Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

CHURCHES OF CHRIST IKUDZIPEREKA PA NTCHITO ZA CHIFUNDO

Mpingo wa CHURCHES OF CHRIST m’boma la MANGOCHI wati ukudzipeleka kwambiri pogwira ntchito za chifundo pambalinso pogwira ntchito zofalitsa uthenga wa chipulumutso, M`busa Denson Mulaleya wa mpingowu...

View Article


MNYAMATA WA ZAKA 17 APHA MCHEMWALI WAKE KU MANGOCHI

Apolisi m’boma la Mangochi akusunga mchitolokosi  mnyamata wina wa zaka 17 kamba komuganizira kuti anamenya ndikupha mchemwali wake. MneneRi wa apolisi m`bomalo Inspector Rodrick Maida, watsimikizira...

View Article


ANTHU ASAFE NDI NJALA - VOICE OF THYOLO

Bungwe la Voice of Thyolo m`boma la Thyolo, ladzudzula boma, kaamba kolekelera kuti anthu omwe anathawa kudera la Mfumu yayikulu Ngonamo kwa Mfumu yayikulu Thomasi m`bomalo, adzimwalira ndi njala...

View Article

SITIKUTEKESEKA NDIKUCHOKA KWA APHUNGU - DPP

Chipani cha Democratic Progessive {DPP} chati sichikutekeseka  ndikuchoka kwa aphungu ena m'chipanichi kukalowa chipani cholamula cha PP. Mneneri wachipanichi a Nicholas Dausi,anena izi pomwe phungu...

View Article

Kodi Chokhalitsa Nchiyani

New Ulaliki titled Kodi Chokhalitsa Nchiyani by Father Clement Mmana

View Article


Ngakhale Ine Ndili Nduna

Ngakhale ine ndili nduna By Samuel Koloko

View Article

Kuthokoza

Ulaliki titled Kuthokoza by Fr. Joseph Kimu

View Article

Chiminingo Cha Mulungu Chimaposa Cha Munthu Wina aliyense

Ulaliki titled Chiminingo Cha Mulungu Chimaposa Cha Munthu Wina Aliyense by Mai Senia Kaunda

View Article


Maiko Onse Tikondane

Song Maiko Onse Tikondane by St Cecilia Sigerege Of Blantyre Diocese

View Article


Muli Nazo

Song titled Muli nazo by St Cecilia Sigerege of Blantyre  Archdiocese  

View Article

Muli Nazo

Song titled Muli Nazo by St Cecilia Sigerege of Blantyre Archdiocese

View Article

Image may be NSFW.
Clik here to view.

EPISIKOPI WA DAYOSIZI YA BERGAMO AYENDERA RADIO MARIA MALAWI

Episikopi wa diyosizi ya Mangochi ya Mpingo wa Katolika Ambuye Allesandro Pagani ayamikira ubale umene ulipo pakati pa diyosiziyi ndi diyosizi  ya Bergamo m’dziko la Itary.   Ambuye Pagani alakhula izi...

View Article

Mwana Akaona Kanthu

Ulaliki titled Mwana Akaona Kanthu  by Samuel Koloko

View Article


Image may be NSFW.
Clik here to view.

ZIPANI ZA NDALE ZIKHALE NDI MFUNDO ZENIZENI”-DR. CHINSINGA

 Katswiri pankhani zandale yemwenso ndi mphunzitsi kusukulu ya Chancellor College Dr. Blessings Chinsinga wati nthawi yakwana yoti atsogoleri andale komanso zipani ziyambe kukonza ndi kufotokozera a...

View Article

Image may be NSFW.
Clik here to view.

PAPA FRANCIS WATSEKULIRA CHAKA CHA ACHINYAMATA

  Mwambo wa nsembe ya misa yotsekulira chaka cha achinyamata wachitika ku   copacabana mu arch diocese ya Rio ya mpingo wa katolika m’dziko la Brazil. Mtsogoleri wa Mpingo wa katolika pa dziko lonse...

View Article


ANTHU OKWIYA AVULAZA ABALE A MFUMU KU NTCHISI

Anthu ena ozungulira dera la mfumu Chikho mboma la Ntchisi avulaza abale a mfumu ya deralo komanso kuwononga katundu wa ndalama zoposa 117 thousand pokwiya ndi ulamuliro wa mfumuyo. Mneneli wa apolisi...

View Article

Image may be NSFW.
Clik here to view.

AWAPEMPHA KUTI AKALEMBETSE MWAUNYINJI MU KAUNDULA WA CHISANKHO

  Anthu a m’dera la Mfumu Yaikulu Amidu m’boma la Balaka awapempha kuti akalembetse mwaunyinji mu kaundula wa chisankho kuti akhale ndi mwayi wodzaponya voti pa chisankho  cha chaka cha mawa. Mmodzi...

View Article


Image may be NSFW.
Clik here to view.

“MUSALOWETSE CHINYENGO PA NTCHITO ZA CHITUKUKO”-SIMPLEX CHITHYOLA

Mabungwe omwe siaboma amene akugwira ntchito zao m’boma la Balaka, awapempha kuti azigwira ntchito zawo mopanda chinyengo komanso mofuna kutukula miyoyo ya anthu mbomalo. Wapampando watsopano wa komiti...

View Article

NASAF IPEREKA NGONGOLE YA MATRACTOR NGATI NJIRA IMODZI YOPITITSIRA PATSOGOLO...

Mtsogoleri wa chipani cha National Salvation Front NASAF a JAMES NYONDO watsindika kuti ntchito yomwe walonjeza yopeleka ngongole ya ma TRACTOR kwa alimi a m’dziko muno siyankhambakamwa chabe ndipo...

View Article

ZOKONZEKERA MSONKHANO WA AMECEA ZIKUYENDA BWINO

Committee yoyendetsa zokonzekera za msonkhano wa ma Episcopi a chigawo cha ku m'mawa ndi pakati muno mu Africa la AMECEA mu m'zinda wa Lilongwe yati ndiyokhutila ndi zokonzekera za msokhanowu....

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live