Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Amayi a Mpingo wa Katolika Apemphedwa Kukwaniritsa Zomwe Akambirana Kumsonkhano

Episkopi wa dayosizi ya Mangochi Ambuye Montfort Sitima,wapempha mamembala a bungwe la amayi mu mpingowu kuti akwaniritse mfundo zomwe amanga kumsonkhano wawo waukulu, womwe watha lamulungu ku sukulu...

View Article


Mafumu a M’boma la Ntcheu Ayamikira Bungwe la CCJP

Mafumu m’boma la Ntcheu ayamikira ntchito yokhudza Chilungamo Choyambilira yomwe nthambi yowona za Chilungamo ndi Mtendere mu mpingo wakatolika mu arkidayosizi ya Lilongwe, imagwira m’bomalo ndi...

View Article


Anthu 26 Afa ndi Mabomba M’dziko la Nigeria

Anthu 26 afa mabomba ataphulika mchigawo cha kumpoto kwa dziko la Nigeria. Mwa anthuwo,anthu makumi awiri,amwalira pa malo ena okwelera basi mtauni ya Gombe ndipo ena asanu ndi mmodzi amwalira ndi...

View Article

Bungwe la NAC Lakana Kulandira Ndalama Kuchokera kwa Anthu Khumi Amalonda

Bungwe lolimbana ndi matenda a Edzi mdziko muno la National Aids Commission NAC,lakana kulandira ndalama zokwana 5 miliyoni kwacha zomwe anthu ena amalonda  anakabweza ku bungwelo mmalo mwa bungwe la...

View Article

Mabungwe Atengepo Mbali pa Ntchito za Ulimi

Ulimi mdziko muno ati ungathe kupita patsogolo mabungwe kuphatikizapo omwe siaboma, atatengapo mbali yaikulu pantchito za ulimi. Mmodzi mwa akuluakulu owona zaulimi mu nthambi ya zaulimi ya Chivala EPA...

View Article


Msikana wa Zaka 13 Wagwidwa ndi Apolisi Mziko la Nigeria Pomuganizira Kuti...

M’sungwana wina wa zaka 13 akuti ali m’manja mwa apolisi mdziko la NIGERIA atamupeza kuti anali m’modzi mwa atsikana amene akhala akugwilitsidwa ntchito ndi zigawenga za gulu la Boko Haram kuti...

View Article

Ambuye Ziyaye Afunila Akhirisitu Ampingo wa Katolika Mafuno Abwino A Khirisimasi

Episcope wa Arch-Diocese ya Lilongwe Ambuye Tarcizio Ziyaye afunila mafuno abwino akhilisimasi kwa akhristu onse ampingowu m’dziko muno. Ambuye Ziyaye anena izi  dzulo utangotha mwambo wa nsembe yamisa...

View Article

Zigawenga Zipha Anthu Oposa Makumi Asanu ndi Limodzi Mdziko la India

 Anthu oposera makumi asanu ndi limodzi afa pakumenyana komwe kwakhala kukuchitika pakati pa mitundu ina m’dziko la India. Nkulu wa apolisi a dzikoli wauza atolankhani m’dzikomo kuti limodzi mwa magulu...

View Article


Anthu Atatu Afa Phanga Litawagumukila Ku Salima

Anthu atatu afa phanga lomwe amakumbamo miyala ya mtengo wapatali ya Garnet litawagumukira  m’boma la Salima. Ofalitsa nkhani za apolisi m’bomali Sergeant Gift Chitowe wati izi zachitika lachinayi pa...

View Article


Asilikali Atatu a Bungwe la African Union Aphedwa Mdziko la Somalia

Asilikali atatu a bungwe la mgwirizano wa maiko a mu Africa la African Union ,aphedwa ndi zigawenga za gulu la Al-shaab kulikulu la bungweli mumzinda wa Mogadishu mdiko la Somalia. Malinga ndi lipoti...

View Article

Ntchito za Kusamalira a Mndende Zayenda Bwino mu Chaka cha 2014

Nthambi yoyang’anira chisamaliro cha anthu ku ndende mu ark-dayosizi ya Blantyre yati ndiyokhutira ndi momwe ntchito zake zayendera mchaka cha 2014. Bambo mlangizi oyang’anira nthambiyi mu...

View Article

Boma Lili ndi Udindo Wosamalira Mabanja

Arkdayosizi ya Blantyre yati boma liri ndi udindo waukulu woonetsetsa kuti mabanja ovomerezeka mdziko muno, akusamalidwa moyenera. Ark-episikopi wa ark-dayosiziyi wolemekezeka Ambuye Thomas Luke Msusa...

View Article

Episkopi wa Archdayosizi ya Lilongwe Wadzudzula Mchitidwe wa Maukwati...

Episkopi wa Arch-diocese ya Lilongwe olemekezeka ambuye Tarcizio Ziyaye wati mchitidwe umene mayiko olemera akumachita polimbikitsa maukwati a pakati pa amuna kapena akazi okhaokha ndi amene...

View Article


Bungwe la MUB Lapindula ndi Ntchito Zake Mu Chaka cha 2014

Chaka cha 2014 akuti chidzakhala chaka chosayiwalika mu mbiri ya bungwe lomenyera ufulu wa anthu osaona la Malawi Union for The Blind (MUB). Mkulu wa bungwelia Ezekiel Kumwenda awuza Radio Maria Malawi...

View Article

Chiwerengero cha Atumiki Ophedwa a Mpingo Wakatolika Chakwera Mdziko la Mexico

Chiwerengero cha ansembe ndi atumiki ena a mpingo wa katolika omwe akhala akuphedwa akuti chakwera kwambiri mdziko la Mexico. Malinga ndi zotsatira za kafukufuku amene bungwe la Catholic Multimedia...

View Article


Mabungwe Olimbikitsa Ufulu Sakugwirizana ndi Ganizo la Ziwonetsero

Mabungwe ena olimbikitsa ufulu wa anthu mchigawo cha kummwera mdziko muno,ati sakugwirizana ndi ziwonetsero zomwe mabungwe ena omenyera ufulu wa anthu akukonza pa 13 mwezi uno wa January. Mkulu...

View Article

Dayosizi ya Mangochi Yati Ana Akuyenera Kuyikidwa Patsogolo mu Nkhani Za Mpingo

Episkopi wa Dayosizi ya Mangochi Ambuye Montfort Sitima ati ana akuyenera kuyikidwa patsogolo pankhani zokhudza mpingo. Ambuye Sitima alankhula izi lachitatu pa msonkhano wa mabungwe a ana otumikira...

View Article


Papa Francisco Wapempha Akhristu kuti Akhale Okonda Kuchita Ntchito za Chifundo

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco wapempha akhristu, kuti aziwonetsa chikhulupiliro chawo, pothandiza anthu ovutika komanso odwala matenda osiyanasiyana. Papa Francisco,...

View Article

Ambuye Stima at Akhristu Akuyenera Kulemekeza Tsiku la Utumiki wa Ana

Episkopi wa Diocese ya Mangochi Ambuye Montfort Stima,ati akhristu a mpingo wakatolika mdziko muno akuyenera kulemekeza tsiku la chaka cha Epifania , lomwe mpingo wakatolika unaliyika mwapadera kuti...

View Article

Makwaya Akuyenera Kutsata Chiphunzitso cha Mpingo pa Kayimbidwe

Magulu oyimba mu mpingo wa katolika ati akuyenera kumayimba nyimbo zawo potsatira chiphunzitso cha mpingowu. Mlangizi woyang’anira za chipembedzo komanso magulu oyimba mu Archdayosizi ya Blantyre Bambo...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>