Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Papa Francisco Akumana ndi Mtsogoleri wa Dziko la Palestine

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse papa Fransiscoanakomana ndi mtsogoleri wa dziko la Palestine ku Vatican pa ulendo wake wokakomana ndi nduna yaikulu ya mdziko la Italy. Malinga ndi...

View Article


Taliban Yatulutsa Kanema Wa Amuna Awiri Amene Akuwasunga

Gulu la za uchifwamba la Taliban ati latulutsa kanema amene akuwonetsa amuna awiri omwe zigawengazi zinawaba ndipo zikuwasunga mokakamiza. Malipoti a wailesi ya BBC ati Kelvin King wa mdziko la America...

View Article


Bambo Hernandez Apezeka Atafa

Wansembe yemwe anasowa masiku apitawa mdziko la Mexico akuti wapezeka atafa mdera lina lotchedwa Parras mdzikolo. Malinga ndi malipoti a CNA wansembeyu Joaqui’n Hernandez  yemwe amatumikira mu dayosizi...

View Article

Mwana Afa Mtengo wa Papaya Utamugwera

Mwana wina wa zaka zitatu wafa mtengo wa zipatso za mapapaya utamugwera m’mudzi mwa Kang’ombe m’dera la mfumu yayikulu Kasakula m’boma la Ntchisi. Wofalitsa nkhani za apolisi m’bomalo,SergeantGladson...

View Article

Zipani Zotsutsa Zidzudzula ma Bank, MRA

Zipani zotsutsa boma m’dziko muno zati zipitiliza ndi ganizo lokakamiza boma kuti lidziunika ndondomeko zomwe ma Bank komanso bungwe lotolera misonkho m’dziko muno la Malawi Revenue Authority...

View Article


Apempha Makhonsolo Athandize Anthu Okhudzidwa Ndi Ngozi Zogwa Mwadzidzidzi

Akuluakulu a makhonsolo onse m’dziko muno awalangiza kuti akonze ndondomeko zabwino zothandizira anthu okhudzidwa ndi ngozi zogwa mwadzidzidzi. Wachiwiri kwa m’tsogoleri wa dziko lino Dr. Saulos...

View Article

MZIHA Ilimbikitsa Ntchito Zokopa Alendo

Bungwe lolimbikitsa za chikhalidwe cha Angoni la Mzimba Heritage Association (MZIHA),lati ligwilitsa bwino ntchito malo odziwika mu mbiri ya mtundu-wu pa ntchito zokopa alendo. Wapampando wa bungweli,...

View Article

Papa Apepesa Okhudzidwa pa Ngozi ya Ndege Mdziko la Hong-Kong

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonsePapa Franciscowapereka uthenga wa chipepeso kwa anthu amene akhudzidwa pa ngozi ya ndege yomwe yagwa mu mzinda waKyrgyzstanmdziko laHong-Kong. Malipoti a...

View Article


Ntchito Yofufuza MH370 Yaimitsidwa

Ntchito yofufuza ndege ya MH370 ya mdziko la Malaysia yomwe inasowa zaka zitatu zapitazo ati ayamba ayiyimitsa. Malinga ndi malipoti a wailesi ya BBC, mayiko a Australia, Malaysia komanso China aganiza...

View Article


Apempha Anthu Apitirize Kugwirana Manja ndi Apolisi

Anthu okhala mdera la mfumu yayikulu Bvumbwe m’boma la Thyolo awapempha kuti apitirize kugwirana manja ndi apolisi pa ntchito yolimbikitsa chitetezo cha ku madera. Mkulu wa apolisi ya m’delari a...

View Article

Sister Mpandira a Chipani Cha Teresian Amwalira

Akulikulu la chipani cha asisisteri chaTeresianmdziko muno alengeza za imfa ya Sister Everina Mpandiraochokera mu parishi yaKanyamamu dayosizi yaDedza. Malinga ndi akulikulu-wa, SisterEverinaanabadwa...

View Article

Cardinal Law Alowa M’manda

Mwambo woyika m’manda m’modzi mwa ma Cardinal a mpingo wakatolika amene anamwalira pa 20 mwezi uno wachitika lero ku likulu la mpingowu ku Vaticanmdziko laItaly. Malinga ndi malipoti a wailesi...

View Article

Dayosizi Ya Mangochi Ichita Chaka Cha Epifania

Mwambo wa chaka cha utumiki wa ana mu dayosizi ya Mangochiwachitikaku parishyaKochemu dayosizi-yi. Malingana ndi mkulu wowona za utumiki wa ana mu dayosizi-yi, mwambo-wu unayamba  ndi mwambo wa  nsembe...

View Article


Khosolo Igwiritsa Ntchito Njira Zamakono Pofalitsa Uthenga Wa Edzi

Ofesi yoona za matenda a Edzi mu mzinda wa Mzuzu yati idzipereka pomwaza mauthenga othandiza pa ntchito zolimbana ndi kufala kwa kachilombo koyambitsa matenda a Edzi ka HIVpogwilitsa ntchito njira...

View Article

Jammeh Watuluka Mdziko la Gambia

Mtsogoleri wakale wa dziko la Gambia, Yahya Jammeh wachoka mdzikolo atavomereza kugonja kwake pa chisankho atalamulira dzikolo kwa zaka 22. Malipoti a wailesi ya BBC ati Jammeh pakadali pano ali mdziko...

View Article


Papa Apempha Akhristu Alimbikitse Umodzi, Apemphelera Okhudzidwa Ndi Zivomerezi

Mtsogoleri wa mpingo wa katolika pa dziko lonse papa Francisco wapempha akhristu kuti agwirane manja popemphelera umodzi  pakati pawo. Malinga ndi malipoti a wailesi ya Vatican ati papa wanena izi...

View Article

Radio Maria Malawi Yakonzeka Kutumikira Omvera Ake Mchaka Cha 2017

Radio Maria Malawiati yakonza ndondomeko zosiyanasiyana pofuna kupititsa patsogolo ntchito za wailesiyi ndi cholinga choti itumikire bwino omvera ake mchaka cha 2017. Mkulu woyendetsa mapologalamuku...

View Article


Anthu 18 Afa Kamba ka Nyengo Yoipa Mdziko la America

Anthu pafupifupi 18 afa ndipo ena ambiri avulala kutsatira nyengo yoipa kum’mwera kwa dziko la America. Malipoti a wailesi ya BBC ati gavanala wa ku Georgia walengeza kuti madera asanu ndi awiri 7...

View Article

Akagwira Jere Zaka Zinayi Kaamba Koba Mbuzi

Bwalo lachiwiri la milandu m’boma la Mangochi, lalamula amuna awiri kuti akakhale kundende ndi kukagwira ntchito yakalavulagaga kwa zaka zinayikaamba kopezeka ndi mulandu wakuba mbuzi. Wapolisi...

View Article

Papa Apempha Akhristu Alimbikitse Umodzi, Apemphelera Okhudzidwa Ndi Zivomerezi

Mtsogoleri wa mpingo wa katolika pa dziko lonse papa Francisco wapempha akhristu kuti agwirane manja popemphelera umodzi  pakati pawo. Malinga ndi malipoti a wailesi ya Vatican ati papa wanena izi...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>