Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Dziko la Gambia Ndi Lokonzeka Kuthetsa Mgwirizano Ndi Bungwe la EU

Dziko la Gambia lati ndilokonzeka kuthetsa mgwilizano wake ndi bungwe la European Union (EU) ngati bungweli lipitilize kukakamiza dzikolo, kuvomeleza kuti anthu azichita maukwati apakati pa amuna...

View Article


Anthu Achitepo Kanthu Polimbana ndi Matenda a Edzi

Tsiku lokumbukira matenda a Edzi padziko lonse ati likuyenera kukhala tsiku limene anthu akuyenera kukumbukira kuti matenda a Edzi alipodi, pochitapo kanthu polimbana ndi matendawa.  Wachiwiri kwa...

View Article


YESAYA ADALALIKA

YESAYA DALALIKA BY DONBOSCO WOMEN CHOIR ARCHDIOCESE OF LILONGWE

View Article

Mabungwe a Achinyamata Mdziko Muno Adzudzula Bungwe la NAC

Mabungwe omenyelera ufulu wa  achinyamata mdziko muno apereka masiku khumi ndi anayi 14, kuti mabungwe omwe analandira ndalama kuthumba la bungwe  lowona za matenda a Edzi  la National Aids Commission...

View Article

Mpingo wa Katolika Susintha Chiphunzitso Chake pa Banja

Episkopi wa Arkidayosizi ya Sydney mdziko la Australia Ambuye Anthony Fisher, atsimikizira a khristu a mpingo wakatolika mdzikolo kuti anthu asayembekezere kuti mpingowu, usintha chiphunzitso chake...

View Article


Anthu Olumala Akusowa Zipangizo Zamakono Zogwiritsa Ntchito

Bungwe lowona za ufulu wa anthu olumala la Federation of Disability Organisation in Malawi FEDOMA ladandaula chifukwa cha kusowa kwa zipangizo za makono zomwe anthu olumala angamagwiritse ntchito....

View Article

Mabungwe Apempha Nthambi ya Ukazitape, Beam, Mulhako kuti Abweze Ndalama za NAC

Mabungwe  Manet+, Manerela+,Cedep,Mehen komanso CHRR,alangiza mabungwe omwe adalandira ndalama kubungwe la NAC mosavomerezeka kuti abweze ndalamazi  pasanathe sabata imodzi. Mabungwewa anena izi...

View Article

Bungwe la CAMA Layimitsa Ziwonetsero za BWB

Bungwe lomenyera ufulu wa anthu ogula la Consumers Association of Malawi CAMA, layamba layimitsa ziwonetsero zomwe linakonza kuti zichitike lachinayi pokwiya ndi vuto la madzi lomwe lafika poyipa...

View Article


Dziko la Philippines Likhazikitsa Masiku a Tchuthi Pamene Papa Francisco...

Pamene mtsogoleri wampingo wakatolika padziko lonse Papa Francisco akuyembekezeka kukacheza mdziko la Philippines mwezi wa mawa, meya wa mzinda wa Manila mdzikolo walamula kuti anthu mu mzindawo...

View Article


Papa Francisco Wati Mchitidwe Wozembetsa Anthu ndi Ukapolo Wamakono

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco wati mchitidwe wozembetsa anthu ndi ukapolo wamakono womwe anthu akukumana nawo. Papa Francisco wanena izi lachiwiri kulikulu la mpingo wa...

View Article

Unduna Wofalitsa Nkhani Wapereka Zotsatira za Kafukufuku wa Kubedwa kwa...

Unduna wofalitsa nkhani lachinayi wapereka zotsatira za kafukufuku yemwe amachitika kunyumba ya boma pankhani ya kubedwa kwa ndalama za boma. Kafukufukuyu wasonyeza kuti mtsogoleri wakale wa dziko lino...

View Article

Nkhanza za kwa Ana Zikusokoneza Maphunziro

Ana ambiri akuti akulephera kuchita bwino pa maphunziro awo kamba ka nkhaza zomwe amakumana nazo pa moyo wawo wa tsiku ndi tsiku. Mkulu woona za chitetezo cha ana ku bungwe la Plan International Malawi...

View Article

Mugabe Wachenjeza kuti Achotsa Ntchito omwe Akumukonzera Chiwembu

Mtsogoleri wa dziko la Zimbabwe Robert Gabriel Mugabe wachenjeza kuti achotsa ntchito komanso kulanga aliyense yemwe angadziwike kuti akukonza zomuchitira chiwembu. Pulezidenti Mugabe wanena izi...

View Article


Mabungwe a Ufulu wa Achinyamata Awopseza kuti Achita Ziwonetsero

Mabungwe anayi owona za ufulu wa achinyamata omwe akugwilira ntchito zawo mchigawo chakumpoto, awopseza kuti achita ziwonetsero ngati mabungwe omwe adatenga ndalama kubungwe la NAC mosavomerezeka,...

View Article

Maria Ukuliranji.

View Article


Satana Samatigwira koma Amatikopa

View Article

Atsikana omwe Anasiyira Sukulu Panjira Ali ndi Mwayi Wopitiriza Maphunziro

Atsikana amene anasiyira sukulu panjira kamba ka zifukwa zosiyanasiyana akuti ali ndi mwayi wotha kukapitiliza maphunziro awo ndi thandizo lochokera ku  bungwe lomwe angolikhadzikitsa kumene la...

View Article


Bungwe la Chilungamo ndi Mtendere CCJP Silikukhutira ndi Kayendetsedwe ka...

Bungwe la Chilungamo ndi Mtendere CCJP mu mpingo wakatolika lati silokhutira ndi momwe boma likuyendetsera ntchito zake pofuna kutukula miyoyo ya anthu mdziko muno. Bungweli lanena izi kudzera...

View Article

Akhristu a Parish ya St.Charles Lwanga ku Zomba Athandiza Radio Maria Malawi

Akhristu a mu Parish ya St.Charles Lwanga  mu dayosizi ya Zomba awayamikira chifukwa  chothandiza Radio Maria Malawi. Bambo Patrick Mwaliwa amalankhula izi pa mwambo wa  misa ya promotion womwe...

View Article

A Polisi Asanu ndi Anayi Amwalira Pangozi Ya Panseu

Mtsogoleri wadziko lino Professor Arthur Peter Mutharika wati ndi wokhumudwa kwambiri ndi imfa ya apolisi asanu ndi anayi  omwe amwalira loweruka pangozi ya galimoto m’boma la Balaka. Malinga ndi...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>