Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Ark diocese Ya Blantyre Ilonjeza Kupitiriza Kuthandiza Radio Maria Malawi

Ark diocese ya Blantyre yati ipitiriza kuthandiza  ntchito za Radio Maria Malawi, pofuna kuti  ntchito zake zofalitsa Uthenga wa bwino zipitilire kupita patsogolo. Mkulu wowona za utumiki mu...

View Article


Kuyipa Sikupindulitsa

View Article


sizodabwitsa zonse zimene ndi zochokera kwa Mulungu

View Article

Kudzidalira kwa Amayi pa Chuma Kungachepetse Nkhaza zomwe Amakumana Nazo

Kudzidalira kwa amayi pa chuma akuti kungathandize kuthetsa nkhanza zochitika pakati pa amayi ndi ana m'dziko muno.  Mkulu oyendetsa ntchito za bungwe la Centre for Altenatives for Victimised Women...

View Article

Bungwe la Amayi Litsindika Kufunika kwa Misonkhano ya Amayi

Amayi a mu Parish ya Kausi mu diocese ya Mangochi atsindika kufunika kwa misonkhano ya amayi yomwe ikuchitika mu dioceseyo kamba koti ikuwathandiza kukhala olimbika ndi odzipereka pa chikhristu chawo....

View Article


Archdayosizi ya Blantyre Ichita Ubale ndi Dayosizi ya Mdziko la Mozambique

Archdayosizi ya Blantyre yayamikira ubale wabwino womwe ulipo pakati pa dayosiziyi ndi dayosizi ya Lichinga mdziko la Mozambique. Arch Episkopi wa archdayosiziyo Ambuye Thomas Luke Msusa ndi omwe...

View Article

A Malawi Apempherere Mvula

Mtsogoleri wadziko lino professor Arthur Peter Mutharika,wapempha a Malawi kuti apemphere kuti mvula iyambe kugwa. Pulezidenti Mutharika wanena izi kudzera mchikalata chomwe nthambi yofalitsa nkhani...

View Article

Boma Latsutsa za Kusalabadira kwa a Mutharika ku Mavuto a Dziko Lino

Boma lati sizowona kuti mtsogoleri wa dziko lino Professor Arthur Peter Mutharika sakulabadira za mavuto omwe anthu mdziko muno akukumana nawo omwe adza chifukwa cha mavuto a zachuma.   Boma lanena izi...

View Article


Dayosizi ya Chikwawa Yayamikira Ntchito za Mabungwe Mpingo Wakatolika

Dayosizi ya Chikwawa yayamikira ntchito zomwe mabungwe a mu mpingo wa katolika akhala akugwira mchaka chomwe chikuthachi. Mlembi wamkulu mu dayosiziyo Bambo Patrick Jambo,ndi omwe ayamikira mabungwewa...

View Article


Ana Awiri a Banja Limodzi Afa ndipo Ena Awiri Avulala Khoma la Nyumba...

Ana awiri a banja limodzi afa ndipo ena awiri avulala khoma la nyumba yomwe anagona litagumuka ndikuwapsinja ku Machinjiri mu mzinda wa Blantyre. Anawo, Agness ndi Pemphero Chaona omwe amakhala ku...

View Article

Mu Mpingo Wakatolika Mulibe Kugawikana, Watero Papa Francisco

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco wati kusiyana maganizo kwa ma episikopi pa nkhani zokhudza banja,sizikutanthauza kuti  mu mpingowu muli kugawikana. Papa Francisco...

View Article

Maphunziro Angachepetse Nkhanza Pakati pa Amayi ndi Atsikana

Kulimbikitsa maphunziro a atsikana ndi njira yabwino yomwe ingathandize dziko lino pothana ndi m’chitidwe wa nkhanza pakati pa amayi ndi atsikana. M’modzi mwa aphungu omwe ali ndi luso la mayimbidwe ku...

View Article

Ana Awiri Afa Atamira pa Dziwe la Madzi

Ana awiri a banja limodzi m’boma la Dowa afa atamira padziwe la madzi m’bomalo. Ofalitsa nkhani za apolisi mbomalo  Sergent Richard  Kaponda watsimikiza za nkhaniyi ndipo wati anawo anamwalira...

View Article


Ma episkopi Mdziko la America Adzudzula Apolisi

Maepisikopi a mdziko la America adzudzula apolisi ku mchitidwe omawopseza anthu oganiziridwa milandu omwe akuti wakula  kwambiri  mdzikolo. Ma episikopiwa adzudzula apolisiwo zitamveka kuti iwo...

View Article

Makolo M’boma la Nsanje Apitiriza Kutsatira Myambo ina Yoyipa.

Makolo ena ku nsanje  akupitirizabe kuchita miyambo ina yoipa monga kukwatiwitsa ana akadali achichepere  komanso kuwagwiritsa ntchito zokhwima zomwe ati zikumakolezera ana ambiri kusiya sukulu. Mkulu...

View Article


Hostel ya Atsikana Imangidwa pa Secondary ya Liwonde M’boma la Machinga.

Kumangidwa kwa hostel ya atsikana pa sukulu ya Secondary ya Liwonde m’boma la Machinga kuthandiza kuti atsikana ambiri ayambe kuchita bwino pa maphunziro awo. Mphunzitsi wa mkulu pa sukuluyi a Welson...

View Article

Kusowa kwa Mauthenga pa Nkhani za HIV ndi AIDS Kukulimbikitsa Kufala kwa...

Mafumu m'boma la Mwanza apempha boma ndi mabungwe kuti alimbikitse ntchito yolimbana ndi kufala kwa ka chilombo ka HIV komwe kamayambitsa matenda a Edzi. Mfumu yaikulu Kanduku ya m'bomalo ndiyomwe...

View Article


Kupempherera Atumiki Ampingo ndi Udindo wa Akhirisitu

Akhristu ampingo wa katolika ati ali ndi udindo opepherela atumiki a mumpingowu kuti asataye utumuki wawo.  Episcope wa arkdiyosizi ya Blantyre Ambuye Luke Msusa ndiwo anena  izi  pamwambo wa malumbiro...

View Article

Apempha Thandizo La Ana Osamva Komanso Osalankhula

Sukulu ya ana osamva ndi kulankhula ya Chisombezi m’boma la Chiladzulu yapempha anthu m’dziko muno kuti  azikonda kulimbikitsa ntchito zopeleka thandizo kwa anthu olumala ndikuti nawo azitha kukhala...

View Article

Bungwe la CRECCOM Liyamikira Mafumu Mboma a Mangochi

Bungwe la CRECCOM layamikira gawo lomwe mafumu akutenga m’boma la Mangochi polimbikitsa maphunziro a asungwana. Mkulu wa bungweli mayi Ziwone Mussa ndi yemwe wanena izi pamwambo opereka mphatso kwa...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>