m’boma la Chiradzulu. Polandira...

View Article

Apempha Amayi Azitanganidwa Kukweza Dziko, Miyoyo Yawo

Amayi ochokera m’mipingo yosiyanasiyana m’dziko muno awapempha kuti azikonda kutanganidwa ndi zinthu zomwe zingathandize pa chitukuko cha miyoyo yawo ndi dziko lino. Mayi Trizer Masauli omwe...

View Article

PMS Yapempha Asemino Akhale Patsogolo mu Utumiki wa Apapa

Bungwe la utumiki wa a Papa mdziko muno la Pontifical Mission Socities PMS lati asemino akuyenera kukhala patsogolo kudziwa zomwe bungwe la utumiki wa apapa limachita. Mkulu wa bungweli mdziko muno...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live