Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Ana Atatu Afa Ndipo Anthu Ena 16 Ali Mchipatala Atadya Chakudya cha P

Ana atatu a banja limodzi amwalira m’boma la Ntchisi ndipo anthu ena 16, awagoneka pa chipatala cha boma m’bomalo atadya chakudya chomwe akuchiganizira kuti chinali ndi poyizoni. M’neneri wa apolisi...

View Article


Mabungwe a mu Mpingo Wakatolika Apeza Njira Zodzetsa Umodzi

Msonkhano wa mabungwe ang’onoang’ono a mumpingo wakatolika omwe wakonzedwa ndi mabungwe a ma episkopi mmayiko a Madagascar ndi Africa uli m’kati mdziko la Ghana. Zina mwa mfundo zomwe nthumwi ku...

View Article


Dziko la Malawi Lichita Mwambo Wokumbukira Kulimbana ndi Nkhanza pa Dziko Lonse

Masiku 16 oganizira komanso kulimbana ndi nkhanza za m’banja padziko lonse ayamba lachiwiri pa 25 November. M’masikuwa mayiko amakhala akukumbukira komanso kulingalira nkhanza zosiyanasiyana zomwe...

View Article

Khansa ya Khomo la Chiberekero, Chiwopsezo Cha Miyoyo ya Amayi

Nthenda ya khansa ya mchiberekero akuti ndi imodzi mwa matenda omwe akupitilira kutenga miyoyo ya amayi kamba koti amayi ambiri samapita kukayezetsa kuti adziwe ngati ali ndi matendawa kapena ayi....

View Article

Nthumwi ku Msonkhano wa PAC Zilephera Kumvana Maganizo pa Ulamuliro wa...

Nthumwi kumsonkhano womva maganizo a akuluakulu pankhani yokhudza ulamuliro wamzigawo womwe umachitikira mumzinda wa Blantyre masiku awiri apitawa,zalephera kumvana chimodzi pankhaniyi. Msonkhanowu...

View Article


Unduna Wowona Za Ntchito, Udzudzula za Mchitidwe Wonyanyala Ntchito

Unduna wowona za ntchito m’dziko muno wapempha anthu ogwira ntchito m’boma kuti adzitsatira malamulo akafuna kunyanyala ntchito pamavuto omwe akukumana nawo. Nduna mu undunawu wolemekezeka a Henry...

View Article

Vuto la Madzi Lakula Mdera la Mchesi

Anthu okhala ku Mchesi m’boma la Lilongwe apempha boma kuti liyambe msanga kupereka madzi awukhondo pogwiritsa ntchito mipopi yomwe idamangidwa kale mderalo. Malinga ndi m’modzi mwa anthu okhudzidwa...

View Article

Mabungwe Osakhala a Boma Awuza Akuluakulu a NAC kuti Atule Pansi Maudindo

Mabungwe osiyanasiyana omwe si aboma  apempha akuluakulu a bungwe lowona za matenda a Edzi mdziko muno la National Aids Commission NAC,kuti atule pansi maudindo awo kaamba kolephera ntchito. Mabungwewa...

View Article


Nthambi za Chitetezo Zidzudzula za Imfa ya Msilikali

Nthambi za chitetezo mdziko muno za Polisi ndi Army zadzudzula imfa ya msilikali wa Army yemwe anaphedwa ndi apolisi loweruka pa 22 November nthawi ya 11 koloko usiku mumzinda wa Zomba. Akuluakulu...

View Article


Anthu 15 Afa ndipo 10 Avulala Atawomberedwa

Anthu khumi ndi asanu aphedwa ndinso ena khumi avulala atawomberedwa ndi anthu ena omwe anakwera ngamila mdziko la Sudan. Mmodzi mwa anthu omwe avulala pachiwembucho wawuza atolankhani kuchipatala...

View Article

Zipembedzo Zidzudzula Mchitidwe wa Uchifwamba Mdzina la Chipembedzo

Nthambi zowona ubale wa mipingo ndi zipembedzo kulikulu la mpingo wakatolika komanso kuchisilamu, zadzudzula magulu osiyanasiyana omwe akuchitira anthu zamtopola mudzina la chipembedzo. Magulu awiriwa...

View Article

Nkhanza za Mbanja Zikukolezera Kufala kwa Matenda a Edzi

Bungwe la Southern Africa Aids Trust SAAT lati nkhanza za m’banja ndi vuto limodzi lomwe likukolezera kufala kwa kachilombo ka HIV komwe kamayambitsa matenda a Edzi. Mkulu wabungweli a Robert Mangwazu...

View Article

SWEET SACRAMENT

SWEET SACRAMENT BY ST CECILIA ST PIUS PARISH

View Article


Sinatusi ya Legio ya Maria Ayikhazikitsa ku Maula Cathedral

Episkopi wa Arch dayosizi ya Lilongwe ya mpingo wakatolika Ambuye Tarsizius Ziyaye walimbikitsa ma membala a bungwe la Legio kuti apitilize kudzipereka pogwira ntchito zawo mu mpingo. Ambuye Ziyaye...

View Article

A ku Banja Adzudzula Madonna Polephera Kusunga Lonjezo

Katswiri woyimba nyimbo za chamba cha POP wa mdziko la America Madonna, amudzudzula kamba kolephera kusunga lonjezo lomwe anapereka kwa makolo a mwana yemwe anamutenga mdziko muno kuti akamulere mdziko...

View Article


Sukulu ya Ukachenjede ya DMI Itengapo Mbali Pokweza Maphunziro a Ana

Ena mwa mabungwe omwe siaboma m’boma la Mangochi ayamikira sukulu ya ukachenjede ya St.John The Batist, DMI,kamba koyikanso chidwi pantchito zosula ana msukulu za pulayimale m’bomalo. Mkulu wabungwe la...

View Article

2014 World AIDS Day Message From The Catholic Health Commission of The...

THEME: GETTING TO ZERO 1.0       Preamble Today in the liturgical calendar of the Catholic Church is the first Sunday of Advent. The Church begins a new Liturgical Year, a new journey of faith. The...

View Article


Radio Maria Malawi Ithokoza Akhristu

Wachiwiri kwa mkulu woyang’anira  ma pulogalamu ku Radio Maria Malawi Bambo Charles Kaponya wayamikira akhristu kamba ka chidwi chawo potenga gawo  lothandiza wailesiyi. Bambo Kaponya amalankhula izi...

View Article

Aphunzitsi a Bungwe la Wild Life Society of Malawi Apindula ndi Ulendo Wawo

Gulu la aphunzitsi a bungwe la Wild Life Society of Malawi lochokera ku Mvera m’boma la Dowa lati kuyenda ndi mbali imodzi ya maphunziro. Mkulu wagululi a Morgan Chafulumira Mwale ndi amene alankhula...

View Article

MRA Ichepetsa Mavuto a Msonkho kwa Eni Minibus

Mavuto okhudza misonkho omwe anthu ochita bizinezi ya ma minibus amakumana nawo ati akuyembekezeka kuchepa kamba koti bungwe lotolera misonkho mdziko muno la  Malawi  Revenue Authority (MRA)  lati...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>