Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Radio Maria Iyamikira Akhristu a ku Mangochi Cathedral

Akhristu a mu Parish ya St.Augustine Mangochi Cathedral mu dayosizi ya Mangochi awayamikira chifukwa  chothandiza Radio Maria Malawi. Mkulu woona za chithandizo ku wailesiyi Mayi Veronica Manyozo ndi...

View Article


Mpingo wa Katolika Mdziko la Iraq Wapempha Akhristu Kusala Zakudya

Mpingo wa katolika mdziko la Iraq wapempha anthu mdzikolo kuti asale zakudya lisanafike tsiku la khirisimasi, pofuna kupempha chifundo cha Mulungu pakati pa akhristu omwe athawa kuzunzidwa mdzikolo...

View Article


APROFET

LUNZU PARISH CHOIR

View Article

AMBUYE AKUBWERA

DON BOSCO CHOIR 2 LILONGWE ARCHDIOCESE

View Article

NAYE YESU AKUBWERA

ST LUKRS CATH. CHOIR MUA PARISH DEDZA DIOCESE

View Article


YESU AKUBWERA

ST BERNADETA WOMEN CHOIR CHIKWAWA DIOCESE

View Article

YESU ADZBWERA

YESU ADZABWERA BY ST MARYS WOMEN CHOIR BANGWE PARISH ARCHDIOCESE YA BLANTYRE

View Article

AMBUYE AKUBWERA

AMBUYE AKUBWERA BY DON BOSCO CHOIR 2 ARCHDIOCESE YA LILONGWE

View Article


Papa Francisco Wapempha Anthu kuti Awonjezere Mapemphero Awo.

Mtsogoleri wampingo wakatolika padziko lonse Papa Francisco,wapempha anthu kuti apemphelere anthu omwe akhudzidwa ndi ziwembu zomwe zachitika mmaiko a Australia ndi Pakistan ,zomwe zaphetsa anthu...

View Article


Ansembe a Chibadwiri mu Diocese ya Mangochi Achita Mbindikiro.

M’bindikiro wa sabata imodzi wa ansembe a chibadwiri mudayosizi ya Mangochi utha mawa. M’bindikirowu unayamba lolemba sabata ino ndipo ukuchitika pofuna  kukonzekera kubadwa kwa Yesu Khristu, kuti nawo...

View Article

AMATIPATSA ZABWINO

AMATIPATSA ZABWINO BY ST BERNADETTA CHOIR BANGWE PARISH BLANTYRE ARCHDIOCESE

View Article

CHARO CHINO

CHARO CHINO BY ST BERNADETTA KANYIKA CHOIR 1 MZUZU DIOCESE

View Article

UKUSEKE VICHI

UKUSEKE VICHI BY ST BERNADETTA KANYIKA CHOIR 1 MZUZU DIOCESE

View Article


Bungwe la Catholic Women Organization(C.W.O.) ku Malawi Lichita Msonkhano...

Msonkhano wawukulu wa bungwe la amayi la Catholic Women Organisation (CWO) wayamba dzulo ku sukulu ya sekondale ya asungwana ya Mary Mount  mu mzinda wa Mzuzu. Msonkhanowu unatsekulilidwa lachinayi ndi...

View Article

Zigawenga Zipha Anthu Oposa Makumi Atatu Mdziko la Nigeria

Anthu oposa makumi atatu aphedwa ndinso ena pafupifupi zana limodzi, abedwa ndi zigawenga  mmudzi wina mdziko la Nigeria. Mmodzi mwa anthu omwe apulumuka pachiwembucho,wawuza wayilesi ya BBC kuti...

View Article


Apempha Anthu Kuthandiza pa Ngongole ya Montfort Press

Arkdayosizi ya Blantyre yapempha anthu akufuna kwabwino kuti athandize arkdayosiziyi pobweza ngongole yomwe kampani yake yotsindikiza mabuku ya Montfort Press ili nayo. Arkidayosiziyi yapereka pempholi...

View Article

Anthu 15 Mwa Anthu 100 Akusiyira Panjira Mankwala a ARV Mdziko muno.

Nthambi yowona za matenda a Edzi mu unduna wa za umoyo yati anthu  khumi ndi asanu 15 mwa anthu 100 aliwonse mdziko muno akumasiyira panjira kumwa mankhwala otalikitsa moyo a ARV pa zifukwa...

View Article


Bungwe la CILIC Liyendera Odwala ndi Amndende.

Bungwe la Civil Liberties Committee (CILIC),lapempha anthu akufuna kwabwino kuti adzipereke pothandiza anthu osowa panthawi ino ya chikondwerero cha Khirisimasi ndi chaka chatsopano. Mkulu woyendetsa...

View Article

Mfumu Mlumbe Iyamikira Diocese ya Zomba.

Diocese ya Zomba ayiyamikira chifukwa chotenga gawo lalikulu lothandiza kupititsa patsogolo ntchito zokweza umoyo wa ana mu Diocese-yo. Mfumu yayikulu Mlumbe ya m’boma la Zomba ndi imene yanena izi...

View Article

Radio Maria Malawi Ichita Chotheka Kukonza Mavuto omwe Ikukumana Nawo

Wachiwiri kwa mkulu wowona za ma programme ku Radio Maria Malawi Bambo Charles Kaponya, wati wailesiyi ichita chotheka kukonza mavuto omwe ma studio ang’onoang’ono a wailesiyi akukumana nawo mdziko...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>